< Psalmów 66 >

1 Przedniejszemu śpiewakowi pieśń psalmu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo. Fuwulani kwa Mulungu ndi chimwemwe, dziko lonse lapansi!
2 Wykrzykuj Bogu wszystka ziemo! Śpiewajcież psalmy na chwałę imienia jego, ogłaszajcie sławę i chwałę jego.
Imbani ulemerero wa dzina lake; kumutamanda kwake kukhale kwaulemerero.
3 Rzeczcież Bogu: Jakoś straszny w sprawach twoich! Dla wielkości mocy twojej obłudnieć się podadzą nieprzyjaciele twoi.
Nenani kwa Mulungu, “Ntchito zanu ndi zoopsa ndithu! Mphamvu yanu ndi yayikulu kwambiri kotero kuti adani anu amawerama pamaso panu.
4 Wszystkać się ziemia kłaniać, i śpiewać ci będzie; psalm śpiewać będzie imieniowi twemu. (Sela)
Dziko lonse lapansi limaweramira inu; limayimba matamando kwa Inu; limayimba matamando pa dzina lanu.” (Sela)
5 Pójdźcież, a oglądajcie sprawy Boże; straszny jest w sprawach swoich przy synach ludzkich.
Bwerani mudzaone zimene Mulungu wachita, ntchito zanu ndi zoopsa ndithu pakati pa anthu.
6 Obrócił morze w ziemię suchą; rzekę przeszli suchą nogą; tameśmyć się weselili w nim.
Iye anasandutsa nyanja kukhala malo owuma, iwo anawoloka pa madzi ndi mapazi. Bwerani, tiyeni tikondwere mwa Iye.
7 Panuje w mocy swej na wieki; oczy jego patrzą na narody, odporni nie wywyższą się. (Sela)
Iye amalamulira ndi mphamvu zake mpaka muyaya, maso ake amayangʼanira anthu a mitundu ina. Anthu owukira asadzitukumule.
8 Błogosławcież narody Boga naszego, i ogłaszajcie głos chwały jego.
Tamandani Mulungu wathu, inu mitundu ya anthu, mulole kuti mawu a matamando ake amveke;
9 Zachował przy zdrowiu duszę naszę, a nie dał się powinąć nodze naszej.
Iye watchinjiriza miyoyo yathu ndi kusunga mapazi athu kuti angaterereke.
10 Albowiemeś nas doświadczył, o Boże! wypławiłeś nas ogniem, tak jako srebro pławione bywa.
Pakuti Inu Mulungu munatiyesa; munatiyenga ngati siliva.
11 Nagnałeś nas był w sieć, a ścisnąłeś uciskiem biodra nasze.
Inu mwatilowetsa mʼndende ndi kutisenzetsa zolemera pa misana yathu.
12 Wsadziłeś człowieka na głowę naszę; weszliśmy byli w ogień i w wodę, wszakżeś nas wywiódł na ochłodę.
Inu munalola kuti anthu akwere pa mitu yathu; ife tinadutsa mʼmoto ndi mʼmadzi, koma Inu munatibweretsa ku malo a zinthu zochuluka.
13 Przetoż wnijdę do domu twego z całopaleniem, a oddam ci śluby moje.
Ine ndidzabwera ku Nyumba yanu ndi nsembe zopsereza ndi kukwaniritsa malumbiro anga.
14 Któreć ślubowały wargi moje, i wyrzekły usta moje w utrapieniu mojem.
Malumbiro amene milomo yanga inalonjeza ndi pakamwa panga panayankhula pamene ndinali pa mavuto.
15 Całopalenie z tłustych baranów będęć ofiarował z kadzeniem, będęć ofiarował woły i kozły. (Sela)
Ndidzapereka nsembe nyama zonenepa kwa Inu ndi chopereka cha nkhosa zazimuna; ndidzapereka ngʼombe zamphongo ndi mbuzi. (Sela)
16 Pójdźcie, słuchajcie, a będę opowiadał wszystkim, którzy się boicie Boga, co uczynił duszy mojej.
Bwerani ndipo mudzamve inu nonse amene mumaopa Mulungu. Ndidzakuwuzani zimene Iyeyo wandichitira.
17 Do niegom usty swemi wołał, a wywyższałem go językiem moim.
Ndinafuwula kwa Iye ndi pakamwa panga, matamando ake anali pa lilime panga.
18 Bym był patrzał na nieprawość w sercu mojem, nie wysłuchałby był Pan.
Ndikanasekerera tchimo mu mtima mwanga Ambuye sakanamvera;
19 Aleć zaiste wysłuchał Bóg, a był pilen głosu modlitwy mojej.
koma ndithu Mulungu wamvetsera ndipo watchera khutu ku mawu a kupempha kwanga.
20 Błogosławiony Bóg, który nie odrzucił modlitwy mojej, ani odjął miłosierdzia swego odemnie.
Matamando akhale kwa Mulungu amene sanakane pemphero langa kapena kuletsa chikondi chake pa ine!

< Psalmów 66 >