< Masalimo 120 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
A Song of Degrees. In mine affliction I cried to the Lord, and he hearkened to me.
2 Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
Deliver my soul, O Lord, from unjust lips, and from a deceitful tongue.
3 Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
What should be given to thee, and what should be added to thee, for [thy] crafty tongue?
4 Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
Sharpened weapons of the mighty, with coals of the desert.
5 Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
Woe is me, that my sojourning is prolonged; I have tabernacled among the tents of Kedar.
6 Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
My soul has long been a sojourner;
7 Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.
I was peaceable among them that hated peace; when I spoke to them, they warred against me without a cause.

< Masalimo 120 >