< Masalimo 70 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
Bože, pohitaj da me izbaviš, Gospode, da mi pomožeš!
2 Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
Nek se postide i posrame koji traže dušu moju! Nek ustupe natrag, i osramote se koji mi zlo žele!
3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
Sa stidom nek se vrate natrag koji mi govore: ha! ha!
4 Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
Nek se tješe i vesele tobom koji traže tebe, i koji ljube spasenje tvoje, neka jednako govore: velik je Bog!
5 Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.
A ja sam ništ i ubog, Bože, pohitaj k meni! ti si pomoæ moja i izbavitelj moj, Gospode, ne èasi!

< Masalimo 70 >