< Yeremiya 43 >

1 Yeremiya atatsiriza kuwawuza anthuwo mawu onse a Yehova Mulungu wawo, amene Yehova anamutuma kuti akawawuze,
A kad izgovori Jeremija svemu narodu sve rijeèi Gospoda Boga njihova, koje mu Gospod Bog njihov zapovjedi za njih, sve te rijeèi,
2 Azariya mwana wa Hosayia ndi Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi anthu onse odzikuza anawuza Yeremiya kuti, “Ukunama iwe! Yehova Mulungu wathu sanakutume kuti unene kuti, ‘Musapite ku Igupto kukakhala kumeneko.’
Tada Azarija sin Osajin i Joanan sin Karijin i svi oni ljudi oholi rekoše Jeremiji govoreæi: nije istina što govoriš; nije te poslao Gospod Bog naš da nam kažeš: ne idite u Misir da se ondje stanite.
3 Koma ndi Baruki mwana wa Neriya amene akukulimbikitsa kuti utiletse zopita ku Igupto ndi kuti mʼmalo mwake tidzipereke mʼmanja mwa Ababuloni, kuti iwo atiphe kapena kutitenga ukapolo ku Babuloni.”
Nego Varuh sin Nirijin podgovara te na nas da nas preda u ruke Haldejcima da nas pogube ili da nas presele u Vavilon.
4 Motero Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo pamodzi ndi anthu onse sanamvere lamulo la Yehova loti akhale mʼdziko la Yuda.
I tako Joanan sin Karijin i sve vojvode i sav narod ne poslušaše glasa Gospodnjega da ostanu u zemlji Judinoj.
5 Mʼmalo mwake, Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo anatenga anthu onse otsala a ku Yuda amene anabwera kudzakhala mʼdziko la Yuda kuchokera ku mayiko onse kumene anabalakirako.
Nego Joanan sin Karijin i sve vojvode uzeše sav ostatak Judin koji se bijaše vratio da živi u zemlji Judinoj iz svijeh naroda u koje bijahu razagnani,
6 Mʼgulu la anthu otengedwalo munali amuna onse, akazi ndi ana, ana aakazi a mfumu, ndiponso anthu amene Nebuzaradani mtsogoleri wa asilikali olonda mfumu anawasiya kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu, mdzukulu wa Safani pamodzinso ndi mneneri Yeremiya ndi Baruki mwana wa Neriya.
Ljude i žene i djecu i kæeri careve, i sve duše što bijaše ostavio Nevuzardan zapovjednik stražarski s Godolijom sinom Ahikama sina Safanova, i Jeremiju proroka i Varuha sina Nirijina,
7 Kotero anthuwo analowa mʼdziko la Igupto chifukwa anakana kumvera Yehova, nakafika ku Tapanesi.
I otidoše u zemlju Misirsku, jer ne poslušaše glasa Gospodnjega; i doðoše do Tafnesa.
8 Ndipo Yehova anayankhula ndi Yeremiya ku Tapanesi kuti,
I doðe rijeè Gospodnja Jeremiji u Tafnesu govoreæi:
9 “Tenga miyala inayi yayikulu ndipo uyikwirire mʼdothi pa chiwundo cha polowera ku nyumba yaufumu ya Farao ku Tapanesi. Uchite zimenezi Ayuda onse akuona.
Uzmi u ruke velikoga kamenja, i pokrij ga kalom u peæi za opeke što je na vratima doma Faraonova u Tafnesu da vide Judejci;
10 Ndipo uwawuze kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti: Ndidzayitana mtumiki wanga Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni, ndipo adzakhazika mpando wake waufumu pa miyala imene ndayikwirira apayi. Iye adzafunyulula tenti yake yaufumu pa miyala imeneyi.
I reci im: ovako veli Gospod nad vojskama Bog Izrailjev: evo, ja æu poslati i dovesti Navuhodonosora cara Vavilonskoga slugu svojega, i metnuæu prijesto njegov na ovo kamenje koje sakrih, i razapeæe carski šator svoj na njemu.
11 Iye adzabwera kudzathira nkhondo Igupto. Iwo oyenera kufa ndi mliri adzafa ndi mliri, iwo oyenera kutengedwa ukapolo adzatengedwa ukapolo, ndipo iwo oyenera kufa ndi lupanga adzafa ndi lupanga.
Jer æe doæi i zatrti zemlju Misirsku; ko bude za smrt otiæi æe na smrt, ko za ropstvo, u ropstvo, ko za maè, pod maè.
12 Adzayatsa moto mʼnyumba zopembedzera milungu ya Igupto. Adzayeretsa dziko la Igupto monga momwe mʼbusa amayeretsera chovala chake pochotsamo nsabwe. Pambuyo pake adzachoka mʼdziko la Igupto mwa mtendere.
I raspaliæu oganj u kuæama bogova Misirskih; i popaliæe ih i odvešæe ih u ropstvo, i ogrnuæe se zemljom Misirskom kao što se pastir ogræe plaštem svojim, i otiæi æe odande s mirom.
13 Ku Iguptoko adzagwetsa zipilala zachipembedzo za ku nyumba yopembedzera mulungu wa dzuwa. Adzatentha ndi moto nyumba za milungu ya ku Igupto.’”
I izlomiæe stupove u domu sunèanom što je u zemlji Misirskoj, i kuæe bogova Misirskih popaliæe ognjem.

< Yeremiya 43 >