< Yesaya 56 >

1 Yehova akuti, “Chitani chilungamo ndi zinthu zabwino, chifukwa chipulumutso changa chili pafupi ndipo ndidzakuwombolani posachedwapa.
Ovako veli Gospod: pazite na sud, i tvorite pravdu, jer æe skoro doæi spasenje moje, i pravda æe se moja objaviti.
2 Ndi wodala munthu amene amachita zimenezi, munthu amene amalimbika kuzichita, amene amasunga Sabata osaliyipitsa, ndipo amadziletsa kuchita zoyipa.”
Blago èovjeku koji tako èini, i sinu èovjeèijemu koji se drži toga èuvajuæi subotu da je ne oskvrni, èuvajuæi ruku svoju da ne uèini zla.
3 Mlendo amene waphatikana ndi Yehova asanene kuti, “Ndithu Yehova wandichotsa pakati pa anthu ake.” Ndipo munthu wofulidwa asanene kuti, “Ine ndine mtengo wowuma basi.”
I neka ne govori tuðin koji pristane uz Gospoda: Gospod me je odluèio od svoga naroda; i neka ne govori uškopljenik: gle, ja sam suho drvo.
4 Popeza Yehova akuti, “Wofulidwa amene amasunga masabata anga, nachita zokomera Ine ndi kusunga pangano langa,
Jer ovako veli Gospod za uškopljenike: koji drže subote moje i izbiraju što je meni ugodno, i drže zavjet moj,
5 ndidzawapatsa dzina ndi mbiri yabwino mʼkati mwa Nyumba yanga ndi makoma ake, kuposa kukhala ndi ana aamuna ndi aakazi. Ndidzawapatsa dzina labwino, losatha ndi losayiwalika.”
Njima æu dati u domu svom i meðu zidovima svojim mjesto i ime bolje nego sinova i kæeri, ime vjeèno daæu svakome od njih, koje se neæe zatrti.
6 Yehova akuti, “Alendo amene amadziphatika kwa Yehova, motero kuti amamutumikira Iye, amakonda dzina la Yehova, amamugwirira ntchito, komanso kusunga Sabata osaliyipitsa ndi kusunga bwino pangano langa,
A tuðine koji pristanu uz Gospoda da mu služe i da ljube ime Gospodnje, da mu budu sluge, koji god drže subotu da je ne oskvrne i drže zavjet moj,
7 amenewa Ine ndidzawafikitsa ku phiri langa lopatulika, ndidzawapatsa chimwemwe mʼnyumba yanga ya mapemphero. Zopereka zawo zopsereza ndi nsembe zawo ndidzazilandira pa guwa langa la nsembe. Paja nyumba yanga idzatchedwa nyumba ya mapemphero ya anthu a mitundu yonse.”
Njih æu dovesti na svetu goru svoju i razveseliæu ih u domu svojem molitvenom; žrtve njihove paljenice i druge žrtve biæe ugodne na oltaru mom, jer æe se dom moj zvati dom molitve svijem narodima.
8 Ambuye Yehova, amene amasonkhanitsa Aisraeli onse ali ku ukapolo akunena kuti, “Ndidzasonkhanitsano anthu ena kuwonjezera amene anasonkhana kale.”
Gospod Gospod govori, koji sabira prognanike Izrailjeve: još æu mu sabrati osim onijeh koji su sabrani.
9 Bwerani, inu zirombo zonse zakuthengo, inu nonse zirombo zamʼnkhalango bwerani mudzadye!
Sve zvijeri poljske, hodite da jedete, sve zvijeri šumske.
10 Atsogoleri onse a Israeli ndi akhungu, onse ndi opanda nzeru; onse ndi agalu opanda mawu, samatha kuwuwa: amagona pansi nʼkumalota amakonda kugona tulo.
Svi su mu stražari slijepi, ništa ne znaju, svi su psi nijemi, ne mogu lajati, sanljivi su, leže, mio im je drijemež.
11 Ali ngati agalu amene ali ndi njala yayikulu; sakhuta konse. Abusa nawonso samvetsa zinthu; onse amachita monga akufunira, aliyense amafunafuna zomupindulitsa iye mwini.
I psi su proždrljivi, koji ne znaju za sitost; i pastiri su koji ne znaju za razum, svaki se okreæe svojim putem, svaki za svojom korišæu sa svoga kraja.
12 Aliyense amafuwulira mnzake kuti, “Bwera, tiye timwe vinyo! Tiyeni timwe mowa mpaka kukhuta! Mawa lidzakhala ngati leroli, kapena kuposa lero lino.”
Hodite, uzeæu vina i napiæemo se silovita piæa, i sjutra æe biti kao danas, i još mnogo više.

< Yesaya 56 >