< Masalimo 29 >

1 Salimo la Davide. Perekani kwa Yehova, inu anthu amphamvu, perekani kwa Yehova ulemerero ndi mphamvu.
Dajte Gospodu, sinovi Božiji, dajte Gospodu slavu i èast.
2 Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake, pembedzani Yehova mwa kukongola kwa chiyero chake.
Dajte Gospodu slavu imena njegova. Poklonite se Gospodu u svetoj krasoti.
3 Liwu la Yehova lili pamwamba pa madzi; Mulungu waulemerero abangula, Yehova abangula pamwamba pa madzi amphamvu.
Glas je Gospodnji nad vodom, Bog slave grmi, Gospod je nad vodom velikom.
4 Liwu la Yehova ndi lamphamvu; liwu la Yehova ndi laulemerero.
Glas je Gospodnji silan, glas je Gospodnji slavan.
5 Liwu la Yehova limathyola mikungudza; Yehova amathyolathyola mikungudza ya ku Lebanoni.
Glas Gospodnji lomi kedre, Gospod lomi kedre Livanske.
6 Iye amachititsa Lebanoni kulumphalumpha ngati mwana wangʼombe, Siriyoni ngati mwana wa njati:
Kao tele skaèu od njega; Livan i Sirion kao mlad bivo.
7 Liwu la Yehova limakantha ngati kungʼanima kwa mphenzi.
Glas Gospodnji sipa plamen ognjeni.
8 Liwu la Yehova limagwedeza chipululu; Yehova amagwedeza chipululu cha Kadesi.
Glas Gospodnji potresa pustinju, potresa Gospod pustinju Kades.
9 Liwu la Yehova limapindapinda mibawa ndi kuyeretsa nkhalango. Ndipo mʼNyumba mwake onse amafuwula kuti, “Ulemerero!”
Glas Gospodnji oprašta košute bremena, i sa šuma skida odijelo; i u crkvi njegovoj sve govori o slavi njegovoj.
10 Yehova amakhala pamwamba pa madzi osefukira, Yehova ndiye mfumu kwamuyaya.
Gospod je sjedio nad potopom, i sjedjeæe Gospod kao car uvijek.
11 Yehova amapereka mphamvu kwa anthu ake; Yehova amadalitsa anthu ake ndi mtendere.
Gospod æe dati silu narodu svojemu, Gospod æe blagosloviti narod svoj mirom.

< Masalimo 29 >