< Masalimo 122 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
Obradovah se kad mi rekoše: hajdemo u dom Gospodnji!
2 Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
Evo, stoje noge naše na vratima tvojim, Jerusalime!
3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
Jerusalim je izidan, kao grad sliven u jednu zgradu.
4 Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
Onamo idu plemena, plemena Gospodnja, po naredbi Izrailjevoj da slave ime Gospodnje.
5 Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
Ondje stoje prijestoli sudski, prijestoli doma Davidova.
6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
Ištite mira Jerusalimu; neka bude dobro onima koji ljube tebe!
7 Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
Neka bude mir oko zidova tvojih, i èestitost u dvorima tvojim!
8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
Radi braæe svoje, i prijatelja svojih govorim: mir ti!
9 Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.
Radi doma Gospoda Boga našega želim ti dobro.

< Masalimo 122 >