< Yobu 11 >

1 Pamenepo Zofari wa ku Naama anayankha kuti,
A Sofar Namaæanin odgovori i reèe:
2 “Kodi mawu ambirimbiriwa nʼkukhala osayankhidwa? Kodi munthu woyankhulayankhulayu nʼkulungamitsidwa?
Zar na mnoge rijeèi nema odgovora? ili æe èovjek govorljiv ostati prav?
3 Kodi anthu nʼkukhala chete atamva kubwebweta kwakoku? Kodi palibe wina amene adzakudzudzule pamene ukuyankhula zonyoza?
Hoæe li tvoje laži umuèkati ljude? i kad se ti rugaš, zar te neæe niko posramiti?
4 Iwe ukunena kwa Mulungu kuti, ‘Zikhulupiriro zanga ndi zopanda zolakwika ndipo ndine wangwiro pamaso panu.’
Jer si rekao: èista je nauka moja, i èist sam pred oèima tvojim.
5 Aa, nʼkanakonda Mulungu akanayankhula kuti Iye atsekule pakamwa pake kutsutsana nawe
Ali kad bi Bog progovorio i usne svoje otvorio na te,
6 ndi kukuwululira chinsinsi cha nzeru yake, pakuti nzeru yeniyeni ili ndi mbali ziwiri. Dziwa izi: Mulungu wayiwala machimo ako ena.
I pokazao ti tajne mudrosti, jer ih je dvojinom više, poznao bi da te Bog kara manje nego što zaslužuje tvoje bezakonje.
7 “Kodi iwe ungathe kumvetsa zinsinsi za Mulungu? Kodi ungafufuze malire a nzeru za Wamphamvuzonse?
Možeš li ti tajne Božije dokuèiti, ili dokuèiti savršenstvo svemoguæega?
8 Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
To su visine nebeske, šta æeš uèiniti? dublje je od pakla, kako æeš poznati? (Sheol h7585)
9 Muyeso wa nzeru zake ndi wautali kupambana dziko lapansi ndipo ndi wopingasa kupambana nyanja.
Duže od zemlje, šire od mora.
10 “Ngati Iye atabwera ndi kukutsekera mʼndende nakutengera ku bwalo la milandu, ndani angathe kumuletsa?
Da prevrati, ili zatvori ili sabere, ko æe mu braniti?
11 Ndithudi, Mulungu amazindikira anthu achinyengo; akaona choyipa, kodi sachizindikira?
Jer zna ništavilo ljudsko, i videæi nevaljalstvo zar neæe paziti?
12 Munthu wopanda nzeru sizingatheke kukhala wanzeru monganso mwana wa bulu wakuthengo sangasanduke munthu.
Èovjek bezuman postaje razuman, premda se èovjek raða kao divlje magare.
13 “Koma ngati upereka mtima wako kwa Iye ndi kutambasulira manja ako kwa Iyeyo,
Da ti upraviš srce svoje i podigneš ruke svoje k njemu,
14 ngati utaya tchimo limene lili mʼdzanja lako ndi kusalola choyipa kuti chikhale mʼmoyo mwako,
Ako je bezakonje u ruci tvojoj, da ga ukloniš, i ne daš da nepravda bude u šatorima tvojim,
15 udzatukula mutu wako wosachita manyazi; udzayima chilili ndipo sudzachita mantha.
Tada æeš podignuti lice svoje bez mane i stajaæeš tvrdo i neæeš se bojati;
16 Udzayiwala ndithu zowawa zako, zidzakhala ngati madzi amene apita kale.
Zaboraviæeš muku, kao vode koja proteèe opominjaæeš je se;
17 Moyo wako udzawala kupambana usana, ndipo mdima udzakhala ngati mmawa.
Nastaæe ti vrijeme vedrije nego podne, sinuæeš, biæeš kao jutro;
18 Udzalimba mtima popeza pali chiyembekezo; ndipo udzayangʼana mbali zonse ndi kugona mosatekeseka.
Uzdaæeš se imajuæi nadanje, zakopaæeš se, i mirno æeš spavati.
19 Udzagona pansi, popanda wina wokuopseza ndipo ambiri adzakupempha kuti uwachitire chifundo.
Ležaæeš, i niko te neæe plašiti, i mnogi æe ti se moliti.
20 Koma anthu oyipa adzafuna thandizo osalipeza, ndipo adzasowa njira yothawirapo; chiyembekezo chawo chidzakhala imfa basi.”
Ali oèi æe bezbožnicima išèiljeti, i utoèišta im neæe biti, i nadanje æe im biti izdisanje.

< Yobu 11 >