< Yobu 26 >

1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,
A Jov odgovori i reèe:
2 “Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu! Walimbitsadi dzanja la munthu wofowoka!
Kako si pomogao slabome! kako si izbavio ruku nejaku!
3 Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru! Ndipotu waonetsadi nzeru zochuluka!
Kako si svjetovao onoga koji je bez mudrosti i pokazao razum izobila!
4 Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa? Ndipo ndi mzimu wa yani umene unayankhula pakamwa pako?
Kome si govorio te rijeèi? i èiji je duh izašao iz tebe?
5 “Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi, ndi zonse zokhala mʼmadzimo.
I mrtve stvari stvorene su pod vodama i stanovnici njihovi.
6 Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
Otkriven je pakao pred njim, niti ima pokrivaèa pogibli. (Sheol h7585)
7 Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho; Iye anakoloweka dziko lapansi mʼmalo mwake pamene panali popanda nʼkanthu komwe.
On je razastro sjever nad prazninom, i zemlju objesio ni na èem.
8 Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake, koma mitamboyo siphulika chifukwa cha kulemera kwa madziwo.
Zavezuje vode u oblacima svojim, i ne prodire se oblak pod njima.
9 Iye amaphimba mwezi wowala, amawuphimba ndi mitambo yake.
Drži prijesto svoj, razapinje oblak svoj nad njim.
10 Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta, kukhala malire pakati pa kuwunika ndi mdima.
Meðu je postavio oko vode dokle ne bude kraj svjetlosti i mraku.
11 Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera, ndi kudabwa pa kudzudzula kwake.
Stupovi nebeski tresu se i drkæu od prijetnje njegove.
12 Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja; ndi nzeru zake anakantha chirombo cha mʼmadzi chija chotchedwa Rahabe.
Silom je svojom pocijepao more i razumom svojim razbio bjesnilo njegovo.
13 Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga, dzanja lake linapha chinjoka chothawa chija.
Duhom je svojim ukrasio nebesa, i ruka je njegova stvorila prugu zmiju.
14 Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake; tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona! Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?”
Gle, to su dijelovi putova njegovijeh; ali kako je mali dio što èusmo o njemu? i ko æe razumjeti grom sile njegove?

< Yobu 26 >