< 1 Mbiri 25 >

1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
I odvoji David s vojvodama za službu sinove Asafove i Emanove i Jedutunove, koji æe prorokovati uz gusle i psaltire i kimvale; i biše izmeðu njih izbrojeni ljudi za posao u svojoj službi:
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
Od sinova Asafovijeh: Zahur i Josif i Netanija i Asarila, sinovi Asafovi, pod rukom Asafa, koji prorokovaše po naredbi carevoj;
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
Od Jedutuna: šest sinova Jedutunovijeh: Gedalija i Sorije i Jesaija, Asavija i Matatija i Simej pod rukom oca svojega Jedutuna, koji prorokovaše uz gusle hvaleæi i slaveæi Gospoda;
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
Od Emana: sinovi Emanovi: Vukija, Matanija, Ozilo, Sevuilo i Jerimot, Ananija i Ananije, Elijata, Gidaltija i Romamti-Ezer, Josvekasa, Malotije, Otir i Maziot.
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
Ti svi bijahu sinovi Emana vidioca careva u rijeèima Božijim da se uzvišuje rog; jer Bog dade Emanu èetrnaest sinova i tri kæeri.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
Svi oni bijahu pod rukom oca svojega pjevajuæi u domu Gospodnjem uz kimvale i psaltire i gusle za službu u domu Božijem, kako car nareðivaše Asafu i Jedutunu i Emanu.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
I bješe ih na broj s braæom njihovom obuèenom pjesmama Gospodnjim, dvjesta i osamdeset i osam, samijeh vještaka.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
I baciše ždrijeb za službu svoju, mali kao veliki, uèitelj kao uèenik;
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
I pade prvi ždrijeb za Asafa na Josifa, drugi na Gedaliju s braæom i sinovima njegovijem, njih dvanaest;
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
Treæi na Zahura, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
Èetvrti na Iserija, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
Peti na Netaniju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
Šesti na Vukiju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
Sedmi na Jesarilu, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
Osmi na Jesaiju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
Deveti na Mataniju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
Deseti na Simeja, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
Jedanaesti na Azareila, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
Dvanaesti na Asaviju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
Trinaesti na Savuila, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
Èetrnaesti na Matatiju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
Petnaesti na Jeremota, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
Šesnaesti na Ananiju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
Sedamnaesti na Josvekasu, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
Osamnaesti na Ananija, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
Devetnaesti na Malotija, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
Dvadeseti na Elijatu, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
Dvadeset prvi na Otira, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
Dvadeset drugi na Gidaltiju, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
Dvadeset treæi na Maziota, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest;
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.
Dvadeset èetvrti na Romamti-Ezera, sinove njegove i braæu njegovu, njih dvanaest.

< 1 Mbiri 25 >