< Masalimo 120 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
Ka Gospodu zavikah u nevolji svojoj, i usliši me.
2 Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
Gospode! izbavi dušu moju od usta lažljivijeh i od jezika lukavoga.
3 Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
Šta æe ti dati i šta æe ti prinijeti jezik lukavi?
4 Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
On je kao oštre strijele u jakoga, kao ugljevlje smrekovo.
5 Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
Teško meni kad sam tuðin kod Meseha, živim kod šatora Kidarskih.
6 Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
Dugo je živjela duša moja s onima koji mrze na mir.
7 Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.
Ja sam miran; ali kad stanem govoriti, u njih je rat.

< Masalimo 120 >