< Aroma 11 >

1 Ine ndikufunsa kuti kodi Mulungu anakana anthu ake? Ayi. Ndi pangʼono pomwe! Inenso ndine Mwisraeli, mmodzi mwa zidzukulu za Abrahamu, ndiponso wa fuko la Benjamini.
Pu leino niita, pu, uNguluve avabeilile avanu vamwene? Ndeili na padebe. Ulwakhuva une nayune neili Mwisraeli, eikhivumbukhu khya Abrahamu, vakhikolo eikhya Benyamini.
2 Mulungu sanawakane anthu ake amene Iye anawadziwiratu. Kodi inu simukudziwa zimene Malemba akunena pa ndime imene Eliya akudandaula kwa Mulungu kuneneza Aisraeli? Iye anati,
UNguluve savabele avanu vamwene, uvuavamanyile ukhuhuma khuvulenguleilo. Pu samlumanyile uvuveige wiita khiikhi ukhukongana nu Eliya, umuasimeleihinche khwa uNguluve savuli ya Vaisraeli?
3 “Ambuye, anthuwa apha aneneri anu ndi kugwetsa maguwa anu ansembe. Ndatsala ine ndekha wamoyo ndipo akufuna kundipha?”
“Ntwa vavabudile avasuhwa vakho, navene vanchinanginie inekhelo nchakho, une nei mwene nene niesiigile, navene vilonda uwumi wango.”
4 Ndipo yankho la Mulungu linali lotani? “Ine ndadzisungira ndekha anthu 7,000 amene sanapembedzepo Baala.”
Pu uwamule wa Nguluve wiita khiikhi khyulyuve? “Neileiveikhile savuli yango avaalufu saba yango avusavikhufugameela amafugamilo uBaali.”
5 Chimodzimodzinso lero lino, alipo Aisraeli pangʼono osankhidwa mwachisomo.
Paninie neiyo, usiekhe ugu leino pu khuvaale uvuvasigile savu ya vuhale wa luhungu.
6 Ndipo ngati ndi mwachisomo, sikungakhalenso mwa ntchito. Ngati zikanatero, chisomo sichikanakhalanso chisomo ayi.
Pui leino yiengave savuli ya luhungu, pusayiva mumivombele. pu apo uluhungu pusalwiva luhungu.
7 Nʼchiyani tsopano? Chimene Aisraeli anachifuna ndi mtima wonse sanachipeze koma osankhidwawo anachipeza. Enawo anawumitsidwa mtima
Khyu khinu khikhi leino? eikhyu uIsrael alikhulonda, sakhivone, pu avahaliwa vakhiwene, na vaange vakhasya.
8 monga kwalembedwa kuti, “Mulungu anawapatsa mzimu wosatha kumvetsa zinthu, maso osatha kupenya; makutu osatha kumva mpaka lero lino.”
Nduvuyeisimbiwe: “Unguluve avapile einumbula eiyavubungefu, amiho ukhula valekhe ukhulola, ni mbulukhutu ukhuta valekhe ukhupuleikha, pupakha eilelo eiye.”
9 Ndipo Davide akuti, “Maphwando awo asanduke msampha ndi diwa lowakola ndi chopunthwitsa kuti alandire chilango.
Vape uDaudi iita, “Nchilekhe imesa nchavo nchive nyaafu, neimitego gwa khwipeinja, nukhwitavuleila khuvene.
10 Maso awo atsekedwe kuti asaone, ndi misana yawo ikhale yokhota nthawi zonse.”
Galekhe amiho gavo gave niehisi pu valekhe ukhulola. Ukhavinamye emisana gyavo khitaduga.”
11 Ine ndikufunsanso kuti, kodi iwo anapunthwa ndi kugwa kotheratu? Ayi. Ndi pangʼono pomwe! Koma chifukwa cha kulakwa kwawo, chipulumutso chinafika kwa a mitundu ina kuti Aisraeli achite nsanje.
Leino niita, “Puvei, kuvinche nu khugwa?” Yelekhe ukhuva ewo lusikhu. Puleino ukhulemwa khwa veene, uvupokhi vufikhe khuvapanji, ukhuta avene vavo vavone wifu.
12 Koma ngati kulakwa kwawo kwapindulitsa dziko lapansi ndi kulephera kwawo kwapindulitsa a mitundu ina, nanga kudzakhala kupindula kwakukulu chotani iwo akadzabwera chonse!
Leino einave ukhulemwa khwavo vukaviwa khilunga, nu puyiengave uvufuve waavo vukavi wavapanji, pukhigelelo khiekhi eikhilutelile puyeve khunkwila nila khwavo?
13 Ine ndikuyankhula kwa inu a mitundu ina monga ine ndili mtumwi wa kwa a mitundu ina ndipo ndimawunyadira utumiki wangawu.
Na leino leino ninchova numwe mwie vunu va panji, neivile isuhwa khuvanu avajilunga ifinge, nikhigineihincha eimbombo ya vutangeli wango.
14 Ine cholinga changa nʼchakuti ndichititse nsanje anthu a mtundu wanga kuti ena mwa iwo apulumutsidwe.
Pamo yanikhuvapela uwifu avaleimbeili gumo nune, pano ya tukhuvapokha vaninie.
15 Pakuti ngati kukanidwa kwawo kunayanjanitsa anthu a dziko lapansi ndi Mulungu, nanga kudzatani, Iye akadzawalandiranso? Kudzakhala monga ngati anthu akufa akuuka.
Pu eingave ukhubeliwa khwavo lweideha no lwa khilunga, ukhyupeileiliwa khwavo ya khwiva ndakhikhi pu uwumi uwakhuhuma khuvunchukha?
16 Ngati chigawo chimodzi cha buledi woperekedwa monga zipatso zoyamba ndi choyera, ndiye kuti zonsezo ndi zoyera. Ngati muzu ndi oyera, nʼchimodzimodzinso nthambi zake.
Einave isekhe itanchi khibana vuyileiwo khu nongeya vutine. Einave undela khibana pu amasasi nagope wuwuwa.
17 Ngati nthambi zina zinakhadzulidwa ndipo inu, inu ndiye nthambi za olivi wakuthengo, nʼkulumikizidwa pamalo pa nthambi zimenezo, ndipo tsopano mukulandira nawo zakudya zochokera ku mizu ya olivi,
Pu einave amasasi maninie gageidewe, uve, lisasi lya msitu lya Mzeituni, ugugwavyaliwe muvene nu pungave waleepyo paninie navene eimilela gya vukani wa Mizeituni.
18 musadzitame kunyoza nthambi zinazo. Ngati mutero, ganizirani ichi kuti Inu simugwiriziza mizu, koma muzu ukugwiriziza inu.
Ulekhe ukhwiginia mumasasi, pu unave vukhiginia saveve yuve vukhugitanga emilela, pu emilela gikhukhutanga uve.
19 Tsono mudzati, “Nthambizo zinakhadzulidwa kuti ine ndilumikizidwepo.”
Puleino ayawita, “Amaswato gagidiewe ukhuta neivuliwe mukhikolo.
20 Nʼzoona. Koma iwo anakhadzulidwa chifukwa chosakhulupirira ndipo inu mukuyima mwachikhulupiriro. Musadzitukumule, koma muchite mantha.
Eiyo lweli, savuli ya khusita ukhwideekha khwavo vagedeiwe, pu uve wa eimile ulukangafu savuli ya lweideikho lwakho. Ulekhe ukwisageila yuve pakyanya fincho pu dwaadage.
21 Pakuti ngati Mulungu sanalekerere nthambi zachibadwidwe, Iye sadzakulekererani inunso.
Pu ulwakhuva eingave uNguluve sagalekhe lenche amaswato amatengule, sakha khuhigile uve na yuve.
22 Nʼchifukwa chake ganizirani za kukoma mtima ndi za ukali wa Mulungu. Ukali uli kwa iwo amene anagwa koma kukoma mtima kwa inu, malinga ngati musamala kukoma mtima kwakeko kupanda kutero inunso mudzakhadzulidwanso.
Lola, leino, imbombo inonu nu vukali wa Nguluve. Khuluvafu lumo, uvukali wa inchile khuva yuta vala avagwile. Pu khuluvafu ulunge, uluhungu lwa Nguluve lukhwincha palyuve ungave yawinchiga muvunonu wa mwene. Einave ate uve nayuveayavubeiliwa.
23 Ngati iwo asiya kukhala osakhulupirira, adzalumikizidwanso pakuti Mulungu akhoza kuwalumikizanso.
Na eingave savakhendelelage mukhusitakhwideekha kwavo, yavi valiwa khange. Ulwa khuva uNguluve alei na makha agakhuvyaleila khange.
24 Pakuti ngati inu, mwa chilengedwe munali mtengo wa olivi wa kuthengo, Mulungu anakukhadzulani nakulumikizani ku mtengo wa olivi wodzalidwa, zomwe ndi zotsutsana ndi chilengedwe, kodi sikudzakhala kwapafupi kwa Iye kuwalumikizanso mu mtengo wawowawo wa olivi?
Pu ulwakhuva umwe mungave mwageidewe khunji khugugwa gwa mbutengulielo Mzeituni gwa msitu, puleino eikyavulenguleilo khileivunge Mzeituni unonu pu sayiva fiva ukhulutilila fincho ava yuta?
25 Abale, ine sindifuna kuti mukhale osadziwa za chinsinsi ichi, kuti mungadziyese nokha anzeru. Kuwuma mtima kumene Aisraeli akuchita ndi kwa kanthawi kufikira chiwerengero cha a mitundu chitalowa.
Ulwa khuva valokolo saninogwa msite ughulumanya ukhukongana ukhu kongana nei siri eiye, ukhuta mulekhe ukhuva nu luhala mumisagiele gyienyo yumwe. Ei siri eiye khukhuta uvukafu vuhumile mu Israeli, imakha ukhunchikwilanila khwa filunga yakhiva khwinchile.
26 Kotero tsono Aisraeli onse adzapulumuka, monga kwalembedwa kuti, “Mpulumutsi adzachokera ku Ziyoni; Iye adzachotsa zoyipa zonse za Yakobo.
Puleino ava Israeli vooni yavipokhiwa, ndu unyeisimbiwe: “Ukhuhuma khu Sayuni ikhwincha upokhi, pu ayihencha uvuvivi ukhuhuma khwa Yakobo.
27 Ndipo ili lidzakhala pangano langa ndi iwo pamene Ine ndidzachotsa machimo awo.”
Na eili puyaliva ndagano pu paninie na veene useikhi uguyakhiva nihencha imbivi nchaavo.”
28 Chifukwa cha Uthenga Wabwino, Aisraeli asanduka adani a Mulungu kuti inu mupindule. Koma kunena za kusankhidwa, iwo ndi okondedwa ndi Mulungu chifukwa cha makolo awo aja.
Khuluvafu lumo ukhu kongana neilivangeili, vivipeiliwa savuli yienyo. Khuluvafu ulunge ukhukonga na vuhale wa Nguluve, vavyaliwe savuli ya vankukhu yavo.
29 Pakuti Mulungu akayitana munthu ndi kumupatsa mphatso sangasinthenso.
Ulwa khuv uluhombo ni nyeilango yu Nguluve sayigevukha.
30 Monga mmene inu munalili, osamvera Mulungu pa nthawi ina, tsopano mwalandira chifundo chifukwa cha kusamvera kwawo.
Ulwakhuva pakhwanda umwe mwale vagolo va Nguluve, puleino mulyupeilile uluhungu lwa Nguluve savuli ya khugalukha kwavo.
31 Chonchonso iwo akhala osamvera tsopano kuti iwonso alandire chifundo chifukwa cha chifundo cha Mulungu kwa inu.
Khunjila yeiyeiyo, leino ava yuta ava vagalwikhe, pu eilyu leivonikhe khukhuta savuli ya khisa ikyu muhungukhiwe umwe mvahile ukhwambeilila uluhungu.
32 Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē g1653)
Ulwakhuva uNguluve avadeindile avanu vooni muvugalukhi, ukhuta pwava vonele eikhisa vooni. (eleēsē g1653)
33 Aa! Nzeru za Mulungu ndi chidziwitso chake ndi zozama kwambiri! Ndani angazindikire maweruzidwe ake, ndipo njira zake angazitulukire ndani?
Umunchi velile mbaha uvukavi nu luhungu nu vumanyi wa Nguluve! Savunchingakhimchi wa uvuheigi wa mwene, ni njeila ncha mwene sanchi manyikhikha!
34 “Kodi wadziwa ndani maganizo a Ambuye? Kapena ndani anakhalapo mlangizi wake?”
“Pu veini uvyakhavu manyile uvufumbwe wantwa? puveini va masago khumwene?
35 “Kodi ndani anapereka mphatso kwa Mulungu, kuti Mulunguyo amubwezere iye?”
Pu veini taasi agelieli ukhupa eikhinu uNguluve pu ahombiwe khange?”
36 Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
Ulwa khuva ukhuhuma khumwene, na khunjila ya mwene na khumwene, ifinu fyooni pufile, khumwene luve ludwando isikhu nchooni. Amina. (aiōn g165)

< Aroma 11 >