< Masalimo 146 >

1 Tamandani Yehova. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.
Hvali, dušo moja, Gospoda.
2 Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse; ndidzayimba nyimbo zamatamando kwa Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.
Hvaliæu Gospoda za života svojega, pjevaæu Bogu svojemu dok me je god.
3 Musamadalire mafumu, anthu osakhalitsa, amene sangathe kupulumutsa.
Ne uzdajte se u knezove, u sina èovjeèijega, u kojega nema pomoæi.
4 Pamene mizimu yawo yachoka, iwo amabwerera ku dothi; zimene ankafuna kuchita zimatha tsiku lomwelo.
Iziðe iz njega duh, i vrati se u zemlju svoju: taj dan propadnu sve pomisli njegove.
5 Wodala ndi amene thandizo lake ndi Mulungu wa Yakobo.
Blago onome, kojemu je pomoænik Bog Jakovljev, kojemu je nadanje u Gospodu, Bogu njegovu,
6 Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo; Yehova, amene ndi wokhulupirika kwamuyaya.
Koji je stvorio nebo i zemlju, more i sve što je u njima; koji drži vjeru uvijek,
7 Iye amachitira chilungamo anthu oponderezedwa ndipo amapereka chakudya kwa anthu anjala. Yehova amamasula amʼndende,
Èini sud onima, kojima se èini krivo; daje hranu gladnima. Gospod driješi svezane,
8 Yehova amatsekula maso anthu osaona, Yehova amadzutsa onse amene awerama pansi, Yehova amakonda anthu olungama.
Gospod otvora oèi slijepcima, podiže oborene, Gospod ljubi pravednike.
9 Yehova amasamalira alendo ndipo amathandiza ana ndi akazi amasiye, koma amasokoneza njira za anthu oyipa.
Gospod èuva došljake, pomaže siroti i udovici; a put bezbožnièki prevraæa.
10 Yehova ndiye Mfumu mpaka muyaya, Mulungu wako iwe Ziyoni, pa mibado yonse. Tamandani Yehova.
Gospod je car dovijeka, Bog tvoj, Sione, od koljena do koljena. Aliluja.

< Masalimo 146 >