< Псалтирь 129 >

1 Песнь восхождения. Много теснили меня от юности моей, да скажет Израиль:
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,” anene tsono Israeli;
2 много теснили меня от юности моей, но не одолели меня.
“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga, koma sanandipambane.
3 На хребте моем орали оратаи, проводили длинные борозды свои.
Anthu otipula analima pa msana panga ndipo anapangapo mizere yayitali:
4 Но Господь праведен: Он рассек узы нечестивых.
Koma Yehova ndi wolungama; Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.”
5 Да постыдятся и обратятся назад все ненавидящие Сион!
Onse amene amadana ndi Ziyoni abwezedwe pambuyo mwamanyazi.
6 Да будут, как трава на кровлях, которая прежде, нежели будет исторгнута, засыхает,
Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba, umene umafota usanakule;
7 которою жнец не наполнит руки своей, и вяжущий снопы - горсти своей;
sungadzaze manja a owumweta kapena manja a omanga mitolo.
8 и проходящие мимо не скажут: “благословение Господне на вас; благословляем вас именем Господним!”
Odutsa pafupi asanene kuti, “Dalitso la Yehova lili pa inu; tikukudalitsani mʼdzina la Yehova.”

< Псалтирь 129 >