< Masalimo 54 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.” Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu; onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.
Bože! imenom svojim pomozi mi, i krjepošæu svojom odbrani me na sudu.
2 Imvani pemphero langa, Inu Mulungu mvetserani mawu a pakamwa panga.
Bože! usliši molitvu moju, èuj rijeèi usta mojih.
3 Alendo akundithira nkhondo; anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga, anthu amene salabadira za Mulungu.
Jer tuðini ustaše na me, i silni traže dušu moju; nemaju Boga pred sobom.
4 Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa; Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.
Gle, Bog je pomoænik moj, Gospod daje snagu duši mojoj.
5 Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe; mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.
Obratiæe zlo na neprijatelje moje, istinom svojom istrijebiæe ih.
6 Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu; ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova, pakuti ndi labwino.
Rado æu prinijeti žrtvu, proslaviæu ime tvoje, Gospode, jer je dobro.
7 Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse, ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.
Jer me izbavljaš od svake nevolje, i na neprijatelje moje bez straha gleda oko moje.

< Masalimo 54 >