< Tito 2 >

1 Ngem sika, ibagam ti maitutop nga addaan iti napudno a panursuro.
Koma iwe uziphunzitsa zogwirizana ndi chiphunzitso choona.
2 Dagiti lallakay ket masapul a managteppel, natakneng, nanakem, nasimbeng iti pammati, iti ayat, ken iti panagibtur.
Phunzitsa amuna achikulire kuti akhale osaledzera, aulemu wawo, odziletsa, okhwima mʼchikhulupiriro, mʼchikondi ndi mʼkupirira.
3 Kasta met dagiti natataengan a babbai a masapul a kanayon nga iparangda dagiti bagbagida kas mararaem, saan a mammadpadakes. Masapul a saanda a paigamer iti adu nga arak. Masapul nga isuroda ti naimbag
Chimodzimodzinso, phunzitsa amayi achikulire kuti akhale aulemu mʼmakhalidwe awo, asakhale osinjirira anzawo kapena zidakwa, koma akhale alangizi abwino.
4 tapno maisuroda dagiti ubbing a babae nga ayatenda iti naimbag a wagas dagiti bukodda nga assawa ken annak.
Tsono atha kulangiza amayi achichepere kukonda amuna awo ndi ana awo.
5 Masapul nga isuroda ida nga agbalin a nanakem, nasin-aw, nasayaat a mangaywan ti balay, ken agtulnogda kadagiti bukodda nga assawa. Masapul nga aramidenda dagitoy a banbanag tapno saan a maumsi ti sao ti Dios.
Kuwaphunzitsa kukhala odziletsa ndi oyera mtima, osamala bwino mabanja awo, okoma mtima, ndi ogonjera amuna awo. Choncho palibe amene adzanyoze mawu a Mulungu.
6 Iti isu met laeng a wagas, allukoyem dagiti agtutubo a lallaki nga agbalin a nanakem.
Momwemonso, uwalimbikitse amuna achichepere kuti akhale odziletsa.
7 Iti amin a wagas iparangmo ti bagim a kas pagulidanan dagiti nasayaat nga ar-aramid; ken no agisuroka, ipakitam ti kinadalus ken kinatakneng.
Pa zonse iwe mwini ukhale chitsanzo pa ntchito zabwino. Pa chiphunzitso chako uwonetsa kuona mtima ndi kutsimikiza mtima kwako.
8 Agibagaka iti mensahe a nasayaat ken awan pakababalawanna tapno ti siasinoman a bumusor ket maibabain, gapu ta awan iti dakes a maibagana maipanggep kadatayo.
Phunzitsa choonadi kuti anthu asapeze chokutsutsa, motero wotsutsana nawe adzachita manyazi chifukwa adzasowa kanthu koyipa kuti atinenere.
9 Dagiti tagabu ket masapul nga agtulnog kadagiti amoda iti amin a banag. Masapul nga ay-aywenda isuda, ken saan a makisuppiat kadakuada.
Phunzitsa akapolo kuti azigonjera ambuye awo mu zinthu zonse ndi kuwakondweretsa. Asamatsutsane nawo
10 Masapul a saanda nga agtakaw. Ngem ketdi, masapul nga ipakitada ti amin a nasayaat a pammati, tapno mapapintasda iti amin a wagas dagiti sursurotayo maipanggep iti Dios a manangisalakantayo.
kapena kumawabera, koma adzionetse kuti ndi odalirika, motero pa zochita zawo zonse adzaonetsa ubwino wa chiphunzitso cha Mulungu, Mpulumutsi wathu.
11 Ta nagparang ti parabur ti Dios kadagiti amin a tattao.
Pakuti chisomo cha Mulungu chimene chimapulumutsa chaonekera kwa anthu onse.
12 Isursuronatayo daytoy a tumallikod iti saan a nadiosan, ken nainlubongan a tarigagay. Ken isursuronatayo nga agbiag a nanakem, nalinteg, ken iti nadiosan a wagas iti daytoy a panawen (aiōn g165)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn g165)
13 kabayatan nga ur-urayentayo nga awaten ti nagasat a namnama, ti panagparang ti dayag ti naindaklan a Diostayo ken Manangisalakan a ni Jesu-Cristo.
pamene tikudikira chiyembekezo chodala; kuonekera kwa ulemerero wa Mulungu wathu wamkulu ndi Mpulumutsi, Yesu Khristu,
14 Inted ni Jesus ti bagina para kadatayo tapno subbotennatayo manipud iti amin nga awanan ti linteg ken tapno pagbalinennatayo a nasin-aw, para kenkuana, a naisangsangayan a tattao a nagagar a mangaramid kadagiti nasayaat nga ar-aramid.
amene anadzipereka yekha chifukwa cha ife kutiwombola ku zoyipa zonse ndi kudziyeretsera yekha anthu amene ndi akeake, achangu pa ntchito yabwino.
15 Ibagam ken iballakadmo dagitoy a banbanag. Mangtubngarka nga addaan iti amin a turay. Saanmo nga itulok nga adda manglaksid kenka.
Tsono zimenezi ndi zinthu zomwe uyenera kuphunzitsa. Uziwalimbikitsa anthu ndi kuwatsutsa komwe. Uzichita zimenezi ndi ulamuliro wonse. Wina aliyense asakupeputse ayi.

< Tito 2 >