< 1 Chronicles 1 >

1 Adam, Seth, Enos,
Adamu, Seti, Enosi
2 Cainan, Mahalalel, Jared,
Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
3 Enoch, Methuselah, Lamech,
Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
4 Noah, Shem, Ham, and Japheth.
Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
5 The sons of Japheth: Gomer, and Magog, and Madai, and Javan, Tubal, Meshech, Tiras.
Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
6 And the sons of Gomer: Ashkenaz, and Riphath, and Togarmah.
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
7 And the sons of Javan: Elishah and Tarshish, Kittim and Rodanim.
Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
8 The sons of Ham: Cush, and Mizraim, and Put, and Canaan.
Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
9 And the sons of Cush: Seba, and Havilah, Sabtah, and Raamah, and Sabteca. And the sons of Raamah: Sheba and Dadan.
Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
10 Then Cush conceived Nimrod, and he began to be powerful upon the earth.
Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
11 Truly, Mizraim conceived Ludim, and Anamim, and Lehabim, and Naphtuhim,
Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
12 as well as Pathrusim and Casluhim: from these the Philistines and the Caphtorim went forth.
Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
13 Truly, Canaan conceived Sidon, his firstborn, as well as the Hittite,
Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
14 and the Jebusite, and the Amorite, and the Girgashite,
Ayebusi, Aamori, Agirigasi
15 and the Hivite, and the Arkite, and the Sinite,
Ahivi, Aariki, Asini
16 and also the Arvadian, and the Samarite, and the Hamathite.
Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
17 The sons of Shem: Elam, and Asshur, and Arphaxad, and Lud, and Aram, and Uz, and Hul, and Gether, and Meshech.
Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
18 Then Arphaxad conceived Shelah, who also himself conceived Eber.
Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
19 And to Eber were born two sons. The name of one was Peleg, because in his days the earth was divided. And the name of his brother was Joktan.
Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
20 Then Joktan conceived Almodad, and Sheleph, and Hazarmaveth, and Jerah,
Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
21 as well as Hadoram, and Uzal, and Diklah,
Hadoramu, Uzali, Dikila
22 and then Obal, and Abimael, and Sheba, indeed
Obali, Abimaeli, Seba,
23 also Ophir, and Havilah, and Jobab. All these are the sons of Joktan.
Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
24 Shem, Arphaxad, Shelah,
Semu, Aripakisadi, Sela
25 Eber, Peleg, Reu,
Eberi, Pelegi, Reu
26 Serug, Nahor, Terah,
Serugi, Nahori, Tera
27 Abram, the same is Abraham.
ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
28 And the sons of Abraham: Isaac and Ishmael.
Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
29 And these are their generations: the firstborn of Ishmael, Nebaioth, and then Kedar, and Adbeel, and Mibsam,
Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
30 and Mishma, and Dumah, Massa, Hadad, and Tema,
Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
31 Jetur, Naphish, Kedemah. These are the sons of Ishmael.
Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
32 And the sons of Keturah, the concubine of Abraham, whom she conceived: Zimran, Jokshan, Medan, Midian, Ishbak, and Shuah. And the sons of Jokshan: Sheba and Dedan. And the sons of Dedan: Asshurim, and Letushim, and Leummim.
Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
33 And the sons of Midian: Ephah, and Epher, and Hanoch, and Abida, and Eldaah. All these are the sons of Keturah.
Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
34 Now Abraham conceived Isaac, whose sons were Esau and Israel.
Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
35 The sons of Esau: Eliphaz, Reuel, Jeush, Jalam, and Korah.
Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
36 The sons of Eliphaz: Teman, Omar, Zepho, Gatam, Kenez, and by Timna, Amalek.
Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
37 The sons of Reuel: Nahath, Zerah, Shammah, Mizzah.
Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
38 The sons of Seir: Lotan, Shobal, Zibeon, Anah, Dishon, Ezer, Dishan.
Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
39 The sons of Lotan: Hori, Heman. Now the sister of Lotan was Timna.
Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
40 The sons of Shobal: Alian, and Manahath, and Ebal, Shephi, and Onam. The sons of Zibeon: Aiah and Anah. The sons of Anah: Dishon.
Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
41 The sons of Dishon: Hamran, and Esheban, and Ithran, and Cheran.
Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
42 The sons of Ezer: Bilhan, and Zaavan, and Akan. The sons of Dishan: Uz and Aran.
Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
43 Now these are the kings who reigned in the land of Edom, before there was a king over the sons of Israel: Bela, the son of Beor; and the name of his city was Dinhabah.
Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
44 Then Bela died, and Jobab, the son of Zerah, from Bozrah, reigned in his place.
Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
45 And when Jobab also had died, Husham, from the land of the Temanites, reigned in his place.
Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
46 Then Husham also passed away, and Hadad, the son of Bedad, reigned in his place. And he struck the Midianites in the land of Moab. The name of his city was Avith.
Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
47 And when Hadad also had died, Samlah from Masrekah reigned in his place.
Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
48 Then Samlah also died, and Shaul from Rehoboth, which is situated beside a river, reigned in his place.
Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
49 Shaul also having died, Baal-hanan, the son of Achbor, reigned in his place.
Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
50 Then he too died, and Hadar reigned in his place. And the name of his city was Pau. And his wife was called Mehetabel, the daughter of Matred, the daughter of Mezahab.
Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
51 And Hadar having died, there began to be commanders in Edom in place of kings: commander Thamna, commander Alvah, commander Jetheth,
Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
52 commander Oholibamah, commander Elah, commander Pinon,
Oholibama, Ela, Pinoni,
53 commander Kanez, commander Teman, commander Mibzar,
Kenazi, Temani, Mibezari,
54 commander Magdiel, commander Iram. These are the commanders of Edom.
Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

< 1 Chronicles 1 >