< Genesis 22 >

1 Nthawi ina zitatha izi, Mulungu anamuyesa Abrahamu. Iye anati, “Abrahamu!” Ndipo iye anayankha kuti, “Ee Ambuye.”
Poslije toga šæaše Bog okušati Avrama, pa mu reèe: Avrame! A on odgovori: evo me.
2 Ndipo Mulungu anati, “Tenga Isake, mwana wako yekhayo amene umamukonda ndi kupita naye ku dziko la Moriya. Ukamupereke iye ngati nsembe yopsereza pa limodzi la mapiri a kumeneko limene ndidzakuwuza.”
I reèe mu Bog: uzmi sada sina svojega, jedinca svojega miloga, Isaka, pa idi u zemlju Moriju, i spali ga na žrtvu tamo na brdu gdje æu ti kazati.
3 Abrahamu anadzuka mmamawa wake namangirira chokhalira pa bulu. Atadula nkhuni zokwanira zowotchera nsembe yopsereza, Abrahamu, antchito ake awiri pamodzi ndi Isake ananyamuka kupita kumalo kumene Mulungu anamuwuza Abrahamu.
I sjutradan rano ustavši Avram osamari magarca svojega, i uze sa sobom dva momka i Isaka sina svojega; i nacijepavši drva za žrtvu podiže se i poðe na mjesto koje mu kaza Bog.
4 Pa tsiku lachitatu, Abrahamu anakweza maso ake ndipo anaona malowo chapatali.
Treæi dan podigavši oèi svoje Avram ugleda mjesto izdaleka.
5 Ndipo Abrahamu anati kwa antchito ake aja, “Bakhalani pano ndi buluyu. Ine ndi mnyamatayu tipita uko kukapemphera, koma tibweranso.”
I reèe Avram momcima svojim: ostanite vi ovdje s magarcem, a ja i dijete idemo onamo, pa kad se pomolimo Bogu, vratiæemo se k vama.
6 Abrahamu anatenga nkhuni za nsembe yopsereza zija namusenzetsa mwana wake Isake, ndipo iye mwini anatenga moto ndi mpeni. Pamene awiriwo amayendera pamodzi,
I uzevši Avram drva za žrtvu naprti Isaku sinu svojemu, a sam uze u svoje ruke ognja i nož; pa otidoše obojica zajedno.
7 Isake anati kwa abambo ake Abrahamu, “Abambo?” Abrahamu anayankha, “Ee mwana wanga.” Isake anafunsa, “Moto ndi nkhuni zilipo, koma nanga mwana wankhosa wa nsembe yopsereza ali kuti?”
Tada reèe Isak Avramu ocu svojemu: oèe! A on reèe: što, sine! I reèe Isak: eto ognja i drva, a gdje je jagnje za žrtvu?
8 Abrahamu anayankha, “Mwana wanga, Mulungu adzipezera yekha mwana wankhosa wa nsembe yopsereza.” Ndipo awiriwo anapitiriza ulendo.
A Avram odgovori: Bog æe se, sinko, postarati za jagnje sebi na žrtvu. I iðahu obojica zajedno.
9 Atafika pamalo pamene Mulungu anamuwuza paja, Abrahamu anamangapo guwa lansembe nayika nkhuni pamwamba pa guwapo. Kenaka anamumanga mwana wake Isake namugoneka paguwapo, pamwamba pa nkhuni paja.
A kad doðoše na mjesto koje mu Bog kaza, Avram naèini ondje žrtvenik, i metnu drva na nj, i svezavši Isaka sina svojega metnu ga na žrtvenik vrh drva;
10 Kenaka Abrahamu anatambasula dzanja lake natenga mpeni kuti aphe mwana wake.
I izmahnu Avram rukom svojom i uze nož da zakolje sina svojega.
11 Koma mngelo wa Yehova anayitana Abrahamu kuchokera kumwamba nati, “Abrahamu! Abrahamu!” Iye anayankha kuti, “Ee Ambuye.”
Ali anðeo Gospodnji viknu ga s neba, i reèe: Avrame! Avrame! A on reèe: evo me.
12 Mngeloyo anati, “Usatambasulire mwanayo dzanja lako kuti umuphe, pakuti tsopano ndadziwa kuti iwe umaopa Mulungu. Iwe sunandimane mwana wako mmodzi yekhayo.”
A anðeo reèe: ne diži ruke svoje na dijete, i ne èini mu ništa; jer sada poznah da se bojiš Boga, kad nijesi požalio sina svojega, jedinca svojega, mene radi.
13 Abrahamu anatukula maso ake ndipo anaona nkhosa yamphongo itakoledwa ndi nyanga zake mu ziyangoyango. Iye anapita nakatenga nkhosa ija ndikuyipha ngati nsembe yopsereza mʼmalo mwa mwana wake.
I Avram podigavši oèi svoje pogleda; i gle, ovan iza njega zapleo se u èesti rogovima; i otišavši Avram uze ovna i spali ga na žrtvu mjesto sina svojega.
14 Choncho Abrahamu anatcha malo amenewa kuti Yehova-Yire (Wopereka). Ndipo mpaka lero amatchula malowo kuti ndi “Pa phiri la Yehova wopereka.”
I nazva Avram ono mjesto: Gospod æe se postarati. Zato se i danas kaže: na brdu, gdje æe se Gospod postarati.
15 Mngelo wa Yehova anayitana Abrahamu kuchokera kumwamba kachiwiri
I anðeo Gospodnji opet viknu s neba Avrama.
16 ndipo anati, “Ndikulumbira mwa Ine ndekha kuti popeza wachita zimenezi, wosandikaniza mwana wako mmodzi yekhayu,
I reèe: sobom se zakleh, veli Gospod: kad si tako uèinio, i nijesi požalio sina svojega, jedinca svojega,
17 ndidzakudalitsa ndithu ndipo ndidzakupatsa zidzukulu zochuluka ngati nyenyezi zamlengalenga komanso ngati mchenga wa mʼmphepete mwa nyanja. Zidzukulu zako zidzalanda mizinda ya adani awo,
Zaista æu te blagosloviti i sjeme tvoje veoma umnožiti, da ga bude kao zvijezda na nebu i kao pijeska na brijegu morskom; i naslijediæe sjeme tvoje vrata neprijatelja svojih.
18 ndipo kudzera mwa chidzukulu chako, mitundu yonse ya anthu pa dziko lapansi idzadalitsika, chifukwa iwe wandimvera.”
I blagosloviæe se u sjemenu tvojem svi narodi na zemlji, kad si poslušao glas moj.
19 Kenaka Abrahamu anabwerera kumene anasiya antchito ake kuja nanyamukira nawo pamodzi kupita ku Beeriseba. Ndipo Abrahamu anakhala ku Beeriseba.
Tada se Avram vrati k momcima svojim, te se digoše, i otidoše zajedno u Virsaveju, jer Avram življaše u Virsaveji.
20 Patapita nthawi, Abrahamu anamva kuti, “Milika nayenso anaberekera Nahori, mʼbale wake ana.
Poslije toga javiše Avramu govoreæi: gle, i Melha rodi sinove bratu tvojemu Nahoru:
21 Woyamba anali Huzi ndipo kenaka mʼbale wake Buzi. Anaberekanso Kemueli, amene anali abambo ake a Aramu.
Uza prvenca i Vuza brata mu, i Kamuila, oca Avramova,
22 Ana ena ndi Kesede Hazo, Pilidasi, Yidilafi ndi Betueli.”
I Hazada i Azava i Faldesa i Jeldafa i Vatuila.
23 Betueli anabereka Rebeka. Milika anaberekera Nahori, mʼbale wake wa Abrahamu, ana aamuna asanu ndi atatu amenewa.
A Vatuilo rodi Reveku. Osam ih rodi Melha Nahoru bratu Avramovu.
24 Mkazi wake wachiwiri, dzina lake Reuma, anamubaliranso Nahori ana awa: Teba, Gahamu, Tahasi ndi Maaka.
A inoèa njegova, po imenu Revma, rodi i ona Taveka i Gama i Tohosa i Moha.

< Genesis 22 >