< Deuteronomo 12 >

1 Awa ndi malangizo ndi malamulo amene muyenera kusamalitsanso kuti muwatsatire mʼdziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu wakupatsani kuti mutenge pa nthawi yonse imene muti mudzakhale mʼdzikomo.
Ovo su uredbe i zakoni koje æete držati i tvoriti u zemlji koju ti je Gospod Bog otaca tvojih dao da je naslijediš, dokle ste god živi na zemlji.
2 Muwonongeretu kwathunthu malo onse a pamwamba pa mapiri ataliatali ndi pa mapiri angʼonoangʼono ndi pansi pa mtengo uliwonse wotambalala pamene mitundu imene muyilande dzikolo ankapembedzerapo milungu yawo.
Raskopajte sasvijem sva mjesta u kojima su služili bogovima svojim narodi koje æete naslijediti, po visokim brdima i po humovima i pod svakijem zelenijem drvetom.
3 Mugumule maguwa awo ansembe, ndi kuphwanya miyala yawo yachipembedzo ndipo mutenthe pa moto mafano awo a Asera: mugwetse mafano a milungu yawo ndi kufafaniza mayina awo mʼmalo amenewo.
Oborite oltare njihove i razbijte likove njihove, i lugove njihove popalite ognjem, i rezane bogove njihove izlomite, i istrijebite ime njihovo iz onoga mjesta.
4 Musapembedze Yehova Mulungu wanu monga mmene amachitira iwowa.
Ne èinite tako Gospodu Bogu svojemu.
5 Koma inu muzifunafuna kumalo kumene Yehova Mulungu wanu adzasankhe pakati pa mafuko anu kuti ayikeko dzina lake ndi kukhalako. Ku malo amenewa muyenera kupitako.
Nego ga tražite u mjestu koje izbere Gospod Bog vaš izmeðu svijeh plemena vaših sebi za stan da ondje namjesti ime svoje, i onamo idite.
6 Kumeneko muzipititsako zopereka zanu ndi nsembe zanu zopsereza, ndi chakhumi chanu ndi mphatso zapadera zimene munalonjeza kupereka ndi zopereka zanu zaufulu ndi ana oyamba a ngʼombe zanu ndi nkhosa zanu.
Onamo nosite žrtve svoje paljenice i druge žrtve svoje i desetke svoje i prinose ruku svojih i zavjete svoje i dragovoljne prinose svoje i prvine od stoke svoje krupne i sitne.
7 Kumeneko, pamaso pa Yehova Mulungu wanu, inu ndi mabanja anu mudzadya ndi kusangalalako pa china chilichonse chimene mudzakhudza, chifukwa Yehova Mulungu wanu wakudalitsani.
I jedite ondje pred Gospodom Bogom svojim, i veselite se vi i porodice vaše svaèim, za što se prihvatite rukom svojom, èim te blagoslovi Gospod Bog tvoj.
8 Musadzachite monga tikuchitira lero lino, aliyense kumachita zimene akuona kuti ndi zoyenera,
Ne èinite kako mi sada ovdje èinimo, što je kome drago.
9 pakuti simunafike ku malo opumulirako ndi ku cholowa chimene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.
Jer još nijeste došli do odmora i našljedstva, koje ti daje Gospod Bog tvoj.
10 Koma mudzawoloka Yorodani ndi kukhazikika mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani ngati cholowa chanu, ndipo Iye adzakupatsani inu mpumulo ku adani anu okuzungulirani kuti mukhale motchinjirizidwa.
Nego kad prijeðete preko Jordana, i stanete živjeti u zemlji koju vam daje Gospod Bog vaš da je naslijedite, i smiri vas od svijeh neprijatelja vaših unaokolo, te stanete živjeti bez straha,
11 Tsono kumalo kumene Yehova Mulungu wanu adzasankhe kuti azikhalako muzikabweretsako chilichonse chimene ndikulamulirani inu: zopereka ndi nsembe zanu zopsereza, chakhumi chanu ndi mphatso zapadera, ndi chuma chanu chonse chosankhika chimene munalonjeza kwa Yehova.
Onda u mjesto koje izbere Gospod Bog vaš da u njemu nastani ime svoje, donosite sve što vam ja zapovijedam, žrtve svoje paljenice i druge žrtve svoje, desetke svoje i prinose ruku svojih i sve što bude najbolje u onome što zavjetujete Gospodu.
12 Ndipo kumeneko inu mukasangalale pamaso pa Yehova Mulungu wanu pamodzi ndi ana anu aamuna ndi ana anu aakazi, antchito anu aamuna ndi adzakazi anu, ndi Alevi a mʼmidzi yanu, amene alibe gawo kapena cholowa chawochawo.
I veselite se pred Gospodom Bogom svojim vi i sinovi vaši i kæeri vaše i sluge vaše i sluškinje vaše, i Levit koji je u mjestu vašem, jer on nema dijela ni našljedstva s vama.
13 Musamalitse kuti musakaphere nsembe zanu zopsereza paliponse pamene mungafune.
Èuvaj se da ne prinosiš žrtava svojih paljenica na kom god mjestu, koje ugledaš;
14 Mukaphere pa malo okhawo amene Yehova adzawasankhe mwa limodzi la mafuko anu, ndipo kumeneko mukasunge chilichonse chimene ndikulamulireni.
Nego na onom mjestu koje izbere Gospod Bog u jednom od tvojih plemena, ondje prinosi žrtve svoje paljenice, i ondje èini sve što ti zapovijedam.
15 Koma mukhoza kumapha ziweto zanu mʼmizinda iliyonse ndi kudya nyama yake mmene mungafunire, ngati kuti ndi agwape kapena mbawala, monga mwadalitso limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani. Woyeretsedwa ndi wosayeretsedwa akhoza kuyidya.
Ali æeš moæi klati i jesti meso kako ti duša zaželi u svakom mjestu svojem po blagoslovu Gospoda Boga svojega, koji ti da; èist i neèist može jesti kao srnu i jelena.
16 Koma musamadye magazi. Muziwathira pansi ngati madzi.
Samo krvi ne jedite; prolijte je na zemlju kao vodu.
17 Musamadyere mʼmizinda yanu chakhumi cha tirigu wanu ndi vinyo watsopano ndi mafuta, kapena za ana oyamba kubadwa a ngʼombe zanu ndi nkhosa zanu, kapena chilichonse chimene mwalonjeza kuchipereka, nsembe zanu zaufulu, kapena mphatso zapadera,
Neæeš moæi jesti u mjestu svojem desetka od žita svojega ni od vina svojega ni od ulja svojega, ni prvina od stoke svoje krupne i sitne, ni onoga što zavjetuješ; ni prinosa dragovoljnijeh, ni prinosa ruku svojih.
18 mʼmalo mwake, muzidya pamaso pa Yehova Mulungu wanu, kumalo kumene Yehova Mulungu wanu adzasankhira inu, ana anu aamuna ndi aakazi, antchito anu aamuna ndi adzakazi anu, ndi Alevi ochokera mʼmizinda yanu, ndipo mudzasangalale pamaso pa Yehova Mulungu wanu pa chilichonse chimene mudzachikhudza.
Nego to jedi pred Gospodom Bogom svojim na mjestu koje izbere Gospod Bog tvoj, ti i sin tvoj i kæi tvoja i sluga tvoj i sluškinja tvoja, i Levit koji je u mjestu tvom; i veseli se pred Gospodom Bogom svojim svaèim za što se prihvatiš rukom.
19 Muonetsetse kuti musawataye Alevi pa masiku onse amene mukhale mʼdziko lanumo.
Èuvaj se da ne ostaviš Levita dok si god živ na zemlji.
20 Yehova Mulungu wanu akadzakulitsa dziko lanu monga anakulonjezerani, ndipo mukapukwa nyama mumanena kuti, “Ndikufuna nyama,” pamenepo mudzadya mmene mungafunire.
Kad raširi Gospod Bog tvoj meðe tvoje, kao što ti je kazao, ako reèeš: da jedem mesa, kad duša tvoja želi da jede mesa, jedi mesa po svoj želji duše svoje.
21 Ngati malo amene Yehova Mulungu wanu awasankha kuti ayike Dzina lake ali kutali kwambiri ndi inu, mukhoza kupha ziweto pakati pa ngʼombe ndi nkhosa zimene Yehova wakupatsani, monga ndinakulamulani, ndipo mʼmizinda yanuyanu mukhoza kuzidya mmene mungafunire.
Ako bi bilo daleko od tebe mjesto koje Gospod Bog tvoj izbere da ondje namjesti ime svoje, zakolji od stoke svoje krupne ili sitne, koju ti da Gospod, kao što sam ti zapovjedio, i jedi u svom mjestu po svoj želji duše svoje.
22 Muzidye ngati mukudya gwape kapena mbawala. Onse oyeretsedwa monga mwa mwambo ndi osayeretsedwa omwe akhoza kudya.
Kako se jede srna i jelen, onako jedi; i èist i neèist neka jede.
23 Koma muonetsetse kuti musadye magazi, chifukwa magazi ndi moyo, ndipo musamadye moyo pamodzi ndi nyama.
Samo pazi da ne jedeš krvi; jer je krv duša, pa ne jedi duše s mesom.
24 Inu musamadye magazi, muziwathira pansi ngati madzi.
Ne jedi je; nego prolij na zemlju kao vodu.
25 Musamadye magazi kuti zikuyendereni bwino inu pamodzi ndi ana anu a pambuyo panu, popeza mudzakhala mukuchita zoyenera pamaso pa Mulungu.
Ne jedi je, da bi dobro bilo tebi i sinovima tvojim nakon tebe, kad èiniš što je ugodno Gospodu.
26 Koma mutenge zinthu zanu zoyeretsedwa ndi china chilichonse chimene munalumbira kupereka, ndi kupita kumalo kumene Yehova adzasankhe.
Ali stvari svoje svete, koje imaš, i što zavjetuješ, uzmi i doði na mjesto koje izbere Gospod.
27 Mupereke nsembe zanu zopsereza pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wanu, nyama pamodzi ndi magazi omwe. Magazi a nsembe zanu athiridwe pambali pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wanu, koma nyamayo mukhoza kudya.
I prinesi žrtve svoje paljenice, meso i krv, na oltaru Gospoda Boga svojega; krv pak od drugih žrtava tvojih neka se prolije na oltar Gospoda Boga tvojega, a meso jedi.
28 Onetsetsani kuti muzimvera mawu onsewa amene ndikukupatsani kuti zinthu zizikuyenderani bwino nthawi zonse inu ndi ana anu chifukwa mudzakhala mukuchita zabwino ndi zoyenera pamaso pa Yehova Mulungu wanu.
Èuvaj i slušaj sve ove rijeèi koje ti ja zapovijedam, da bi dobro bilo tebi i sinovima tvojim nakon tebe dovijeka kad èiniš što je dobro i pravo pred Gospodom Bogom tvojim.
29 Yehova Mulungu wanu adzachotsa pamaso panu mitundu ya anthu amene mukufuna kuwathira nkhondo ndi kuwalanda dzikolo. Koma mukawapirikitsa ndi kukhazikika mʼdziko lawo,
Kad istrijebi Gospod Bog tvoj ispred tebe narode ka kojima ideš da naslijediš zemlju njihovu, i naslijedivši je kad se nastaniš u zemlji njihovoj,
30 ndipo pamene iwo awonongeka pamaso panu, samalirani kuti musakodwe mu msampha pa kufufuza za milungu yawo, nʼkumati, “Kodi anthu a mitunduwa amatumikira bwanji milungu yawo? Ifenso tichita momwemo.”
Èuvaj se da se ne uhvatiš u zamku pošavši za njima pošto se potru ispred tebe, i da ne potražiš bogova njihovijeh, i reèeš: kako su ovi narodi služili svojim bogovima, tako æu i ja èiniti.
31 Musapembedze Yehova Mulungu wanu momwe amachitira iwowo, chifukwa popembedza milungu yawoyo amachita zonyansa zamitundumitundu zimene Yehova amadana nazo. Amatentha ngakhale ana awo aamuna ndi aakazi pa moto ngati nsembe za kwa milungu yawo.
Ne èini tako Gospodu Bogu svojemu; jer oni èiniše svojim bogovima sve što je gadno pred Gospodom i na što on mrzi; jer su i sinove svoje i kæeri svoje sažizali bogovima svojim.
32 Onetsetsani kuti mukuchita zimene ndikukulamulirani. Musawonjezerepo kapena kuchotserapo.
Što vam god ja zapovijedam sve držite i tvorite, niti što dodajte k tome ni oduzmite od toga.

< Deuteronomo 12 >