< Numeri 6 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
And the Lord spak to Moises and seide, Speke thou to the sones of Israel,
2 “Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Ngati mwamuna kapena mkazi afuna kuchita lonjezo lapadera, lonjezo lodzipatula yekha kwa Yehova ngati Mnaziri,
and thou schalt seie to hem, Whanne a man ether a womman makith auow, that thei be halewid, and thei wolen halewe hem silf to the Lord,
3 sayenera kumwa vinyo kapena zakumwa zosasa ndipo asamamwe chakumwa chilichonse cha mphesa. Asamamwe madzi a mphesa kapena kudya mphesa zaziwisi kapena zowuma.
thei schulen absteyne fro wyn and fro al thing that may make drunkun; thei schulen not drynke vynegre of wyn, and of ony other drynkyng, and what euer thing is pressid out of the grape; thei schulen not ete freisch grapis and drie,
4 Pa nthawi yonse imene ali Mnaziri, asamadye chilichonse chopangidwa kuchokera ku mphesa ngakhale mbewu zake kapena makungu ake.’
alle dayes in whiche thei ben halewid bi a vow to the Lord; thei schulen not ete what euer thing may be of the vyner, fro a grape dried `til to the draf.
5 “‘Pa nthawi yonse ya lonjezo lodzipatula yekhalo, asamete kumutu kwake ndi lumo. Akhale wopatulika mpaka nthawi yake yonse ya kudzipatula yekha kwa Yehova itatha. Alileke tsitsi la pamutu pake kuti likule.’
In al tyme of his departyng a rasour schal not passe on his heed, `til to the day fillid in which he is halewid to the Lord; he schal be hooli while the heer of his heed `schal wexe.
6 Pa nthawi yonse imene munthuyo wadzipatula yekha kwa Yehova asayandikire mtembo.
In al the tyme of his halewing he schal not entre on a deed bodi,
7 Ngakhale abambo ake kapena amayi ake kapena mchimwene wake kaya mchemwali wake atamwalira, asadzidetse pokhudza mitembo yawo chifukwa kulumbira kwake kwa kudzipatula yekha kwa Yehova kuli pamutu pake.
and sotheli he schal not be defoulid on the deed bodi of fadir and of moder, of brothir and of sistir, for the halewyng of his God is on his heed;
8 Munthuyo ndi wopatulika masiku onse odzipereka kwake kwa Yehova.
ech dai of his departyng schal be hooli to the Lord.
9 “Ngati munthu wina afa mwadzidzidzi pafupi naye ndi kudetsa tsitsi lake loperekedwalo, amete mutu wake pa tsiku lodziyeretsa, tsiku lachisanu ndi chiwiri.
But if ony man is deed sudeynly bifore hym, the heed of his halewyng schal be defoulid, which he schal schaue anoon in the same dai of his clensyng, and eft in the seuenthe dai;
10 Tsono pa tsiku lachisanu ndi chitatu abweretse nkhunda ziwiri kapena mawunda awiri anjiwa kwa wansembe pa khomo lolowera ku tenti ya msonkhano.
forsothe in the eiyte dai he schal offre twei turtlis, ether twei `briddis of a culuer, to the preest, in the entryng of the boond of pees of witnessyng.
11 Wansembe apereke imodzi kuti ikhale nsembe yauchimo ndi ina nsembe yopsereza yotetezera tchimo chifukwa anachimwa popezeka pafupi ndi mtembo. Ndipo tsiku lomwelo apatulenso tsitsi la pamutu pake.
And the preest schal make oon for synne, and the tothir in to brent sacrifice; and the preest schal preie for hym, for he synnede on a deed bodi, and he schal halewe his heed in that dai.
12 Adzipereke kwa Yehova pa nthawi yodzipatula ndipo abweretse nkhosa yayimuna ya chaka chimodzi ngati nsembe yopepesera. Masiku akale sawerengedwanso chifukwa anadzidetsa pa nthawi yodzipatulira kwake.
And he schal halewe to the Lord the daies of his departyng, and he schal offre a lomb of o yeer for synne, so netheles that the formere daies be maad voide, for his halewyng is defoulid.
13 “Tsono ili ndi lamulo la Mnaziri pamene nthawi yodzipatula kwake yatha: Abwere naye pa khomo la tenti ya msonkhano.
This is the lawe of consecracioun. Whanne the daies schulen be fillid, whiche he determynede by a vow, the preest schal brynge hym to the dore of the tabernacle of boond of pees, and schal offre his offryng to the Lord,
14 Pamenepo apereke chopereka chake kwa Yehova: Nkhosa yayimuna ya chaka chimodzi yopanda chilema kuti ikhale nsembe yopsereza, mwana wankhosa wamkazi mmodzi wopanda chilema kuti ikhale nsembe yauchimo, ndi nkhosa imodzi yayikulu yayimuna kuti ikhale nsembe yachiyanjano,
a lomb of o yeer with out wem, in to brent sacrifice, and a scheep of o yeer with outen wem, for synne, and a ram with out wem, a pesible sacrifice;
15 ndipo abwere pamodzi ndi nsembe yachakudya ndi nsembe yachakumwa ndi dengu la buledi wopanda yisiti, makeke opangidwa ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, ndi timitanda ta buledi topakidwa mafuta.
also a panyere of theerf looues, that ben spreynt togidere with oile, and cakis sodun in watir, and aftir anoyntid with oile, with out sourdow, and fletyng sacrifices of alle bi hem silf;
16 “Wansembe apereke zimenezi pamaso pa Yehova ndi kuchita nsembe ya uchimo ndi nsembe yopsereza.
whiche the preest schal offre bifor the Lord, and schal make as wel for synne as in to brent sacrifice.
17 Apereke dengu la buledi wopanda yisiti ndiponso nsembe yachiyanjano kwa Yehova ya nkhosa yayimuna, pamodzi ndi chopereka cha chakudya ndi chopereka cha chakumwa.
Sotheli he schal offre the ram a pesible sacrifice to the Lord, and he schal offre togidere a panyere of therf looues and fletyng sacryfices, that ben due bi custom.
18 “Mnaziriyo amete tsitsi limene analipereka lija pa khomo la tenti ya msonkhano. Atenge tsitsilo ndi kuliyika pa moto umene uli pansi pa nsembe yachiyanjano.
Thanne the Nazarei schal be schauun fro the heer of his consecracioun, bifor the doore of the tabernacle of boond of pees; and the preest schal take hise heeris, and schal putte on the fier, which is put vndur the sacrifice of pesible thingis.
19 “Mnaziriyo atatha kumeta tsitsi analiperekalo, wansembe ayike mʼmanja mwake mwendo wa mmwamba wankhosa yayimuna umene waphikidwa ndipo atengenso keke ndi kamtanda ka buledi, zonse zopanda yisiti zomwe zili mʼdengu lija.
And he schal take the schuldur sodun of the ram, and o `cake of breed with out sourdow fro the panyere, and o theerf caak first sodun in watir and aftirward fried in oile, and he schal bitake in the hondis of the Nazarei, aftir that his heed is schauun.
20 Wansembe aziweyule pamaso pa Yehova ngati nsembe yoweyula. Zimenezi ndi zopatulika ndipo ndi za wansembe pamodzi ndi chidale chimene anachiweyula ndi ntchafu yomwe anayipereka ija. Zitatha izi, Mnaziri akhoza kumwa vinyo.
And the preest schal reise in the `siyt of the Lord the thingis takun eft of hym. And the thingis halewid schulen be the preestis part, as the brest which is comaundid to be departid, and the hipe. Aftir these thingis the Nasarey may drynke wyn.
21 “Ili ndi lamulo la Mnaziri yemwe walonjeza kudzipereka kwa Yehova podzipatula yekha kuphatikiza pa zomwe angathe kukwaniritsa. Ayenera kukwaniritsa lonjezo lomwe wachitalo potsata lamulo la Mnaziri.”
This is the lawe of the Nasarei, whanne he hath avowyd his offryng to the Lord in the tyme of his consecracioun, outakun these thingis whiche his hond fyndith. By this that he avowide in soule, so he schal do, to the perfeccioun of his halewyng.
22 Yehova anawuza Mose kuti,
And the Lord spak to Moyses and seide,
23 “Uza Aaroni ndi ana ake aamuna kuti, ‘Umu ndi mmene muzidalitsira Aisraeli. Muzinena kuti,
Speke thou to Aaron and to hise sones, Thus ye schulen blesse the sones of Israel, and ye schulen seie to hem,
24 “‘Yehova akudalitse ndi kukusunga;
The Lord blesse thee, and kepe thee;
25 Yehova awalitse nkhope yake pa iwe, nakuchitira chisomo;
the Lord schewe his face to thee, and haue mercy on thee;
26 Yehova akweze nkhope yake pa iwe, nakupatse mtendere.’”
the Lord turne his cheer to thee, and yyue pees to thee.
27 Choncho akadzatchula dzina langa podalitsa Aisraeli, Ine ndidzawadalitsadi.
Thei schulen clepe inwardli my name on the sones of Israel, and Y schal blesse hem.

< Numeri 6 >