< Masalimo 13 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
How long, O Jehovah? Will thou forget me forever? How long will thou hide thy face from me?
2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
How long shall I take counsel in my soul, having sorrow in my heart all the day? How long shall my enemy be exalted over me?
3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
Consider and answer me, O Jehovah my God. Lighten my eyes, lest I sleep the death,
4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
lest my enemy say, I have prevailed against him, lest my adversaries rejoice when I am moved.
5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
But I have trusted in thy loving kindness. My heart shall rejoice in thy salvation.
6 Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.
I will sing to Jehovah because he has dealt bountifully with me.

< Masalimo 13 >