< Masalimo 12 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide. Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika; okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
Pomagaj, Gospode; jer nesta svetijeh, jer je malo vjernijeh meðu sinovima èovjeèijim.
2 Aliyense amanamiza mʼbale wake; ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.
Laž govore jedan drugome, usnama lažljivijem govore iz srca dvolièna.
3 Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo ndi pakamwa paliponse podzikuza.
Istrijebiæe Gospod sva usta lažljiva, jezik velièavi,
4 Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu; pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
Ljude, koji govore: jezikom smo jaki, usta su naša u nas, ko je gospodar nad nama?
5 “Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu ndi kubuwula kwa anthu osowa, Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova, “Ndidzawateteza kwa owazunza.”
Videæi stradanje nevoljnih i uzdisanje ništih, sad æu ustati, veli Gospod, i izbaviti onoga kome zlobe.
6 Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi, oyengedwa kasanu nʼkawiri.
Rijeèi su Gospodnje rijeèi èiste, srebro u vatri oèišæeno od zemlje, sedam puta pretopljeno.
7 Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.
Ti æeš nas, Gospode, odbraniti, i saèuvati nas od roda ovoga dovijeka.
8 Oyipa amangoyendayenda ponseponse anthu akamayamikira zochita zawo.
Bezbožnici idu naokolo; kad se oni podižu, sramote se sinovi èovjeèiji.

< Masalimo 12 >