< 2 Mbiri 22 >

1 Anthu a mu Yerusalemu anayika Ahaziya mwana wamngʼono kwambiri wa Yehoramu kukhala mfumu mʼmalo mwake, popeza gulu lankhondo limene linabwera ndi Aarabu ku misasa, linapha ana onse aakulu. Motero Ahaziya mwana wa Yehoramu mfumu ya Yuda anayamba kulamulira.
A Jerusalimljani zacariše na njegovo mjesto Ohoziju najmlaðega sina njegova, jer starije sve pobi èeta koja doðe s Arapima u oko; i tako Ohozija sin Joramov posta car Judin.
2 Ahaziya anali wa zaka 22 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu chaka chimodzi. Dzina la amayi ake linali Ataliya, chidzukulu cha Omuri.
Imaše Ohozija èetrdeset i dvije godine kad poèe carovati, i carova godinu dana u Jerusalimu. Materi mu bješe ime Gotolija, kæi Amrijeva.
3 Nayenso anayenda mʼnjira ya banja la Ahabu, pakuti amayi ake anamulimbikitsa kuchita zolakwika.
I on hoðaše putovima doma Ahavova, jer ga mati nagovaraše na zla djela.
4 Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova monga momwe banja la Ahabu linachitira, pakuti atamwalira abambo ake, iwo anakhala alangizi ake, kumene kunali kudziwononga kwake.
I èinjaše što je zlo pred Gospodom kao dom Ahavov; jer mu oni bijahu savjetnici po smrti oca njegova na pogibao njegovu.
5 Iyeyo anatsatiranso uphungu wawo pamene anapita ndi Yehoramu, mwana wa Ahabu, mfumu ya Israeli kukachita nkhondo ndi Hazaeli mfumu ya Aramu ku Ramoti Giliyadi. Aaramu anavulaza Yehoramu,
I po njihovu svjetu hodeæi izide s Joramom sinom Ahavovijem carem Izrailjevijem na vojsku na Azaila cara Sirskoga u Ramot Galadski; i ondje Sirci raniše Jorama.
6 kotero iye anabwerera ku Yezireeli kuti akachire mabala amene anamuvulaza ku Ramoti pa nkhondo ndi Hazaeli mfumu ya Aaramu. Ndipo Ahaziya, mwana wa Yehoramu mfumu ya Yuda anapita ku Yezireeli kukaona Yehoramu mwana wa Ahabu chifukwa anavulazidwa.
A on se vrati da se lijeèi u Jezraelu od rana koje mu zadaše u Rami, kad se bijaše s Azailom carem Sirskim. A Azarija sin Joramov car Judin doðe u Jezrael da vidi Jorama sina Ahavova, jer bijaše bolestan.
7 Mulungu anakonza kuti Ahaziya akaphedwe pa ulendo wake wokacheza. Ahaziya atafika, iye ndi Yoramu anapita kukakumana ndi Yehu mwana wa Nimisi, amene Yehova anamudzoza kuti akawononge banja la Ahabu.
Ali bijaše od Boga na propast Ohoziji što doðe k Joramu; jer došav otide s Joramom na Juja sina Nimsijina, kojega Gospod pomaza da istrijebi dom Ahavov.
8 Pamene Yehu ankalanga banja la Ahabu anapeza atsogoleri a ku Yuda ndiponso ana aamuna a abale ake a Ahaziya amene amatumikira Ahaziya, ndipo anawapha.
Jer kad Juj izvršivaše osvetu na domu Ahavovu, naðe knezove Judine i sinove braæe Ohozijine, koji služahu Ohoziji, i pogubi ih.
9 Kenaka anapita kukafunafuna Ahaziya, ndipo anthu ake anagwira Ahaziya pamene amabisala mu Samariya. Anabwera naye kwa Yehu ndipo anaphedwa. Iwo anamuyika mʼmanda, pakuti anati, “Iyeyu anali mwana wa Yehosafati amene anafunafuna Yehova ndi mtima wake wonse.” Kotero panalibe wamphamvu mʼbanja la Ahaziya kuti nʼkukhala mfumu.
Potom potraži Ohoziju, i uhvatiše ga kad se krijaše u Samariji, i dovedavši ga k Juju pogubiše ga, i pogreboše ga; jer rekoše: sin je Josafata koji je tražio Gospoda svijem srcem svojim. I tako ne bi nikoga od doma Ohozijina koji bi mogao biti car.
10 Ataliya, amayi ake a Ahaziya, ataona kuti mwana wawo wafa, ananyamuka nakapha onse a banja laufumu la Yuda.
Zato Gotolija mati Ohozijina vidjevši da joj sin pogibe, usta i pobi sve carsko sjeme doma Judina.
11 Koma Yehoseba, mwana wamkazi wa mfumu Yehoramu, anatenga Yowasi mwana wa Ahaziya, momuba ndi kumuchotsa pakati pa ana aamuna a mfumu amene amati aphedwe ndipo anamuyika iye ndi mlezi wake mʼchipinda chogona. Motero Yehoseba, mwana wamkazi wa mfumu Yehoramu, mkazi wa wansembe Yehoyada, yemwe anali mlongo wake wa Ahaziya anamubisa mwanayo kuti Ataliya asamuphe.
Ali Josaveta kæi careva uze Joasa sina Ohozijina i ukrade ga izmeðu sinova carevijeh, koje ubijahu; i sakri ga s dojkinjom njegovom u ložnicu. I tako Josaveta kæi cara Jorama žena Jodaja sveštenika sakri ga od Gotolije, jer bijaše sestra Ohozijina, te ga ne ubi.
12 Mwanayo anakhala mobisala pamodzi ndi iwo mu Nyumba ya Mulungu kwa zaka zisanu ndi chimodzi muulamuliro wa Ataliya.
I bijaše s njima sakriven u domu Božijem šest godina; a Gotolija carovaše u zemlji.

< 2 Mbiri 22 >