< Zekariya 12 >

1 Uthenga wa Yehova kwa Israeli. Yehova, amene amayala mlengalenga, amene amayika maziko a dziko lapansi, ndiponso amene amalenga mzimu wokhala mwa munthu, akunena kuti,
The birthun of the word of the Lord on Israel. And the Lord seide, stretchynge forth heuene, and founding erthe, and makynge the spirit of a man in hym, Lo!
2 “Taonani, ndidzasandutsa Yerusalemu kukhala chakumwa choledzeretsa chimene chidzasokoneza mitundu yonse ya anthu yomuzungulira. Yuda adzazingidwa pamodzinso ndi Yerusalemu.
Y schal putte Jerusalem a lyntel of glotonye to alle puplis in cumpas, but and Juda schal be in `a segyng ayens Jerusalem.
3 Pa tsiku limenelo, pamene mitundu yonse ya anthu a dziko lapansi idzasonkhana kulimbana naye, ndidzasandutsa Yerusalemu thanthwe losatheka kusunthidwa ndi mitundu yonse ya anthu. Onse oyesa kumusuntha adzadzipweteka.
And it schal be, in that dai Y schal putte Jerusalem a stoon of birthun to alle puplis; alle that schulen lifte it, schulen be to-drawun with kittyng doun, and alle rewmes of erthe schulen be gaderid ayens it.
4 Pa tsiku limenelo kavalo aliyense ndidzamuchititsa mantha kuti asokonezeke, ndipo wokwerapo wake ndidzamuchititsa misala,” akutero Yehova. “Ndidzayangʼanira nyumba ya Yuda koma ndidzachititsa khungu akavalo onse a anthu a mitundu ina.
In that dai, seith the Lord, Y schal smyte ech hors in drede, `ether leesynge of mynde, and the stiere `of hym in woodnesse; and on the hous of Juda Y schal opene myn iyen, and schal smyte with blyndnesse ech hors of puplis.
5 Pamenepo atsogoleri a Yuda adzayankhula mʼmitima mwawo kuti, ‘Anthu a ku Yerusalemu ndi amphamvu, chifukwa Yehova Wamphamvuzonse ndiye Mulungu wawo.’
And duikis of Juda schulen seie in her hertis, Be the dwellers of Jerusalem coumfortid to me in the Lord of oostis, the God of hem.
6 “Pa tsiku limenelo ndidzasandutsa atsogoleri a Yuda kukhala ngati mbawula yotentha pakati pa nkhuni, ngati sakali yoyaka pa mitolo ya tirigu. Adzatentha mitundu yonse ya anthu yowazungulira, kumanja ndi kumanzere, koma Yerusalemu sadzasuntha pa malo ake.
In that dai Y schal putte the duykis of Juda as a chymnei of fier in trees, and as a broond of fier in hei; and thei schulen deuoure at the `riythalf and lefthalf alle puplis in cumpas. And Jerusalem schal be enhabitid eftsoone in his place, `in Jerusalem.
7 “Yehova adzapulumutsa malo okhala Yuda poyamba, kuti ulemu wa nyumba ya Davide ndi wa anthu okhala mu Yerusalemu usapambane ulemu wa Yuda.
And the Lord schal saue the tabernaclis of Juda, as in bigynnyng, that the hous of Dauid `glorie not greetli, and the glorie of men dwellynge in Jerusalem be not ayens Juda.
8 Pa tsiku limenelo Yehova adzatchinjiriza onse okhala mu Yerusalemu, kotero kuti anthu ofowoka kwambiri pakati pawo adzakhala ngati Davide, ndipo nyumba ya Davide idzakhala ngati Mulungu, ngati mngelo wa Yehova wowatsogolera.
In that dai the Lord schal defende the dwelleris of Jerusalem; and he that schal offende of hem, schal be in that dai as Dauid, and the hous of Dauid schal be as of God, as the aungel of the Lord in the siyt of hym.
9 Pa tsiku limenelo ndidzawononga mitundu yonse yofuna kuthira nkhondo Yerusalemu.
And it schal be, in that dai Y schal seke for to al to-breke alle folkis that comen ayens Jerusalem.
10 “Ndipo pa nyumba ya Davide ndi pa anthu okhala mu Yerusalemu ndidzakhuthulirapo mzimu wachisomo ndi wopemphera. Iwo adzandiyangʼana Ine, amene anamubaya, ndipo adzamulirira kwambiri monga momwe munthu amalirira mwana wake mmodzi yekhayo, ndiponso adzamva chisoni kwambiri monga momwe amachitira ndi mwana woyamba kubadwa.
And Y schal helde out on the hous of Dauid, and on dwelleris of Jerusalem, the spirit of grace, and of preieris; and thei schulen biholde to me, whom thei `fitchiden togidere. And thei schulen biweile hym with weilyng, as on `the oon bigetun; and thei schulen sorewe on hym, as it is wont `for to be sorewid in the deth of the firste bigetun.
11 Pa tsiku limenelo mudzakhala kulira kwakukulu mu Yerusalemu, monga kulira kwa ku Hadadi-Rimoni ku chigwa cha Megido.
In that dai greet weilyng schal be in Jerusalem, as the weilyng of Adremon in the feeld of Magedon.
12 Dziko lidzalira kwambiri, fuko lililonse pa lokha, akazi awo pa okhanso: fuko la Davide pamodzi ndi akazi awo, fuko la Natani pamodzi ndi akazi awo,
And erthe schal weile; meynees and meynees bi hem silf; the meynees of the hous of Dauid bi hem silf, and the wymmen of hem bi hem silf;
13 nyumba ya Levi pamodzi ndi akazi awo, fuko la Simei pamodzi ndi akazi awo,
meynees of the hous of Nathan bi hem silf, and the wymmen of hem bi hem silf; meynees of the hous of Leuy bi hem silf, and the wymmen of hem bi hem silf; meynees of Semei bi hem silf, and the wymmen of hem bi hem silf.
14 ndiponso mafuko onse pamodzi ndi akazi awo.
All othere meynees, meynees and meynees bi hem silf, and the wymmen of hem bi hem silf.

< Zekariya 12 >