< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
A Vildad Sušanin odgovori i reèe:
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
Vlast je i strah u njega, èini mir na visinama svojim.
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
Vojskama njegovijem ima li broja? i koga ne obasjava vidjelo njegovo?
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
I kako æe èovjek biti pravedan pred Bogom? i kako æe èist biti roðeni od žene?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
Gle, ni mjesec ne bi sjao, ni zvijezde ne bi bile èiste pred njim,
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
Akamoli èovjek, crv, i sin èovjeèji, moljac.

< Yobu 25 >