< 1 Mbiri 24 >

1 Magulu a ana a Aaroni anali awa: Ana a Aaroni anali Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.
A meðu sinovima Aronovijem ovi su redovi: sinovi Aronovi bjehu Nadav i Avijud, Eleazar i Itamar.
2 Koma Nadabu ndi Abihu anamwalira abambo awo asanamwalire, ndipo analibe ana aamuna. Kotero Eliezara ndi Itamara ankatumikira monga ansembe.
Ali Nadav i Avijud umriješe prije oca svojega i nemahu djece; zato biše sveštenici Eleazar i Itamar.
3 Mothandizidwa ndi Zadoki chidzukulu cha Eliezara ndi Ahimeleki chidzukulu cha Itamara, Davide anawagawa mʼmagulu molingana ndi ntchito yawo yotumikira.
I razdijeli ih David: Sadoka, koji bijaše od sinova Eleazarovijeh, i Ahimeleha, koji bijaše od sinova Itamarovijeh, po redu njihovu u službi njihovoj.
4 Atsogoleri ambiri anapezeka pakati pa zidzukulu za Eliezara kusiyana ndi zidzukulu za Itamara ndipo anagawidwa moyenera: atsogoleri 16 a mabanja ochokera kwa Eliezara, ndipo atsogoleri asanu ndi atatu a mabanja ochokera kwa zidzukulu za Itamara.
I naðe se sinova Eleazarovijeh više poglavica nego sinova Itamarovijeh, kad ih razdijeliše: od sinova Eleazarovijeh bijaše poglavica po domovima otaèkim šesnaest, a od sinova Itamarovijeh osam po domovima otaèkim.
5 Anawagawa mosakondera pochita maere, pakuti iwo anali akuluakulu a ku malo opatulika ndi akuluakulu a Mulungu pakati pa zidzukulu za Eliezara ndi Itamara.
I biše razdijeljeni ždrijebom i jedan i drugi; jer poglavari u svetinji i poglavari pred Bogom bijahu i od sinova Eleazarovijeh i od sinova Itamarovijeh.
6 Mlembi Semaya mwana wa Netaneli, Mlevi, analemba mayina awo pamaso pa mfumu ndi akuluakulu ake: wansembe Zadoki, Ahimeleki mwana wa Abiatara ndi atsogoleri a mabanja a ansembe ndiponso Alevi, banja limodzi kuchokera kwa Eliezara kenaka limodzi kuchokera kwa Itamara.
I popisa ih Semaja sin Natanailov pisar od plemena Levijeva pred carem i knezovima i Sadokom sveštenikom i Ahimelehom sinom Avijatarovijem i pred poglavarima porodica otaèkih meðu sveštenicima i Levitima, jedan dom otaèki uzevši za Eleazara a jedan za Itamara.
7 Maere woyamba anagwera Yehoyaribu, achiwiri anagwera Yedaya,
I pade prvi ždrijeb na Jojariva, drugi na Jedaju,
8 achitatu anagwera Harimu, achinayi anagwera Seorimu,
Treæi na Harima, èetvrti na Seorima,
9 achisanu anagwera Malikiya, achisanu ndi chimodzi anagwera Miyamini,
Peti na Malhiju, šesti na Mejamina,
10 achisanu ndi chiwiri anagwera Hakozi, achisanu ndi chitatu anagwera Abiya,
Sedmi na Akosa, osmi na Aviju,
11 achisanu ndi chinayi anagwera Yesuwa, a khumi anagwera Sekaniya,
Deveti na Isuja, deseti na Sehaniju,
12 a 11 anagwera Eliyasibu, a 12 anagwera Yakimu,
Jedanaesti na Elijasiva, dvanaesti na Jakima,
13 a 13 anagwera Hupa, a 14 anagwera Yesebeabu,
Trinaesti na Ufu, èetrnaesti na Jesevava,
14 a 15 anagwera Biliga, a 16 anagwera Imeri,
Petnaesti na Vilgu, šesnaesti na Imira,
15 a 17 anagwera Heziri, a 18 anagwera Hapizezi,
Sedamnaesti na Ezira, osamnaesti na Afisisa,
16 a 19 anagwera Petahiya, a 20 anagwera Ezekieli,
Devetnaesti na Petaju, dvadeseti na Jezekila,
17 a 21 anagwera Yakini, a 22 anagwera Gamuli,
Dvadeset prvi na Jahina, dvadeset drugi na Gamula,
18 a 23 anagwera Delaya, ndipo a 24 anagwera Maaziya.
Dvadeset treæi na Delaju, dvadeset èetvrti na Maziju.
19 Umu ndi mmene anasankhidwira kuti azigwira ntchito yotumikira pamene alowa mʼNyumba ya Yehova, motsatira dongosolo limene anapatsidwa ndi kholo lawo Aaroni, monga momwe Yehova Mulungu wa Israeli anamulamulira.
To je red njihov za službu njihovu, kojim idu u dom Gospodnji na posao svoj po naredbi Arona oca svojega, kako mu bješe zapovjedio Gospod Bog Izrailjev.
20 Za zidzukulu zina zonse za Levi: Kuchokera kwa ana a Amramu: Subaeli; kuchokera kwa ana a Subaeli: Yehideya.
A od ostalijeh sinova Levijevih bijaše od sinova Amramovijeh Suvailo; od sinova Suvailovijeh Jedaja,
21 Kwa Rehabiya, kuchokera kwa ana ake: Mtsogoleri anali Isiya.
Od Reavije, od sinova Reavijinih poglavar Jesija;
22 Kuchokera ku banja la Izihari: Selomoti; kuchokera kwa ana a Selomoti: Yahati.
Od sinova Isarovijeh Selomot, od sinova Selomotovijeh Jat;
23 Ana a Hebroni: woyamba anali Yeriya, wachiwiri anali Amariya, wachitatu anali Yahazieli ndipo Yekameamu anali wachinayi.
A od sinova Jerijinih Amarija drugi, Jazilo treæi, Jekameam èetvrti;
24 Mwana wa Uzieli: Mika; kuchokera kwa ana a Mika: Samiri.
Od sinova Uzilovijeh Miha; od sinova Mišinijeh Samir;
25 Mʼbale wa Mika: Isiya; kuchokera kwa ana a Isiya: Zekariya.
Brat Mišin Jesija; od sinova Jesijinih Zaharija.
26 Ana a Merari: Mahili ndi Musi. Mwana wa Yaaziya: Beno.
Sinovi Merarijevi: Malije i Musije; od sinova Jazijinih Veno.
27 Ana a Merari: Kuchokera kwa Yaaziya: Beno, Sohamu, Zakuri ndi Ibiri.
Sinovi Merarijevi od Jazije: Veno i Soam i Zahur i Ivrije;
28 Kuchokera kwa Mahili: Eliezara, amene analibe ana aamuna.
Od Malija Eleazar, koji nemaše sinova;
29 Kuchokera kwa Kisi: Mwana wa Kisi: Yerahimeeli.
Od Kisa, od sinova Kisovijeh: Jerameilo;
30 Ndipo ana a Musi: Mahili, Ederi ndi Yerimoti. Awa anali Alevi potsata mabanja a makolo awo.
I od sinova Musijevih Malije i Eder i Jerimot. To bijahu sinovi Levitski po domovima otaca svojih.
31 Iwonso anachita maere, monga anachitira abale awo, zidzukulu za Aaroni, pamaso pa mfumu Davide, ndi Zadoki ndi Ahimeleki, atsogoleri a mabanja a ansembe ndi Alevi. Mabanja a mwana wamkulu anachita nawo mofanana ndi a mwana wamngʼono.
I oni bacaše ždrijeb prema braæi svojoj, sinovima Aronovijem, pred Davidom i Sadokom i Ahimelehom i poglavarima domova otaèkih meðu sveštenicima i Levitima, od domova otaèkih svaki poglavar prema bratu svojemu mlaðemu.

< 1 Mbiri 24 >