< Masalimo 16 >

1 Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
Èuvaj me, Bože; jer se u te uzdam.
2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
Rekoh Gospodu: ti si Gospod moj, nemam dobra osim tebe.
3 Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
U svetima koji su na zemlji i u velikima sva je utjeha moja.
4 Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
Neka drugi umnožavaju idole svoje, neka trèe k tuðima; ja im neæu ljevati krvavih naljeva, niti æu metnuti imena njihovijeh u usta svoja.
5 Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
Gospod je moj dio našljedstva i èaše; ti podižeš dostojanje moje.
6 Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
Uže mi je zahvatilo prekrasna mjesta, i dio mi je moj mio.
7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
Blagosiljam Gospoda, koji me urazumljuje; tomu me i noæu uèi što je u meni.
8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
Svagda vidim pred sobom Gospoda: on mi je s desne strane da ne posrnem.
9 Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
Toga radi raduje se srce moje, i veseli se jezik moj, još æe se i tijelo moje smiriti u uzdanju;
10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
Jer neæeš ostaviti duše moje u paklu, niti æeš dati da svetac tvoj vidi truhlost. (Sheol h7585)
11 Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.
Pokazaæeš mi put životni: obilje je radosti pred licem tvojim, utjeha u desnici tvojoj dovijeka.

< Masalimo 16 >