< 1 Mbiri 2 >

1 Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,
Forsothe the sones of Israel weren Ruben, Symeon, Leuy, Juda, Isachar, and Zabulon,
2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
Dan, Joseph, Beniamyn, Neptalym, Gad, Aser.
3 Ana a Yuda anali awa: Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha.
The sones of Juda weren Her, Onam, Sela; these thre weren borun to hym of Sue, a douyter of Canaan. Sotheli Her, the first gendrid sone of Juda, was yuel bifor the Lord, and he killide hym.
4 Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
Forsothe Thamar, wijf of the sone of Judas, childide to hym Phares, and Zaram; therfor alle the sones of Judas weren fyue.
5 Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.
Sotheli the sones of Phares weren Esrom, and Chamul.
6 Ana a Zera anali awa: Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
And the sones of Zare weren Zamry, and Ethen, and Eman, and Calchab, and Dardan; fyue togidere.
7 Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
The sone of Charmy was Achar, that disturblide Israel, and synnede in the theft of thing halewid to the Lord.
8 Mwana wa Etani anali Azariya.
The sone of Ethan was Azarie.
9 Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
Sotheli the sones of Esrom, that weren borun to hym, weren Jeramael, and Aram, and Calubi.
10 Ramu anabereka Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda.
Forsothe Aram gendryde Amynadab. Sotheli Amynadab gendride Naason, the prince of the sones of Juda.
11 Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,
And Naason gendride Salmon; of which Salmon Booz was borun.
12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
Sotheli Booz gendride Obeth; which hym silf gendride Ysay.
13 Yese anabereka Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea,
Forsothe Ysai gendride the firste gendride sone, Elyab, the secounde, Amynadab; the thridde, Samaa;
14 wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,
the fourthe, Nathanael;
15 wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.
the fyuethe, Sadai; the sixte, Asom;
16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.
the seuenthe, Dauyd; whose sistris weren Saruya, and Abigail. The sones of Saruye weren thre, Abisai, Joab, and Asahel.
17 Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
Forsothe Abigail childide Amasa, whos fadir was Gether Hismaelite.
18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.
Sotheli Caleph, sone of Esrom, took a wijf, Azuba bi name, of whom he gendride Jerioth; and hise sones weren Jesar, and Sobab, and Ardon.
19 Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.
And whanne Azuba was deed, Caleph took a wijf Effrata, whiche childide Hur to hym.
20 Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
Forsothe Hur gendride Hury; Hury gendride Beseleel.
21 Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.
After these thingis Esrom entride to the douytir of Machir, fadir of Galaad, and he took hir, whanne he was of sixti yeer; and sche childide Segub to hym.
22 Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.
But also Segub gendride Jair; and he hadde in possessioun thre and twenti citees in the lond of Galaad;
23 (Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
and he took Gessur, and Aran, the citees of Jair, and Chanath, and the townes therof of seuenti citees. Alle these weren the sones of Machir, fadir of Galaad.
24 Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
Sotheli whanne Esrom was deed, Caleph entride in to Effrata. And Esrom hadde a wijf Abia, which childide to hym Assir, fadir of Thecue.
25 Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali: Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya.
Forsothe sones weren borun of Jezrameel, the firste gendrid of Esrom; Ram, the first gendrid of hym, and Aran, and Ason, and Achia.
26 Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
Also Jezrameel weddide anothir wijf, Athara bi name, that was the modir of Onam.
27 Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa: Maazi, Yamini ndi Ekeri.
But and the sones of Ram, the firste gendrid of Jezrameel, weren Mohas, and Jamyn, and Achaz.
28 Ana a Onamu anali awa: Shamai ndi Yada. Ana a Shamai anali awa: Nadabu ndi Abisuri.
Forsothe Onam gendride sones, Semey, and Juda. Sotheli the sones of Semei weren Nadab, and Abisur;
29 Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
forsothe the name of the wijf of Abisur was Abigail, that childide to hym Haaobban, and Molid.
30 Ana a Nadabu anali awa: Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
Sotheli the sones of Nadab weren Saled and Apphaym; forsothe Saled diede without children.
31 Ana a Apaimu anali awa: Isi, amene anabereka Sesani. Sesani anabereka Ahilai.
Sotheli the sone of Apphaym was Jesi, which Jesi gendride Sesan; sotheli Sesan gendride Oholi.
32 Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa: Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
Forsothe the sones of Jada, brother of Semei, weren Jether and Jonathan; but Jether diede with out sones; treuli Jonathan gendride Phalech,
33 Ana a Yonatani anali awa: Peleti ndi Zaza. Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
and Ziza. These ben the sones of Jerameel.
34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.
Forsothe Sesan hadde not sones, but douytris, and a seruaunt of Egipt, Jeraa bi name;
35 Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
and he yaf his douyter to wijf to Jeraa, whiche childide Ethei to hym.
36 Atayi anali abambo ake a Natani, Natani anali abambo ake a Zabadi,
Forsothe Ethei gendride Nathan, and Nathan gendride Zadab.
37 Zabadi anali abambo a Efilali, Efilali anali abambo a Obedi,
Also Zadab gendride Ophial, and Ophial gendride Obed.
38 Obedi anali abambo a Yehu, Yehu anali abambo a Azariya,
Obed gendride Yeu, Yeu gendride Azarie,
39 Azariya anali abambo a Helezi, Helezi anali abambo a Eleasa,
Azarie gendride Helles, Helles gendride Elasa,
40 Eleasa anali abambo ake a Sisimai, Sisimai anali abambo a Salumu,
Elasa gendride Sesamoy, Sesamoy gendride Sellum,
41 Salumu anali abambo a Yekamiya, Yekamiya anali abambo a Elisama.
Sellum gendride Jecamya, Jecamia gendride Elisama.
42 Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa: Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
Forsothe the sones of Caleph, brothir of Jerameel, weren Mosa, the firste gendrid sone of hym; thilke is the fadir of Ziph; and the sones of Maresa, the fadir of Hebron.
43 Ana a Hebroni anali awa: Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema.
Certis the sones of Ebron weren Chore, and Raphu, Recem, and Samma.
44 Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.
Forsothe Samma gendride Raam, the fadir of Jerechaam; and Recem gendride Semei.
45 Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
The sone of Semei was Maon; and Maon was the fadir of Bethsur.
46 Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
Sotheli Epha, the secundarie wijf of Caleph, childide Aram, and Musa, and Theser; forsothe Aram gendride Jezen.
47 Ana a Yahidai anali awa: Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
The sones of Jadai weren Regon, and Jethon, and Zesum, Phalez, and Epha, and Saaph.
48 Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.
Matha, the secoundarie wijf of Caleph, childide Zaber, and Tharana.
49 Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.
Forsothe Saaph, the fadir of Madmenas, gendride Sue, the fadir of Magbena, and the fader of Gabaa; sotheli the douyter of Caleph was Axa.
50 Izi zinali zidzukulu za Kalebe. Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa: Sobala abambo a Kiriati Yearimu,
These weren the sones of Caleph. The sones of Hur, the firste gendrid sone of Effrata, weren Sobal, the fader of Cariathiarim;
51 Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
Salma, the fader of Bethleem; Ariph, the fader of Bethgader.
52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,
Sotheli the sones of Sobal, fader of Cariatiarim, that siy the myddil of restingis,
53 ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
and was of the kynrede of Caryathiarym, weren Jethrey, and Aphutei, and Samathei, and Maserathei. Of these weren borun Sarytis, and Eschaolitis.
54 Zidzukulu za Salima zinali izi: Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori,
The sones of Salma, fadir of Bethleem, and of Netophati, weren the corouns of the hows of Joab, and the half of restyng of Sarai.
55 ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.
And the kynredis of scryuens, dwellynge in Jabes, syngynge, and sownynge, and dwellynge in tabernaclis. These ben Cyneis, that camen of the heete of the fadir of the hows of Rechab.

< 1 Mbiri 2 >