< Psalmów 16 >

1 Złota pieśń Dawidowa.
Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
2 Strzeż mię, o Boże! bo w tobie ufam. Rzecz, duszo moja! Panu: Tyś Pan mój, a dobroć moja nic ci nie pomoże,
Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
3 Ale świętym, którzy są na ziemi, i zacnym, w których wszystko kochanie moje.
Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
4 Rozmnożą się boleści tych, którzy się za cudzym bogiem kwapią; nie ukuszę ze krwi mokrych ofiar ich, ani wezmę imion ich w usta moje.
Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
5 Pan jest cząstką dziedzictwa mego, i kielicha mego, ty zatrzymujesz los mój.
Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
6 Sznury mi przypadły na miejscach wesołych, a dziedzictwo wdzięczne przyszło na mię.
Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
7 Będę błogosławił Pana, który mi dał radę, gdyż i w nocy ćwiczą mię nerki moje.
Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
8 Stawiałem Pana zawsze przed oczyma swemi; a iż on jest po prawicy mojej, nie będę wzruszony.
Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
9 Przetoż uweseliło się serce moje, a rozradowała się chwała moja; dotego ciało moje mieszkać będzie bezpiecznie.
Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
10 Bo nie zostawisz duszy mojej w grobie, ani dopuścisz świętemu twemu oglądać skażenia. (Sheol h7585)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
11 Oznajmisz mi drogę żywota; obfitość wesela jest przed obliczem twojem, rozkoszy po prawicy twojej aż na wieki.
Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.

< Psalmów 16 >