< Masalimo 131 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
Jehovah, my heart is not haughty, nor my eyes lofty. Neither do I exercise myself in grand matters, or in things too wonderful for me.
2 Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
Surely I have stilled and quieted my soul like a weaned child with his mother. Like a weaned child is my soul within me.
3 Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
O Israel, hope in Jehovah from this time forth and for evermore.

< Masalimo 131 >