< Markos 14 >

1 Fısıh ve Mayasız Ekmek Bayramı'na iki gün kalmıştı. Başkâhinlerle din bilginleri İsa'yı hileyle tutuklayıp öldürmenin bir yolunu arıyorlardı.
Tsopano panali patatsala masiku awiri okha kuti tsiku la Paska ndi Phwando la Buledi wopanda yisiti lifike, ndipo akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo ankafunafuna mpata woti amugwire Yesu ndi kumupha.
2 “Bayramda olmasın, yoksa halk arasında kargaşalık çıkar” diyorlardı.
Iwo anati, “Koma osati nthawi yaphwando, chifukwa anthu angachite chiwawa.”
3 İsa Beytanya'da cüzamlı Simun'un evinde sofrada otururken yanına bir kadın geldi. Kadın kaymaktaşından bir kap içinde çok değerli, saf hintsümbülü yağı getirmişti. Kabı kırarak yağı O'nun başına döktü.
Pamene Iye anali mʼBetaniya, atakhala pa tebulo akudya mʼnyumba ya munthu wodziwika kuti Simoni wakhate, anabwera mayi ndi botolo la mafuta onunkhira amtengo wapamwamba opangidwa ndi nadi. Anaphwanya botololo nakhuthula mafutawo pa mutu wa Yesu.
4 Bazıları buna kızdılar; birbirlerine, “Bu yağ niçin böyle boş yere harcandı? Üç yüz dinardan fazlaya satılabilir, parası yoksullara verilebilirdi” diyerek kadını azarlamaya başladılar.
Ena mwa iwo amene analipo, anakwiya nati kwa wina ndi mnzake, “Chifukwa chiyani akuwononga mafuta onunkhirawa?
5
Akanatheka kugulitsidwa ndi ndalama zambiri zoposa malipiro a pa chaka ndipo ndalamazo ndi kupatsa osauka.” Ndipo anamudzudzula iye mwaukali.
6 “Kadını rahat bırakın” dedi İsa. “Neden üzüyorsunuz onu? Benim için güzel bir şey yaptı.
Yesu anati, “Musiyeni, chifukwa chiyani mukumuvutitsa? Wandichitira Ine chinthu chabwino.
7 Yoksullar her zaman aranızdadır, dilediğiniz anda onlara yardım edebilirsiniz; ama ben her zaman aranızda olmayacağım.
Anthu osauka mudzakhala nawo nthawi zonse, ndipo mukhoza kuwathandiza nthawi iliyonse mungafune. Koma simudzakhala ndi Ine nthawi zonse.
8 Kadın elinden geleni yaptı, beni gömülmeye hazırlamak üzere daha şimdiden bedenimi yağladı.
Wachita zimene akanatha. Wathira mafuta onunkhira pa thupi langa nthawi isanakwane kukonzekera kuyikidwa kwanga mʼmanda.
9 Size doğrusunu söyleyeyim, Müjde dünyanın neresinde duyurulursa, bu kadının yaptığı da onun anılması için anlatılacak.”
Zoonadi, ndikuwuzani kuti kulikonse kumene Uthenga Wabwino udzalalikidwa pa dziko lonse, zimene wachitazi zidzanenedwa pomukumbukira iye.”
10 Bu arada Onikiler'den biri olan Yahuda İskariot, İsa'yı ele vermek amacıyla başkâhinlerin yanına gitti.
Kenaka Yudasi Isikarioti, mmodzi mwa khumi ndi awiriwo, anapita kwa akulu a ansembe kuti akamupereke Yesu.
11 Onlar bunu işitince sevindiler, Yahuda'ya para vermeyi vaat ettiler. O da İsa'yı ele vermek için fırsat kollamaya başladı.
Iwo anakondwa pakumva zimenezi ndipo analonjeza kumupatsa iye ndalama. Ndipo ankadikira mpata wabwino woti amupereke.
12 Fısıh kurbanının kesildiği Mayasız Ekmek Bayramı'nın ilk günü öğrencileri İsa'ya, “Fısıh yemeğini yemen için nereye gidip hazırlık yapmamızı istersin?” diye sordular.
Pa tsiku loyamba la Phwando la Buledi wopanda yisiti, nthawi imene mwa mwambo inali ya kupha mwana wankhosa wa Paska, ophunzira a Yesu anafunsa Iye kuti, “Mufuna tipite kuti kumene tikakonzekere kuti mukadyere Paska?”
13 O da öğrencilerinden ikisini şu sözlerle önden gönderdi: “Kente gidin, orada su testisi taşıyan bir adam çıkacak karşınıza. Onu izleyin.
Pamenepo anatumiza awiri mwa ophunzira ake, nawawuza kuti, “Pitani mu mzinda, ndipo mukakumana ndi mwamuna wonyamula mtsuko wa madzi. Kamutsatireni iye.
14 Adamın gideceği evin sahibine şöyle deyin: ‘Öğretmen, öğrencilerimle birlikte Fısıh yemeğini yiyeceğim konuk odası nerede? diye soruyor.’
Kawuzeni mwini nyumba imene iye akalowemo kuti, ‘Aphunzitsi akufunsa: kodi chili kuti chipinda changa cha alendo, kumene ndidyere Paska ndi ophunzira anga?’
15 Ev sahibi size üst katta döşenmiş, hazır büyük bir oda gösterecek. Orada bizim için hazırlık yapın.”
Iye adzakuonetsani chipinda chachikulu chapamwamba, chokhala kale ndi zonse ndi chokonzedwa kale. Katikonzereni ife Paska kumeneko.”
16 Öğrenciler yola çıkıp kente gittiler. Her şeyi, İsa'nın kendilerine söylediği gibi buldular ve Fısıh yemeği için hazırlık yaptılar.
Ophunzirawo anachoka, napita mu mzindawo ndipo anakapeza zinthu monga mmene Yesu anawawuzira. Choncho anakakonza Paska.
17 Akşam olunca İsa Onikiler'le birlikte geldi.
Ndipo kutada Yesu anafika ndi khumi ndi awiriwo.
18 Sofraya oturmuş yemek yerlerken İsa, “Size doğrusunu söyleyeyim” dedi, “Sizden biri, benimle yemek yiyen biri bana ihanet edecek.”
Pamene ankadya pa tebulo Iye anati, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti mmodzi wa inu adzandipereka, mmodzi amene akudya ndi Ine.”
19 Onlar da kederlenerek birer birer kendisine, “Beni demek istemedin ya?” diye sormaya başladılar.
Iwo anamva chisoni, ndipo mmodzi ndi mmodzi anati kwa Iye, “Kodi ndine?”
20 İsa onlara, “Onikiler'den biridir, ekmeğini benimle birlikte sahana batırandır” dedi.
Iye anayankha kuti, “Ndi mmodzi mwa khumi ndi awirinu, amene akusunsa buledi mʼmbale pamodzi ndi Ine.
21 “Evet, İnsanoğlu kendisi için yazılmış olduğu gibi gidiyor, ama İnsanoğlu'na ihanet edenin vay haline! O adam hiç doğmamış olsaydı, kendisi için daha iyi olurdu.”
Mwana wa Munthu adzapita monga momwe zinalembedwera za Iye. Koma tsoka kwa munthu amene adzapereka Mwana wa Munthu! Kukanakhala bwino kwa iye akanapanda kubadwa.”
22 İsa yemek sırasında eline ekmek aldı, şükredip ekmeği böldü ve, “Alın, bu benim bedenimdir” diyerek öğrencilerine verdi.
Pamene ankadya, Yesu anatenga buledi, nayamika ndipo anamunyema nagawira ophunzira ake nanena kuti, “Tengani, ili ndi thupi langa.”
23 Sonra bir kâse alıp şükretti ve bunu öğrencilerine verdi. Hepsi bundan içti.
Kenaka anatenga chikho, nayamika nachipereka kwa iwo ndipo onse anamweramo.
24 “Bu benim kanım” dedi İsa, “Birçokları uğruna akıtılan antlaşma kanıdır.
Iye anawawuza kuti, “Awa ndi magazi anga a pangano amene akhetsedwa chifukwa cha ambiri.
25 Size doğrusunu söyleyeyim, Tanrı'nın Egemenliği'nde yenisini içeceğim o güne dek, asmanın ürününden bir daha içmeyeceğim.”
Zoonadi, ndikuwuzani kuti sindidzamwanso kuchokera ku chipatso cha mphesa mpaka tsikulo pamene ndidzamwa chatsopano mu ufumu wa Mulungu.”
26 İlahi söyledikten sonra dışarı çıkıp Zeytin Dağı'na doğru gittiler.
Atayimba nyimbo, anapita ku phiri la Olivi.
27 Bu arada İsa öğrencilerine, “Hepiniz sendeleyip düşeceksiniz” dedi. “Çünkü şöyle yazılmıştır: ‘Çobanı vuracağım, Koyunlar darmadağın olacak.’
Yesu anati, “Nonse mudzandithawa, pakuti kwalembedwa: “‘Kantha Mʼbusa, ndipo nkhosa zidzabalalika.’
28 Ama ben dirildikten sonra sizden önce Celile'ye gideceğim.”
Koma ndikadzauka, ndidzatsogola kupita ku Galileya.”
29 Petrus O'na, “Herkes sendeleyip düşse bile ben düşmem” dedi.
Petro anati, “Ngakhale onse adzakuthaweni, ine sindidzatero.”
30 “Sana doğrusunu söyleyeyim” dedi İsa, “Bugün, bu gece, horoz iki kez ötmeden sen beni üç kez inkâr edeceksin.”
Yesu anayankha kuti, “Zoona ndikukuwuza kuti lero lino, usiku uno, tambala asanalire kawiri, iweyo udzandikana katatu.”
31 Ama Petrus üsteleyerek, “Seninle birlikte ölmem gerekse bile seni asla inkâr etmem” dedi. Öğrencilerin hepsi de aynı şeyi söyledi.
Koma Petro ananenetsa kuti, “Ngakhale kutakhala kufa nanu, ine sindidzakukanani.” Ndipo ena onse ananena chimodzimodzi.
32 Sonra Getsemani denilen yere geldiler. İsa öğrencilerine, “Ben dua ederken siz burada oturun” dedi.
Ndipo anapita ku malo otchedwa Getsemani, ndipo Yesu anati kwa ophunzira ake, “Khalani pano pamene Ine ndi kupemphera.”
33 Petrus'u, Yakup'u ve Yuhanna'yı yanına aldı. Hüzünlenmeye ve ağır bir sıkıntı duymaya başlamıştı.
Iye anatenga Petro, Yakobo ndi Yohane, ndipo anayamba kumva chisoni kwambiri ndi kuvutika mu mtima.
34 Onlara, “Ölesiye kederliyim” dedi. “Burada kalın, uyanık durun.”
Iye anawawuza kuti, “Moyo wanga wagwidwa ndi chisoni chofa nacho. Khalani pano ndipo musagone.”
35 Biraz ilerledi, yüzüstü yere kapanıp dua etmeye başladı. “Mümkünse o saati yaşamayayım” dedi.
Atapita patsogolo pangʼono, anagwa pansi ndi kupemphera kuti ngati ndi kotheka oralo limupitirire.
36 “Abba, Baba, senin için her şey mümkün, bu kâseyi benden uzaklaştır. Ama benim değil, senin istediğin olsun.”
Iye anati, “Abba, Atate, zinthu zonse ndi zotheka ndi Inu. Chotsereni chikhochi. Komabe chitani zimene Inu mukufuna, osati zimene Ine ndikufuna.”
37 Öğrencilerinin yanına döndüğünde onları uyumuş buldu. Petrus'a, “Simun” dedi, “Uyuyor musun? Bir saat uyanık kalamadın mı?
Kenaka anabwerera kwa ophunzira ake ndipo anawapeza akugona, Iye anati kwa Petro, “Simoni, kodi uli mtulo? Kodi simukanatha kukhala maso kwa ora limodzi?
38 Uyanık durup dua edin ki, ayartılmayasınız. Ruh isteklidir, ama beden güçsüzdür.”
Khalani tcheru ndi kupemphera kuti musalowe mʼmayesero. Mzimu ukufuna, koma thupi ndi lofowoka.”
39 Yine uzaklaştı, aynı sözleri tekrarlayarak dua etti.
Kenakanso anachoka ndi kukapemphera chimodzimodzi.
40 Geri geldiğinde öğrencilerini yine uyumuş buldu. Onların göz kapaklarına ağırlık çökmüştü. İsa'ya ne diyeceklerini bilemiyorlardı.
Iye atabwerera, anawapezanso akugona, chifukwa mʼmaso mwawo munadzaza tulo. Iwo sanadziwe choti anene kwa Iye.
41 İsa üçüncü kez yanlarına döndü, “Hâlâ uyuyor, dinleniyor musunuz?” dedi. “Yeter! Saat geldi. İşte İnsanoğlu günahkârların eline veriliyor.
Atabweranso kachitatu, anawafunsa kuti, “Kodi mukugonabe ndi kupumula? Pakwana! Nthawi yafika. Taonani, Mwana wa Munthu akuperekedwa mʼmanja mwa anthu ochimwa.
42 Kalkın, gidelim. İşte bana ihanet eden geldi!”
Nyamukani! Tiyeni tizipita! Uyu wondipereka Ine wafika!”
43 Tam o anda, İsa daha konuşurken, Onikiler'den biri olan Yahuda çıkageldi. Yanında başkâhinler, din bilginleri ve ileri gelenler tarafından gönderilmiş kılıçlı sopalı bir kalabalık vardı.
Iye akuyankhulabe, Yudasi, mmodzi mwa khumi ndi awiriwo, anatulukira. Anali ndi gulu la anthu litanyamula malupanga ndi zibonga, otumidwa ndi akulu a ansembe, aphunzitsi amalamulo, ndi akuluakulu.
44 İsa'ya ihanet eden Yahuda, “Kimi öpersem, İsa O'dur. O'nu tutuklayın, güvenlik altına alıp götürün” diye onlarla sözleşmişti.
Tsopano womupereka anapangana chizindikiro ndi iwo kuti: “Amene ndikapsompsone ndi iyeyo; mukamugwire ndi kumutenga ali womangidwa.”
45 Gelir gelmez İsa'ya yaklaştı, “Rabbî” diyerek O'nu öptü.
Atapita kwa Yesu nthawi yomweyo, Yudasi anati, “Aphunzitsi,” ndipo anapsompsona.
46 Onlar da İsa'yı yakalayıp tutukladılar.
Anthu anamugwira Yesu ndi kumumanga.
47 İsa'nın yanında bulunanlardan biri kılıcını çekti, başkâhinin kölesine vurup kulağını uçurdu.
Kenaka mmodzi wa iwo amene anayima pafupipo anatulutsa lupanga lake nakhapa wantchito wa wamkulu wa ansembe, nʼkudula khutu lake.
48 İsa onlara, “Niçin bir haydutmuşum gibi beni kılıç ve sopalarla yakalamaya geldiniz?” dedi.
Yesu anati, “Kodi Ine ndikutsogolera gulu lowukira, kuti mubwera ndi malupanga ndi zibonga kudzandigwira?
49 “Her gün tapınakta, yanıbaşınızda öğretiyordum, beni tutuklamadınız. Ama bu, Kutsal Yazılar yerine gelsin diye oldu.”
Tsiku ndi tsiku ndinali ndi inu, kuphunzitsa mʼmabwalo a Nyumba ya Mulungu, koma inu simunandigwire. Koma malemba ayenera kukwaniritsidwa.”
50 O zaman öğrencilerinin hepsi O'nu bırakıp kaçtı.
Pamenepo ophunzira ake onse anathawa namusiya yekha.
51 İsa'nın ardından sadece keten beze sarınmış bir genç gidiyordu. Bu genç de yakalandı.
Mnyamata wamngʼono amene anangofundira nsalu yokha, wopanda chovala ankamutsatira Yesu. Atamugwira,
52 Ama keten bezden sıyrılıp çıplak olarak kaçtı.
anathawa wamaliseche kusiya nsalu yake mʼmbuyo.
53 İsa'yı görevli başkâhine götürdüler. Bütün başkâhinler, ileri gelenler ve din bilginleri de orada toplandı.
Anamutengera Yesu kwa mkulu wa ansembe, ndipo akulu a ansembe, akuluakulu ndi aphunzitsi amalamulo anasonkhana pamodzi.
54 Petrus, İsa'yı başkâhinin avlusuna kadar uzaktan izledi. Avluda nöbetçilerle birlikte ateşin başında oturup ısınmaya başladı.
Petro anamutsatira ali patali, mpaka ku bwalo la mkulu wa ansembe. Kumeneko anakhala pansi ndi alonda namawotha moto.
55 Başkâhinler ve Yüksek Kurul'un öteki üyeleri, İsa'yı ölüm cezasına çarptırmak için kendisine karşı tanık arıyor, ama bulamıyorlardı.
Akulu a ansembe ndi onse olamulira a Ayuda ankafunafuna umboni womutsutsa Yesu kuti amuphe, koma sanapeze wina uliwonse.
56 Birçok kişi O'na karşı yalan yere tanıklık ettiyse de, tanıklıkları birbirini tutmadı.
Ambiri anamunenera Iye maumboni abodza, koma maumboni awo sanagwirizane.
57 Bazıları kalkıp O'na karşı yalan yere şöyle tanıklık ettiler: “Biz O'nun, ‘Elle yapılmış bu tapınağı yıkacağım ve üç günde, elle yapılmamış başka bir tapınak kuracağım’ dediğini işittik.”
Kenaka ena anayimirira namunenera umboni wonama womutsutsa Iye kunena kuti,
“Tamumva akunena kuti, ‘Ndidzawononga Nyumba ya Mulungu iyi yopangidwa ndi anthu ndipo mʼmasiku atatu ndidzamanga ina, osati yopangidwa ndi munthu.’”
59 Ama bu noktada bile tanıklıkları birbirini tutmadı.
Ngakhale iwonso umboni wawo sunagwirizane.
60 Sonra başkâhin topluluğun ortasında ayağa kalkarak İsa'ya, “Hiç yanıt vermeyecek misin? Nedir bunların sana karşı ettiği bu tanıklıklar?” diye sordu.
Kenaka mkulu wa ansembe anayimirira pakati pawo namufunsa Yesu kuti, “Kodi suyankha? Kodi umboni uwu ndi wotani umene anthu akukuchitira?”
61 Ne var ki, İsa susmaya devam etti, hiç yanıt vermedi. Başkâhin O'na yeniden, “Yüce Olan'ın Oğlu Mesih sen misin?” diye sordu.
Koma Yesu anakhala chete ndipo sanayankhe. Mkulu wa ansembe anabwereza kumufunsa Iye kuti, “Kodi ndiwe Khristu Mwana wa Wodalitsikayo?”
62 İsa, “Benim” dedi. “Ve sizler, İnsanoğlu'nun Kudretli Olan'ın sağında oturduğunu ve göğün bulutlarıyla geldiğini göreceksiniz.”
Yesu anati, “Ndine, ndipo mudzaona Mwana wa Munthu atakhala kudzanja lamanja la Wamphamvuzonse ndipo akubwera mʼmitambo ya kumwamba.”
63 Başkâhin giysilerini yırtarak, “Artık tanıklara ne ihtiyacımız var?” dedi. “Küfürü işittiniz. Buna ne diyorsunuz?” Hepsi İsa'nın ölüm cezasını hak ettiğine karar verdiler.
Mkulu wa ansembe anangʼamba zovala zaunsembe zake. Iye anafunsa kuti, “Chifukwa chiyani tikufuna mboni zinanso?
Mwamva mwanowo. Muganiza chiyani?” Onse anavomereza kuti ndi woyenera imfa.
65 Bazıları O'nun üzerine tükürmeye, gözlerini bağlayarak O'nu yumruklamaya başladılar. “Haydi, peygamberliğini göster!” diyorlardı. Nöbetçiler de O'nu aralarına alıp tokatladılar.
Kenaka ena anayamba kumulavulira malovu; anamumanga mʼmaso, namumenya ndi zibakera ndipo anati, “Nenera!” Ndipo asilikali anamutenga namumenya.
66 Petrus aşağıda, avludayken, başkâhinin hizmetçi kızlarından biri geldi. Isınmakta olan Petrus'u görünce onu dikkatle süzüp, “Sen de Nasıralı İsa'yla birlikteydin” dedi.
Petro ali chakumunsi kwa bwalo la milandu, mmodzi wa atsikana a ntchito a mkulu wa ansembe anabwera.
Ataona Petro akuwotha moto, anamuyangʼanitsitsa. Iye anati, “Iwenso unali pamodzi ndi Mnazareti, Yesu.”
68 Petrus ise bunu inkâr ederek, “Senin neden söz ettiğini bilmiyorum, anlamıyorum” dedi ve dışarıya, dış kapının önüne çıktı. Bu arada horoz öttü.
Koma iye anakana nati, “Sindikudziwa kapena kumvetsetsa zimene ukuyankhula.” Ndipo anachoka napita ku chipata.
69 Hizmetçi kız Petrus'u görünce çevrede duranlara yine, “Bu adam onlardan biri” demeye başladı.
Pamene mtsikana wantchitoyo anamuona iye, anatinso kwa iwo amene anayimirira pomwepo, “Munthu uyu ndi mmodzi mwa iwo.”
70 Petrus tekrar inkâr etti. Çevrede duranlar az sonra Petrus'a yine, “Gerçekten onlardansın; sen de Celileli'sin” dediler.
Anakananso kachiwiri. Patapita kanthawi pangʼono, amene anayimirira pafupi anati kwa Petro, “Zoonadi ndiwe mmodzi wa iwo, pakuti ndiwe mu Galileya.”
71 Petrus kendine lanet okuyup ant içerek, “Sözünü ettiğiniz o adamı tanımıyorum” dedi.
Iye anayamba kudzitemberera, nalumbira kuti, “Sindimudziwa munthu ameneyu.”
72 Tam o anda horoz ikinci kez öttü. Petrus, İsa'nın kendisine, “Horoz iki kez ötmeden beni üç kez inkâr edeceksin” dediğini hatırladı ve hüngür hüngür ağlamaya başladı.
Nthawi yomweyo tambala analira kachiwiri. Pamenepo Petro anakumbukira mawu amene Yesu ananena anamuwuza kuti, “Tambala asanalire kawiri, iwe udzandikana katatu.” Ndipo iye anasweka mtima nayamba kulira.

< Markos 14 >