< Masalimo 11 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mwa Yehova ine ndimathawiramo. Nanga mungathe bwanji kunena kwa ine kuti, “Thawira ku phiri lako ngati mbalame.
U Gospoda se uzdam; zašto govorite duši mojoj: “leti u goru kao ptica;
2 Pakuti taona oyipa akunga mauta awo; ayika bwino mivi yawo pa zingwe za uta, pobisala pawo kuti alase olungama mtima.
Jer evo grješnici nategoše luk, zapeše strijelu svoju za tetivu, da iz mraka strijeljaju prave srcem.
3 Tsono ngati maziko awonongeka, olungama angachite chiyani?”
Kad su raskopani temelji, šta æe uèiniti pravednik?”
4 Yehova ali mʼNyumba yake yoyera; Yehova ali pa mpando wake waufumu kumwamba. Iye amayangʼanitsitsa ana a anthu; maso ake amawayesa.
Gospod je u svetom dvoru svom, prijesto je Gospodnji na nebesima; oèi njegove gledaju; vjeðe njegove ispituju sinove èovjeèije.
5 Yehova amayesa olungama, koma moyo wake umadana ndi oyipa, amene amakonda zachiwawa.
Gospod ispituje pravednoga; a bezbožnoga i kojemu je milo èiniti zlo nenavidi duša njegova.
6 Iye adzakhuthulira pa oyipa makala amoto ndi sulufule woyaka; mphepo yotentha idzakhala yowayenera.
Pustiæe na bezbožnike dažd od živoga ugljevlja, ognja i sumpora; i ognjeni vjetar biæe im dio iz èaše;
7 Pakuti Yehova ndi wolungama, Iye amakonda chilungamo; ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake.
Jer je Gospod pravedan, ljubi pravdu; lice æe njegovo vidjeti pravednici.

< Masalimo 11 >