< Miyambo 25 >

1 Iyi ndi miyambo inanso ya Solomoni, imene anthu a Hezekiya mfumu ya ku Yuda analemba.
Ve awm Solomon ak awicyih, Juda sangpahrang Hezekiah ak thlangkhqi ing a mi qee tlaih ni.
2 Ulemerero wa Mulungu uli pa kubisa zinthu; ulemerero wa mafumu uli pa kufufuza zinthuzo.
Ik-oeih thuh taw Khawsa a boeimangnaakna awm nawh, sangpahrang a boeimangnaak taw ce ak thuh qu sui nawh pho sak ni.
3 Monga momwe kwatalikira kumwamba ndi momwe kulili kuzama kwa dziko lapansi, ndi momwemonso alili maganizo a mfumu kusadziwika kwake.
Khan ve saang soeih nawh, dek awm dung soeih nawh, sangpahrangkhqi kawlung awm sim boeih hly kawi am ni.
4 Chotsa zoyipa mʼsiliva ndipo wosula adzapanga naye ziwiya.
Ngun eek ce meet lah, cawhtaw ngun ak sepkung hamna them ak leek soeihna coeng kaw.
5 Chotsa munthu woyipa pamaso pa mfumu; ndipo ufumu wake udzakhazikika mu chilungamo.
Sangpahrang haiawh thlak thawlh ce thoeng unawh, a sangpahrang ngawihdoelh ce dyngnaak ing cak sakna awm kaw.
6 Usamadzikuze ukakhala pamaso pa mfumu, ndipo usamakhale pamalo pa anthu apamwamba;
Sangpahrang haiawh namah ingkaw namah koeh kyihcah qu nawh, boeikhqi a haiawh hyn koeh lo.
7 paja ndi bwino kuti mfumu ichite kukuwuza kuti, “Bwera pamwamba pano,” kulekana ndi kuti ikuchititse manyazi chifukwa cha wina wokuposa. Chimene wachiona ndi maso ako,
Na huh khawi boei a haiawh chah na phyih anglakawh “ngawihnaak ak leekawh ngawi lah,” a mi nitinaak ce leek bet hy.
8 usafulumire kupita nacho ku bwalo la milandu nanga udzachita chiyani pa mapeto pake ngati mnansi wako adzakuchititsa manyazi?
Khqah qu ham hqii koeh tawn sak, a huna na imcengkhqi ing chah a mini phyih sak awhtaw, ikaw na sai hly am sim kawp ti.
9 Kamba mlandu ndi mnansi wako, koma osawulula chinsinsi cha munthu wina
Na kawnglam ce na imceng ingqawi kqawn haih nih nawh, thlakchang ak awihyp mah koeh pho kawp ti.
10 kuopa kuti wina akamva mawu ako adzakuchititsa manyazi ndipo mbiri yako yoyipa sidzatha.
A nik sim ing ni zyi kawm saw, nang ming seetnaak am qeeng thai kaw.
11 Mawu amodzi woyankhulidwa moyenera ali ngati zokongoletsera zagolide mʼzotengera zasiliva.
Ak thymna awi kqawn balh taw ngun bawm awhkaw sui thaih ing myih hy.
12 Kwa munthu womvetsa bwino, kudzudzula kwa munthu wanzeru kuli ngati ndolo zagolide kapena chodzikongoletsera china cha golide wabwino kwambiri.
Ak ngaikung ang haawh thlakcyi ak awi kqawn taw sui hathen ing sui ak leek soeih aawi ingqawi myih hy.
13 Wamthenga wodalirika ali ngati madzi ozizira pa nthawi yokolola kwa anthu amene amutuma; iye amaziziritsa mtima bwana wake.
Ak tyikungkhqi ham dyihthing ypawm taw caang ah tym awhkaw daam tui ing myih nawh, a boei ak kaw caih sak hy.
14 Munthu wonyadira mphatso imene sayipereka ali ngati mitambo ndi mphepo yopanda mvula.
A mapek ak pena ak kqawn qu nawh, ak oe qu taw amak aa cingmai ingkaw khawhli ing myih hy.
15 Kupirira ndiye kumagonjetsa mfumu, ndipo kufewa mʼkamwa kutha kumafatsitsa munthu wowuma mtima.
Kawdungnaak ing ukkung kaw dawm sak thai nawh, awih neem ing quh awm ek sak thai hy.
16 Ngati upeza uchi, ingodya okukwanira, kuopa ungakoledwe nawo ndi kuyamba kusanza.
Khawitui na hu lek? Khoek neh sak nawh aw, a ni lawnnaak dy na ai awhtaw laawk kawp ti.
17 Uzipita kamodzikamodzi ku nyumba ya mnzako ukawirikiza kupita, udzadana naye.
Na imceng venna koeh plam aih, ning huuna nawh ni sawhna lat kaw.
18 Munthu wochitira mnzake umboni wonama, ali ngati chibonga kapena lupanga kapena muvi wakuthwa.
A imceng ak khanawh ak thym simpyikung na amak dyi taw thingboeng, cimca ingkaw pala ak hqaat ing myih hy.
19 Kudalira munthu wosankhulupirika pa nthawi ya mavuto, kuli ngati dzino lobowoka kapena phazi lolumala.
Kyinaak huhawh amak ypawm thlang ak yp naak taw haa ak ek ingkaw khaw ak khoem ing myih hy.
20 Kuyimbira nyimbo munthu wachisoni kuli ngati kuvula zovala pa nyengo yozizira kapena kuthira mchere pa chilonda.
Thlang ak kawsee venna hla ak sakung taw chikca awh thlang angki suh pek ingkaw thui hqoep awh kuuk sak ing myih hy.
21 Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye; ngati ali ndi ludzu mupatse madzi kuti amwe.
Na qaal phoen a cawih awh buh pe nawh tui a hoet awh aawk kawi tui pe lah,
22 Pochita izi, udzamusenzetsa makala a moto pa mutu pake, ndipo Yehova adzakupatsa mphotho.
Ceamyihna na sai awhtaw a lukhanawh maih eh ling na tloeng pek ing myih kawm saw, Bawipa ing zoseennaak ni pe kaw.
23 Monga momwe mphepo yampoto imabweretsera mvula, chonchonso mjedu umadzetsa mkwiyo.
Asiip ben nakaw zilh ing khawkaa a lawpyi amyihna thlang ak theet ing kawsonaak lawpyi hy.
24 Nʼkwabwino kukhala pa ngodya ya denga kuposa kukhala mʼnyumba ndi mkazi wolongolola.
Nu, hqo ak lo poepa ingqawi imkhui oet awh awm haih anglakawh iptih kilawh awm leek bet hy.
25 Mthenga wabwino wochokera ku dziko lakutali ali ngati madzi ozizira kwa munthu waludzu.
Khawkhla nakaw awithang leek taw thlang tui ak hoet ham tuiding ing myih hy.
26 Munthu wolungama amene amagonjera munthu woyipa ali ngati kasupe wodzaza ndi matope kapena chitsime cha madzi oyipa.
Thlakdyng, thlakche lam ak pleeng taw khawcui awhkaw deknaawng ingkaw tuih nuu ing myih hy.
27 Sibwino kudya uchi wambiri, sibwinonso kudzifunira wekha ulemu.
Khawitui khawzah aawk am leek nawh, cemyih koepna thlang amah ham kyihcahnaak ak sui taw thlang leek am ni.
28 Munthu amene samatha kudziretsa ali ngati mzinda umene adani awuthyola ndi kuwusiya wopanda malinga.
Thlang amah ak kawlung amak doen noeng taw vawngchungnaak ak tlu khaw ing myih hy.

< Miyambo 25 >