< Masalimo 90 >

1 Pemphero la Mose munthu wa Mulungu. Ambuye, mwakhala muli malo athu okhalamo pa mibado yonse.
Gospode! ti si nam utoèište od koljena do koljena.
2 Mapiri asanabadwe, musanalenge nʼkomwe dziko lapansi ndi dziko lonse, kuyambira muyaya mpaka muyaya Inu ndinu Mulungu.
Prije nego se gore rodiše i sazda se zemlja i vasiljena, i od vijeka i do vijeka ti si Bog.
3 Inu mumabwezera anthu ku fumbi, mumati, “Bwerera ku fumbi iwe mwana wa munthu.”
Ti povraæaš èovjeka u truhlež, i govoriš: vratite se sinovi ljudski!
4 Pakuti zaka 1,000 pamaso panu zili ngati tsiku limene lapita kapena ngati kamphindi ka usiku.
Jer je tisuæa godina pred oèima tvojima kao dan juèerašnji, kad mine, i kao straža noæna.
5 Inu mumasesa anthu mʼtulo ta imfa, iwo ali ngati udzu watsopano wa mmawa,
Ti ih kao povodnjem odnosiš; oni su kao san, kao trava, koja rano vene,
6 ngakhale kuti mmawa umaphuka watsopano, pofika madzulo wauma ndi kufota.
Ujutru cvjeta i uvene, uveèe se pokosi i sasuši.
7 Ife tathedwa ndi mkwiyo wanu; ndipo taopsezedwa ndi kuyipidwa kwanu.
Jer nas nestaje od gnjeva tvojega, i od jarosti tvoje u smetnji smo.
8 Mwayika mphulupulu zathu pamaso panu, machimo athu obisika poonekera pamaso panu.
Stavio si bezakonja naša preda se, i tajne naše na svjetlost lica svojega.
9 Masiku athu onse amatha ali pansi pa ukali wanu; timatsiriza zaka zathu ndi kubuwula.
Svi se dani naši prekraæuju od srdnje tvoje, godine naše prolaze kao glas.
10 Kuchuluka kwa masiku athu ndi 70, kapena 80 ngati tili ndi mphamvu; komabe zaka zonsezi ndi za mavuto ndi nkhawa, zimatha mofulumira ndipo ife timawulukira kutali.
Dana godina naših svega ima do sedamdeset godina, a u jaèega do osamdeset godina: i sam je cvijet njihov muka i nevolja; jer teku brzo, i mi odlijeæemo.
11 Kodi ndani amadziwa mphamvu ya mkwiyo wanu? Pakuti ukali wanu ndi waukulu ngati ulemu umene uyenera Inu.
Ko zna silu gnjeva tvojega i tvoju jarost, da bi te se kao što treba bojao?
12 Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola, kuti tikhale ndi mtima wanzeru.
Nauèi nas tako brojiti dane naše, da bismo stekli srce mudro.
13 Lezani mtima Inu Yehova! Kodi mudzatikwiyira mpaka liti? Achitireni chifundo atumiki anu.
Povrati se, Gospode! Dokle æeš? Smiluj se na sluge svoje.
14 Mutikhutitse mmawa ndi chikondi chanu chosatha, kuti tiyimbe ndi chimwemwe ndi kukhala okondwa masiku athu onse.
Ujutru nas nasiti dobrote svoje, i radovaæemo se i veseliti u sve dane svoje.
15 Tisangalatseni masiku ambiri monga masiku amene mwatisautsa, kwa zaka zambiri monga momwe tinaonera mavuto.
Obraduj nas prema danima, u koje si nas muèio, i prema godinama, u koje smo gledali nevolju.
16 Ntchito zanu zionetsedwe kwa atumiki anu, kukongola kwanu kwa ana awo.
Neka se pokaže na slugama tvojim djelo tvoje, i slava tvoja na sinovima njihovijem.
17 Kukoma mtima kwa Ambuye Mulungu wathu kukhale pa ife; tikhazikitsireni ntchito ya manja athu; inde, khazikitsani ntchito ya manja athu.
Neka bude dobra volja Gospoda Boga našega s nama, i djelo ruku naših dovrši nam, i djelo ruku naših dovrši.

< Masalimo 90 >