< Masalimo 1 >

1 Wodala munthu amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa, kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa, kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
Thlak che a cuihnaak awh amak cet man, thlak thawlhkhqi a ceh lam awh amak dyi man, huhsit qaihsaikhqi ang ngawihnaak awh amak ngawi man thlang taw a zoseen hy.
2 Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
A awmhlynaak taw Bawipa a cawngpyinaak awi awh awm nawh, ce cawngpyinaak awi ce than dai poek poepa hy.
3 Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi, umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake ndipo masamba ake safota. Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
Anih taw tui keng awhkaw thing ling, qah tym awh ak qah, a hah amak reu man ing lo qu nawh, a ik-oeih sainaak a hoei awh laang poepa hy.
4 Sizitero ndi anthu oyipa! Iwo ali ngati mungu umene umawuluzidwa ndi mphepo.
Thlak chekhqi taw cemyihna am awm kawm uh! A mingmih taw canghi zilh ing a zawn amyihna ni ami awm.
5 Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo, kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
Cedawngawh thlak chekhqi taw awidengnaak awh am dyi thai kawm u saw, thlak thawlhkhqi awm thlakdyngkhqi ang cunnaak awh am dyi thai ti kawm uh.
6 Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama, koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.
Bawipa ing thlakdyngkhqi a lam ce sim hy, cehlai thlak chekhqi a lam taw plawci kaw.

< Masalimo 1 >