< 2 Mbiri 27 >

1 Yotamu anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16. Dzina la amayi ake linali Yerusa mwana wa Zadoki.
Dvadeset i pet godina bijaše Jotamu kad poèe carovati, i carova šesnaest godina u Jerusalimu; materi mu bješe ime Jerusa, kæi Sadokova.
2 Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga anachitira Uziya abambo ake, kupatula kuti iyeyo sanalowe mʼNyumba ya Yehova. Komabe anthu anapitirira kuchita zoyipa.
On èinjaše što je pravo pred Gospodom sasvijem kako je èinio Ozija otac njegov, samo što ne uðe u crkvu Gospodnju; ali narod još bijaše pokvaren.
3 Yotamu anamanganso chipata chakumtunda cha Nyumba ya Yehova ndipo anagwira ntchito yayikulu yomanga khoma la ku phiri la Ofeli.
On naèini visoka vrata na domu Gospodnjem, i na zidu Ofilu mnogo nazida.
4 Iye anamanga mizinda mʼmapiri a ku Yuda ndipo anamanganso malinga ndi nsanja mʼmadera a ku nkhalango.
Još sazida i gradove u gori Judinoj, i u šumama pogradi dvorove i kule.
5 Yotamu anachita nkhondo ndi mfumu ya Aamoni ndipo anawagonjetsa. Chaka chimenecho Aamoni anapereka makilogalamu 3,400, matani 1,000 a tirigu ndiponso matani 1,000 a barele. Aamoni anabweretsa zinthu zomwezi chaka chachiwiri ndi chachitatu.
I vojeva s carem sinova Amonovijeh i svlada ih; i dadoše mu sinovi Amonovi one godine sto talanata srebra i deset tisuæa kora pšenice i jeèma deset tisuæa. Toliko mu dadoše sinovi Amonovi i druge i treæe godine.
6 Yotamu anakula mphamvu chifukwa anayenda molungama pamaso pa Yehova Mulungu wake.
I tako osili Jotam, jer upravi putove svoje pred Gospodom Bogom svojim.
7 Zina ndi zina zokhudza ulamuliro wa Yotamu, kuphatikizapo nkhondo zake zonse ndi zinthu zina zimene anachita, zinalembedwa mʼbuku la mafumu a Israeli ndi Yuda.
A ostala djela Jotamova i svi ratovi njegovi i putovi njegovi, eno su zapisani u knjizi o carevima Izrailjevijem i Judinijem.
8 Iye anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16.
Dvadeset i pet godina bješe mu kad poèe carovati, i carova šesnaest godina u Jerusalimu.
9 Yotamu anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda mu Mzinda wa Davide. Ndipo Ahazi mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
I poèinu Jotam kod otaca svojih, i pogreboše ga u gradu Davidovu; a na njegovo se mjesto zacari Ahaz sin njegov.

< 2 Mbiri 27 >