< Зәбур 15 >

1 Давут язған күй: — Пәрвәрдигар, ким чедириңда туралайду? Ким пак-муқәддәс теғиңда маканлишиду?
Salimo la Davide. Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika? Kodi ndani angathe kukhala mʼphiri lanu loyera?
2 Кимки тамамән дуруслуқта маңса, Һәққанийлиқни жүргүзсә, Көңлидә һәқиқәтни сөзлисә;
Munthu wa makhalidwe abwino, amene amachita zolungama, woyankhula choonadi chochokera mu mtima mwake,
3 Тили билән гәп тошумиса, Өз йеқиниға яманлиқ қилмиса, Хошнисиниң әйивини колап ачмиса,
ndipo mʼkamwa mwake simutuluka mawu osinjirira, amene sachitira choyipa mnansi wake kapena kufalitsa mbiri yoyipa ya munthu mnzake,
4 Пәс адәмни көзгә илмиса, Пәрвәрдигардин әйминидиғанларни һөрмәтлисә, Өзигә зиянлиқ болған тәғдирдиму ичкән қәсимини өзгәртмисә,
amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa. Koma amalemekeza amene amaopa Yehova, amene amakwaniritsa zomwe walonjeza ngakhale pamene zikumupweteka,
5 Пулни хәқләргә өсүмгә бәрмисә, Бигуналарниң зийиниға пара алмиса; Кимки мошуларни қилса, Мәңгүгә тәврәнмәс.
amene amakongoletsa ndalama zake popanda chiwongoladzanja ndipo salandira chiphuphu pofuna kutsutsa anthu osalakwa. Iye amene amachita zinthu zimenezi sadzagwedezeka konse.

< Зәбур 15 >