< Lukha 19 >

1 U Yesu aingile akhagenda pagati pa Yeriko.
Yesu analowa mu Yeriko napitirira.
2 Napo pale nu munu yumo alikhulambuliwa Sakhaye. Ale mbaha va vasongasogo khageale momafu.
Kunali munthu kumeneko dzina lake Zakeyu; iye anali mkulu wa wolandira msonkho ndipo anali wolemera.
3 Anokhwagwa ukhumbona U Yesu munu vandakhikhi, alemilwe ukhumbona ulwakhuva avanu vodegile, umwene ale isupi fincho.
Iye ankafuna kuona Yesu kuti ndani, koma pokhala wamfupi sanathe chifukwa cha gulu la anthu.
4 Pwu, akhalogola nambivi khuvanu, akhatoga mbinkhi ambone U Yesu ulwakhuva U Yesu agendile injila ila.
Choncho iye anathamangira patsogolo ndipo anakwera mu mtengo wamkuyu kuti amuone Iye, pakuti Yesu ankadutsa njira imeneyo.
5 U Yesu avileafikhe pala akhalola khukhiya akhambula, sakhayo ikha nambivi, ulwakhuva ilelo nilenda munyumba yako.'
Yesu atafika pa malopo, anayangʼana mmwamba ndipo anati kwa iye, “Zakeyu, tsika msangamsanga. Ine ndiyenera kukhala mʼnyumba mwako lero.”
6 Akha gakha nambivi, akhikha akhamwambelila khuluhekhelo.
Ndipo nthawi yomweyo anatsika ndipo anamulandira mosangalala.
7 Avanu voni vavilevalole incho, vakhakhuta, vakhata, 'Alutile khukhugendela umunu utulanogwa.'
Anthu onse ataona zimenezi anayamba kungʼungʼudza, nati, “Iye akupita kuti akakhale mlendo wa wochimwa.”
8 U sakhai akhima akhanchova Ntwa, Lola Ntwa nusu ya khyuma kyango nikhuvapo avalemilwe, yegave nepokhile khumunu ikhinu, nikhumbunchekhencha mara khane. '
Koma Zakeyu anayimirira ndipo anati kwa Ambuye, “Taonani Ambuye! Theka la chuma changa ndipereka kwa osauka ndipo ngati ndinamubera wina aliyense pa chilichonse, ndidzamubwezera mochulukitsa kanayi.”
9 U Yesu akhambula, elelo uvupokhi vufikhe mnyumba eye, ulwakhuva mwape mwana va Abrahamu.
Yesu anati kwa iye, “Lero chipulumutso chafika mʼnyumba ino, chifukwa munthu uyu nayenso ndi mwana wa Abrahamu.
10 Ulwakhuva umwana va munu inchile khulonda nu khuvapo kha avanu avayagile. '
Pajatu Mwana wa Munthu anabwera kudzafunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.”
11 Vavile vapulikhe ewo, akhedelela ukhunchova akhakhumya ikhihwani, ulwakhuva alepipi ne Yerusalemu, avene vakhata uludeva lwa Nguluve lukhegelile lulepakhuvonekha nambivi.
Pamene iwo ankamvera izi, Iye anapitiriza kuwawuza fanizo, chifukwa Iye anali kufupi ndi Yerusalemu ndipo anthu ankaganiza kuti ufumu wa Mulungu ukanaoneka nthawi yomweyo.
12 Pwu akhavavula, “Ukhalani yumo alutile khukhilunga ikhyakuvutali akhambilile uludeva nu khukhilivukha.
Iye anati, “Munthu wa banja laufumu anapita ku dziko lakutali kukadzozedwa ufumu ndipo kenaka abwerenso kwawo.
13 Akhavilanga avavombi vamwene khinchigo, akhavapa ifineigo kumi, akhavavula, 'Mvombage iligunchi mpakha nelavanikhi ilivukha.'
Tsono iye anayitana antchito ake khumi ndi kuwapatsa ndalama khumi. Iye anati, ‘Gwiritsani ntchito ndalama izi mpaka nditabwerera.’
14 Pwu avanuva mwene vakhambi pela vakhasuha avakhape tamu valute vakhoge nukhuta, satwinogwa umunu uyo atulogonchage.'
“Koma anthu ake anamuda ndipo anatuma nthumwi pambuyo pake kukanena kuti, ‘Sitikufuna munthuyu kuti akhale mfumu yathu.’
15 Pwu avileakhiliwikhe khukhaya wuvapile uvutwa, akhavavula avavombi uwuavalekhile indalama velagiwe khumwene, alumaye utengo ugwavapatile khumbo iyuvakhavokhavombelega.
“Iye analandira ufumuwo ngakhale zinali zotero, ndipo anabwerera kwawo. Kenaka iye anatumiza uthenga kwa antchito ake amene anawapatsa ndalama aja, ndi cholinga chakuti adziwe chimene anapindula nazo.
16 Uvakwanda akhincha, akhanchova, 'Ntwa, ikhibina khyako kiholile amabina kumi khuvulogolo. '
“Woyamba anabwera ndipo anati, ‘Bwana ndalama zanu zapindula khumi zina.’
17 Pwu ukalani akhambula, lunonu, ulembombi inonu. Ulwa khuva ukhale mwidekhinchi khumbombo endebe, wiva mwemelenchi khu vunchege khinchigo. '
“Bwana wakeyo anayankha kuti, Wachita bwino wantchito wabwino. ‘Chifukwa wakhulupirika pa zinthu zazingʼono, lamulira mizinda khumi.’
18 Uvaveli akhincha, akhata, 'Ntwa, ikhibina khyakho kholile amabina gakhano.'
“Wachiwiri anabwera ndipo anati, ‘Bwana, ndalama zanu zapindula zisanu zina.’
19 Ukalani akhambula,'Tola uvuloleli khuvunchegi vukhano. '
“Bwana anayankha kuti, ‘Iwe lamulira mizinda isanu.’
20 Nu yuge akhincha, akhata, 'Ntwa ulupa ulutalama lwakho, Ngalubinile vunonu mumwenda,
“Kenaka wantchito wina anabwera ndipo anati, ‘Bwana, ndalama yanu nayi; ine ndinayibisa ndi kuyisunga mʼkansalu.
21 Ulwakhuva gadwadile uve ulemunu ikhali. Vutola khila ikhyuvekhile nukhubena ikhu suvyalile. '
Ine ndimakuopani, chifukwa ndinu munthu wowuma mtima. Inu mumatenga chimene simunachiyike ndi kukolola chimene simunadzale.’
22 Ukalani akhambula, 'Khumamenyu gakho nilhukhuhega, vivombi vembivi. Ukhalumayile ukhuta une numunu nkali, nitolaikhi sanivikhile nu khubena ikhisa nivyalile.
“Bwana wake anayankha kuti, ‘Ine ndikukuweruza iwe ndi mawu ako omwewo. Ndiwe wantchito woyipa. Kani umadziwa kuti ndine munthu wowuma mtima ndi wotenga chimene sindinasungitse, ndi kukolola chimene sindinadzale?
23 Khikhi, sukhavekhe ulutalama lwago khubengi, wunikhilivukha nitole paninie nulutitu?
Nanga nʼchifukwa chiyani sunasungitse ndalama yanga, kuti ine pobwera, ndidzayitenge ndi chiwongoladzanja?’
24 Ukalani akhavavula avanu avaemile pale, 'Pokhaga ubina mkhape ula unyamibina khinchigo.'
“Ndipo iye anawuza amene anayimirira pafupi kuti, ‘Tengani ndalama yake ndi kumupatsa amene ali ndi ndalama khumiyo!’”
25 Vakhambula, 'Ntwa, umwene alenemibina khinchigo. '
Iwo anati, “Bwana iyeyu ali nazo kale khumi!”
26 Nikhuvavula, khila avyalinafyo akhwogelenchiwa afinge, uvialivuvule, vitola nafilafila afialienafyo.
Iye anayankha kuti, “Ndikukuwuzani kuti, aliyense amene ali nazo, adzapatsidwa zambiri, koma amene alibe, adzalandidwa ngakhale chimene ali nacho.
27 Ulwakhuva avalugu vago, sawa khanogwa ukhata nive nkhu ludeva vavo, vag'eg'e apa mvabude khuvulogolo khulyune.”
Tsono adani anga aja amene sankafuna kuti ndikhale mfumu yawo, abweretseni pano ndi kuwapha ine ndikuona.”
28 Avile anchovile ewo, alikhulule kuvulogolo alikhutoga ukhuluta ku Yerusalemu.
Yesu atatha kunena izi, anayendabe kupita ku Yerusalemu.
29 Avile akhagelile khu Bethfage, na ku Bethania, pawipi nekhikyamba ikhya Mizeituni, akhava sukha avakuongi vavile,
Iye atayandikira ku Betifage ndi Betaniya pa phiri lotchedwa Olivi, Iye anatuma awiri a ophunzira nati kwa iwo,
30 Akhata: 'Mlutage mumbunchege uvulipipi. wumwingile, mkha londage ikhyana khya ligodowe ikyusakhitogiwe. Muhudulage, mukhag'eg'e khulyune.
“Pitani mʼmudzi uli patsogolo panu, mukakalowa mʼmudzimo, mukapeza mwana wabulu womangiriridwa amene wina aliyense sanakwerepo. Mukamumasule ndi kubwera naye kuno.
31 Umunu agavavunche, 'khikhi mukhwavula? 'Munchova, “Ntwa ikhuyelonda.”
Ngati wina aliyense akakufunsani kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani mukumumasula mwana buluyo?’ Mukamuwuze kuti, ‘Ambuye akumufuna.’”
32 Avasukhiwe vakhaluta vakhayivona inyana ya ligodowe nduwvu U Yesu avavulile.
Otumidwawo anapita nakamupeza mwana wabulu monga momwe Yesu anawawuzira.
33 Vavilevikhwavula inyana ya ligodowe, avanyaligodowe vakhavavula, 'Khikhi mukhwavula inyana ya ligodowe ile?'
Pamene ankamasula mwana wabuluyo, eni ake anawafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani mukumasula mwana wabuluyo?”
34 Vakhanchova, 'U Ntwa ikhuyelonda. '
Iwo anayankha kuti, “Ambuye akumufuna.”
35 Pwu vakhahelekha kwa Yesu, vakhatandikha imienda giavo pakyanya panyana ya ligodowe vakhantoncha U Yesu pakhinya.
Iwo anabweretsa buluyo kwa Yesu, naponya zovala zawo pa bulupo ndi kumukwezapo Yesu.
36 Avileiluta avanuvalikhutandancha imienda ngivo musevo.
Pamene ankapita, anthu anayala zovala zawo mu msewu.
37 Avileikhwi mkhiyamba ikhiya Mizeituni, ikhipuga khoni ikhiya vakongi valikhululitela na khuginya U Nguluve khumamenyu amavakha, khumbombo imbakha inchovanchiwene,
Iye atafika pafupi ndi pamene msewu umatsikira ku phiri la Olivi, gulu lonse la ophunzira linayamba kuyamika Mulungu mwachimwemwe ndi mawu ofuwula chifukwa cha zodabwitsa zonse anaziona.
38 Valikhula, 'Uyu usayiwa ukurudeva uviikuwineha khulitawa lya Ntwa! Ulukhugu khukyanya, nulunonehekhencho khukyanya!'
“Yodala mfumu imene ikubwera mʼdzina la Ambuye!” “Mtendere kumwamba ndi ulemerero mmwambamwamba!”
39 Avafarisai palulundamano vakhambula, Ndemi, vanunanche avakhongi vakho. '
Ena mwa Afarisi mʼgulumo anati kwa Yesu, “Aphunzitsi, adzudzuleni ophunzira anu!”
40 U Yesu akhanda, akhata, 'Nivavule, vagave ava vinunula amaganga giywegapa fincho. '
Iye anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani kuti, ngati atakhala chete, miyala idzafuwula.”
41 U Yesu avileakhegelile mumbo nchege akhalila,
Iye atayandikira ku Yerusalemu ndi kuona mzindawo, anawulirira
42 Akhanchova mwalemulumaye nayumwe ikhigono ikhyilelo imbombo inchikhugegela uluhungu! Lino nchifikha mikhe pamikho gakho.
nati, “Iwe ukanadziwa lero lino zinthu zokubweretsera mtendere, koma tsopano zabisikira maso ako.
43 Ulwakhuva ifigono fikhwincha udugu vakho alanchenga uvunehege panie nuve, nukhukhu naugula nukhukhudidelencha ukhuma khwoni.
Pakuti masiku adzabwera pamene adani ako adzamanga mitumbira yankhondo nakuzungulira, nadzakutsekereza mbali zonse.
44 Vikhukhugwisya pasi uve na vana vakho. Savakhakhulekhele iliwe limo pakhya panige, ulwakha sawalumaye usikhikhi U Nguruve apwavakhanogwagwa ukhukhupokha.'
Iwo adzakugwetsera pansi, iwe, ana ako onse a mʼkati mwako. Iwo sadzasiya mwa iwe mwala wina pa unzake, chifukwa sunazindikire nthawi ya kubwera kwa Mulungu.”
45 U Yesu akhigila Mtempeli, akhategula ukhuvamanyisya avagunchaga,
Kenaka Iye analowa mʼdera la Nyumba ya Mulungu ndi kuyamba kutulutsa kunja amene amachita malonda.
46 Akhavavula, “Yesimbiwe, “Inyumba yago yiva nyumba ya khuvisayila, 'Umwe mvekhile ukhuva lipagala lya vakhenchi.”
Iye anawawuza kuti, “Zinalembedwa kuti Nyumba yanga idzakhala nyumba ya mapemphero, koma inu mwayisadutsa phanga la achifwamba.”
47 U Yesu alikhumanyisya khila khigono Mtempeli. Avantwa na vamayisi va ndagilo na valogonchi va vanu vakhanogwa ukhumbuda,
Tsiku lililonse amaphunzitsa mʼNyumba ya Mulungu. Koma akulu a ansembe, aphunzitsi amalamulo ndi atsogoleri pakati pa anthu amayesetsa kuti amuphe.
48 Pwu vakhahemwa injila iya khugakha fwo, ulwakhuva avanu voni valikhupulikhencha nulukhala.
Komabe iwo sanathe kupeza njira ina iliyonse kuti achite izi, chifukwa anthu onse anakhulupirira mawu ake.

< Lukha 19 >