< Luka 15 >

1 Tsopano amisonkho ndi “ochimwa” ankasonkhana kudzamvera mawu ake.
Pu avasonga songo voni na vange avatula nogwa valutile khwa Yisu nu khupulihincha.
2 Koma Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo amangʼungʼudza nati, “Munthu uyu amalandira ochimwa ndi kudya nawo.”
Pu Avikhwandikha vavipile nukhunchova, “Umunu uyu ikhuvahegelencha avanyasambi nu khulya paniniye na vene.”
3 Ndipo Yesu anawawuza fanizo ili:
Puu uYisu akhanchova ikhihwani khuvene akhanchova akhata
4 “Tiyerekeze kuti mmodzi mwa inu ali ndi nkhosa 100 ndipo imodzi yatayika, kodi iye sangasiye 99 zija kutchire ndi kupita kukafuna yotayikayo mpaka atayipeza?
“Veni khulyumwe uvi alining'osi “100” nchingayage yimo, pu sakhahege khulonda yila yimo iyiyagile sikhunchilekha “99” iluta khulonda yila yimo, iluta khulonda iyi yagile nu khuyivona?
5 Ndipo iye akayipeza, amayinyamula pa phewa lake mwachimwemwe
Nu mwene wayiwene pu ikhumibikha palivega nu khuhovokha.
6 ndi kupita kwawo. Kenaka amayitana anzake ndi anansi pamodzi, ndi kuti, ‘Kondwerani nane; ine ndayipeza nkhosa yanga yotayika ija.’
Nifikha khunjengo, ikhuvilanga avanine na avabadihine akhavavula akhata muhovokhage paniniye nune, ukhuva niyiwene ing'osi yango iyi khayagile.
7 Ine ndikukuwuzani kuti momwemonso kudzakhala chikondwerero chachikulu kumwamba chifukwa cha wochimwa mmodzi amene watembenuka mtima kusiyana ndi anthu olungama 99 amene ali otembenuka mtima kale.”
nikhuvavula vulevule ukhuta khulava nu khuhovokha umo unyasambi vuipela nu khukhuta, ukhulutilila avanyavulwel vala “99” avu vene vanchila khusita khupela
8 “Kapena tiyeni tifanizire mayi amene anali ndi ndalama zasiliva khumi ndipo imodzi nʼkutayika, kodi sayatsa nyale ndi kusesa mʼnyumba ndi kufuna mosamalitsa mpaka atayipeza?
Khwale veni udala uvi iyancha ihela “10” nu khuyancha ihela yimo sa khatole ikhisikhi nukhumwemwesya nukhuhuma ukhulonda na makha goni nukhupata ihela yimo?
9 Ndipo pamene wayipeza, amayitana anzake, ndi anansi pamodzi nati, ‘Kondwerani nane; ine ndayipeza ndalama yanga yotayika ija.’
Vu awene iyiwene ihela ya mwene ikhuvilonga avanine nu khuvilanga avanine nukhuvilanga avabadihine nukhuta muhovokhage panine nune ukhuva niyiwene ihela iyikhayagile.
10 Momwemonso, Ine ndikukuwuzani kuti angelo a Mulungu amakondwera kwambiri chifukwa cha wochimwa mmodzi amene watembenuka mtima.”
Pu nikhuvavula nita khukhule ukhuhovokha khuvulongolo khunsuhwa nu Nguluve ulwakhuva unyasambi yumo apelile.”
11 Yesu anapitiriza kunena kuti, “Panali munthu amene anali ndi ana aamuna awiri.
Nu Yisu akhanchova, “Umunu umo ale na vana vavili
12 Wamngʼonoyo anati kwa abambo ake, ‘Abambo, patseni gawo langa la chuma chanu.’ Ndipo iye anawagawira awiriwo chuma chawo.
umwana udebe akhambula udadaye, Dada ume iligavo ilya vuhele uwa kyuma iyinogilwe khulyione nu vuhale. Pu akhagava ikyuma mugati imbene.
13 “Pasanapite nthawi, wamngʼonoyo anasonkhanitsa chuma chake chonse, napita ku dziko lakutali ndipo kumeneko anayamba kumwaza chuma chake mʼnjira zachitayiko.
Pu isikhu nchi nyingi umwana udebe akhalundamana fyoni ifyalinafyo akhaluta khukhilunga ikya khuvutali nukhu, akha khinila ihela nchoni, nu khugula ifinu ifipelwapelwa, ifi vivi nu khutaganiya ikyuma nu khuhovokha ne khilunga.
14 Iye atawononga zonse, kunagwa njala yoopsa mʼdziko lonselo ndipo anayamba kusauka.
Umwene vualile ikyuma kyooni, inchala imbaha yikhingila ikhilunga khila pu akhava ne njela imbaha.
15 Iye anapita kwa nzika ina ya dzikolo nakakhala naye ndi kumagwira ntchito, amene anamutumiza ku munda kukadyetsa nkhumba.
Akhaluta khulonda imbombo khu munu uva khilunga khila, nu mwene akhang'ilikha khukyalo khya mwene ukhudima ingube.
16 Iye analakalaka atakhutitsa mimba yake ndi makoko amene nkhumbazo zinkadya, koma panalibe wina amene anamupatsa kanthu.
Pu alikhunogwa ukhulya nu khwiguta na makhandi aganchisinche ingube, ulwakhuva, asikhuli umunu uvi apile ikyakhulya.
17 “Maganizo ake atabweramo, iye anati, ‘Ndi antchito angati a abambo anga amene ali ndi chakudya chimene amadya nʼkutsalako ndipo ine ndili pano kufa ndi njala!
Pu umwana udebe akhasaga munumbula ya mwene, akhanchova va vombi, akhanchova vavombi valingi khwa dada vilya nu khunywa ifingi nune nifwa ne nchala!
18 Ine ndinyamuka ndi kubwerera kwa abambo anga ndipo ndikati kwa iwo: abambo, ine ndachimwira kumwamba ndi kwa inu.
Nune nihega nilutakhwa dada vango, nukhumbula, “Dada usyikhile khukyanya na pa khilunga na khumiho gakho.
19 Ndine wosayeneranso kutchedwa mwana wanu; munditenge ngati mmodzi wa antchito anu.’
Sanenogile ukhuta neve mwana vakho; umbikhe ndumbomba mbombo vakho.”
20 Ndipo iye ananyamuka ndi kupita kwa abambo ake. “Koma iye akanali patali, abambo ake anamuona ndipo anamvera chisoni; anathamangira mwanayo, namukumbatira ndi kupsompsona.
Pu akhahega akhaluta khwa dada va mwene. Vu anchige khuvutali udada va mwene akhambona nu khuvona ikhisa akhaluta na mbivoi nu khunyila nu khukhumbata nu khubusu.
21 “Mwanayo anati, ‘Abambo, ine ndachimwira kumwamba ndi inunso. Ine sindiyenera konse kutchedwa mwana wanu.’
Pu umwana ula akhambula akhata, 'dada nelimalunde gakho, usikhile khukyanya na pasi apa na khuvulongolo khumiho gakho savinogile ukhwilangiwa ukhuta neli mwana wako.'
22 “Koma abambowo anati kwa antchito ake, ‘Fulumirani! Bweretsani mkanjo wabwino kwambiri ndipo mumuveke. Muvekeni mphete ndi nsapato.
Pu udada akhavavula avavombi va mwene, mulote umwenda unonu mufwali nche, pete nu khufwa lincha ifilato mumalende.
23 Bweretsani mwana wangʼombe wonenepa ndipo iphani. Tiyeni tikhale ndi phwando ndi kukondwerera.
Pu mukhatole isenga iyi dutwive mubude tulye nu khuhekhela.
24 Pakuti mwana wangayu anali wakufa, ndipo ali ndi moyonso; iye anatayika ndipo wapezeka.’ Chomwecho anayamba kukondwerera.
Ulwakhuva umwana vango afyulelino mwuoni. Ayagile lino avonikhe pu vakhatengula ukhuhekhela.
25 “Nthawi imeneyi, mwana wake wamkulu uja anali ku munda. Iye atafika pafupi ndi nyumba, anamva anthu akuyimba ndi kuvina.
Pu lino umwanaumbaha ale khukyalo, vu ikhwincha nu khuhegelela khukyaya akhapulikha inyimbo nu khwovela nu khukhina.
26 Ndipo iye anayitana mmodzi wa antchito, namufunsa chimene chimachitika.
Akhilanga uveimbombo yumo akhambuncha, khulikhikhi khukhuta khikhi?
27 Iye anayankha kuti, ‘Mʼbale wako wabwera ndipo abambo ako apha mwana wangʼombe wonenepa chifukwa wabwera wamoyo ndipo ali bwino.’
Umbomba mbombo akhata uvuvavo iuchile nu dada vakho abudile isenga iyidutwive ulwakhuva avuyile vunonu.'
28 “Mwana wamkulu anakwiya ndipo anakana kulowa. Chomwecho abambo ake anatuluka ndi kumudandaulira.
Umwana umbaha avipile ukhulutilila, akhabela nu khwingila mnyumba gati nu dada akhabembelesya ingile.
29 Koma iye anayankha abambo ake kuti, ‘Taonani! Zaka zonsezi ndakhala ndikukutumikirani kugwira ntchito yowawa ndipo palibe pamene sindinamvere malamulo anu. Koma inu simunandipatse ngakhale mwana wambuzi kuti ine ndichite phwando ndi anzanga.
Pu akhambula udadaye, 'Lola une, nekhuvombili imiakha gimingi, nu khwibata indagilo nchoni sugele ukhuma mwenamene, ukhuta ne hekhele na vayango.
30 Koma pamene mwana wanu uyu amene wawononga chuma chanu ndi achiwerewere wabwera ku nyumba, inu mwamuphera mwana wangʼombe wonenepa.’”
Ulwakhuva, vuinchile umwana vakho uve avangile ikhyama kyakho kyoni nu khulya ne valiguubudile igwada iyedutwive.
31 Abambowo anati, “Mwana wanga, iwe umakhala ndi ine nthawi zonse ndipo zonse ndili nazo ndi zako.
Udada akhambula akhata, 'Mwana vango, uve ukhale nune isikhu nchoni, nune vyoni ifi nelinafyo vyakho.
32 Koma tinayenera kukondwera ndi kusangalala, chifukwa mʼbale wako uyu anali wakufa ndipo ali ndi moyonso; iye anali wotayika ndipo wapezeka.”
Pu yikhale lunonu khulyufwe ukhuhekhela nu khuhovokha, vu ulukhololwu avonikhe vu akhayagile, akhafyule lino alikhuwumi; na avonikhe.”

< Luka 15 >