< Deuteronomo 15 >

1 Kumapeto kwa zaka zisanu ndi ziwiri zilizonse, muzikhululukirana ngongole.
Svake sedme godine opraštaj.
2 Zimenezi muzichita motere: wobwereketsa aliyense adzakhululukira ngongole imene anabwereketsa kwa Mwisraeli mnzake. Iye asadzafunenso kuti Mwisraeli mnzakeyo kapena mʼbale wake amubwezere chifukwa nthawi ya Ambuye yokhululukirana ngongole yalengezedwa.
A opraštanje da biva ovako: kome je ko dužan što, neka oprosti što bi mogao tražiti od bližnjega svojega; neka ne traži od bližnjega svojega i od brata svojega, jer je opraštanje Gospodnje oglašeno.
3 Mukhoza kulonjerera ngongole kwa mlendo, koma mukhululukire ngongole ina iliyonse imene mʼbale wanu ali nayo.
Od tuðina traži, ali što bi imao u brata svojega, ono neka mu oprosti ruka tvoja,
4 Komabe pasadzakhale wosauka pakati panu chifukwa Yehova Mulungu wanu adzakudalitsani kwambiri mʼdziko limene adzakupatsani kuti likhale lanu ngati cholowa chanu.
Da ne bi bilo siromaha meðu vama, jer æe te obilno blagosloviti Gospod u zemlji koju ti Gospod Bog tvoj da u našljedstvo da je tvoja.
5 Adzakudalitsani pokhapokha ngati mudzamveradi Yehova Mulungu wanu posunga ndi kutsatira malamulo onse amene ndikukupatsani lero.
Samo ako dobro uzaslušaš glas Gospoda Boga svojega gledajuæi da èiniš sve ove zapovijesti, koje ti ja zapovijedam danas,
6 Pakuti Yehova Mulungu wanu adzakudalitsani monga analonjeza, ndipo inu mudzabwereketsa chuma kwa mitundu yambiri ya anthu koma inu simudzabwereka kwa aliyense. Mudzalamulira mitundu yambiri ya anthu koma inuyo palibe amene adzakulamulireni.
Blagosloviæe te Gospod Bog tvoj, kao što ti je kazao, te æeš davati u zajam mnogim narodima, a ni od koga neæeš uzimati u zajam, i vladaæeš mnogim narodima, a oni tobom neæe vladati.
7 Ngati pali mʼbale wanu wina wosauka mu mzinda wanu wina uliwonse mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, musawumitse mitima yanu kapena kuchita kaligwiritsa kwa mʼbale wanu wosaukayo.
Ako bude u tebe koji siromah izmeðu braæe tvoje u kom mjestu tvom, u zemlji tvojoj, koju ti daje Gospod Bog tvoj, nemoj da ti se stvrdne srce tvoje i da stisneš ruku svoju bratu svojemu siromahu.
8 Koma mukhale ofewa manja ndipo mumukongoze mʼbale wanu momasuka pa chilichonse chimene akufuna.
Nego otvori ruku svoju i pozajmi mu rado koliko mu god treba u potrebi njegovoj.
9 Musayesere ndi pangʼono pomwe kusunga maganizo oyipa awa mu mtima mwanu: “Chaka chachisanu ndi chiwiri, chaka chokhululukirana ngongole, chayandikira,” kuti musaonetse mtima woyipa kwa mʼbale wanu wosauka nʼkusamupatsa chilichonse. Iye angadzakunenereni inu mlandu kwa Ambuye, ndipo mudzapezeka wochimwa.
Èuvaj se da ne bude kakvo nevaljalstvo u srcu tvom, pa da reèeš: blizu je sedma godina, godina oprosna; i da oko tvoje ne bude zlo prema bratu tvojemu siromahu, pa da mu ne daš, a on zato da vapije ka Gospodu na te, i bude ti grijeh.
10 Mumupatse iye mowolowamanja ndipo muchite zimenezi mosasungira kanthu kumtima. Tsono chifukwa cha zimenezi, Yehova Mulungu wanu adzakudalitsani pa ntchito zanu zonse ndi pa chilichonse chimene mukhudza.
Podaj mu, i neka ne žali srce tvoje kad mu daš; jer æe za tu stvar blagosloviti tebe Gospod Bog tvoj u svakom poslu tvom i u svemu za što se prihvatiš rukom svojom.
11 Anthu osauka sadzatha mʼdziko lanu. Chomwecho ndikukulamulani kuti mukhale ofewa manja kwa abale anu ndi kwa osauka, osowa mʼdziko mwanu.
Jer neæe biti bez siromaha u zemlji; zato ti zapovijedam i kažem: otvoraj ruku svoju bratu svojemu, nevoljniku i siromahu svojemu u zemlji svojoj.
12 Ngati mʼbale wanu wamwamuna kapena wamkazi adzigulitsa yekha kwa inu, nakugwirirani ntchito zaka zisanu ndi chimodzi, muzimumasula mʼchaka cha chisanu ndi chiwiri.
Ako ti se proda brat tvoj Jevrejin ili Jevrejka, neka ti služi šest godina, a sedme godine otpusti ga od sebe slobodna.
13 Ndipo pamene mumumasula, musangomulola apite chimanjamanja.
A kad ga otpustiš od sebe slobodna, nemoj ga otpustiti prazna.
14 Mumupatse mowolowamanja zochokera pa ziweto zanu, kopunthira tirigu ndi kopsinyira vinyo. Inu mumupatse iye monga Yehova Mulungu wanu wakudalitsirani.
Daruj ga èim izmeðu stoke svoje i s gumna svojega i iz kace svoje; podaj mu èim te je blagoslovio Gospod Bog tvoj.
15 Kumbukirani kuti munali akapolo mʼdziko la Igupto ndipo Yehova Mulungu wanu anakupulumutsani. Nʼchifukwa chake ndikukupatsani lamulo ili lero lino.
I opominji se da si bio rob u zemlji Misirskoj i da te je izbavio Gospod Bog tvoj; zato ti ja zapovijedam ovo danas.
16 Koma ngati kapoloyo akuwuzani kuti, “Ine sindikufuna kumasulidwa,” chifukwa choti wakukondani inuyo pamodzi ndi banja lanu ndiponso kuti kwamukomera iyeyo kuti azikhalabe nanu,
Ako li ti reèe: neæu da idem od tebe, zato što te ljubi i dom tvoj, jer mu je dobro kod tebe,
17 pamenepo muzitenga chobowolera chachitsulo ndi kubowola khutu lake pa chitseko, ndipo mukatero adzakhala kapolo wanu moyo wake wonse. Mdzakazi wanu muzimuchitanso chimodzimodzi.
Tada uzmi šilo i probuši mu uho na vratima, i biæe ti sluga dovijeka; i sluškinji svojoj uèini tako.
18 Musaone ngati chopweteka kumasula wantchito wanu, chifukwa ntchito imene wayigwira pa zaka zisanu ndi chimodzi zimenezi ndi yopindula kawiri pa ntchito imene akanagwira waganyu chabe. Ndipo Yehova Mulungu wanu adzakudalitsani pa chilichonse chimene mukuchita.
Nemoj da ti bude teško kad ga otpuštaš od sebe slobodna, jer je dvojinom onoliko koliko najamnik zaslužio u tebe za šest godina, da bi te blagoslovio Gospod Bog tvoj u svemu što radiš.
19 Mumupatulire Yehova Mulungu wanu choyamba kubadwa chachimuna chilichonse pa ngʼombe ndi nkhosa zanu. Musamazigwiritse ntchito ngʼombe zoyamba kubadwa kapena kumeta nkhosa zoyamba kubadwa.
Sve prvence u stoci svojoj krupnoj i sitnoj što bude muško, posveti Gospodu Bogu svojemu; ne radi na prvencu od krave svoje, i ne strizi prvenca od ovaca svojih.
20 Inuyo ndi banja lanu, chaka chilichonse muzizidya zimenezi pamaso pa Yehova Mulungu wanu pa malo amene Iye adzasankhe.
Pred Gospodom Bogom svojim jedi ih ti i porodica tvoja svake godine na mjestu koje izbere Gospod.
21 Ngati chiweto chili ndi chilema monga kulumala kapena chosaona, kapena ngati chili ndi cholakwika chachikulu chilichonse, musachipereke nsembe kwa Yehova Mulungu wanu.
Ako li na njemu bude mana, ako bude hromo ili slijepo, ili koja god zla mana bude na njemu, ne kolji ga Gospodu Bogu svojemu.
22 Muzichidya mʼmizinda yanuyanu. Onse odetsedwa monga mwa mwambo ndi oyeretsedwa omwe akhoza kuchidya monga akudya gwape kapena mbawala.
U svom mjestu pojedi ga; i èist i neèist neka jede kao srnu i jelena.
23 Koma musadye magazi ake. Muwathire pansi ngati madzi.
Samo krvi od njega ne jedi; prolij je na zemlju kao vodu.

< Deuteronomo 15 >