< Jonasza 2 >

1 I modlił się Jonasz Panu, Bogu swemu, we wnętrznościach onej ryby,
Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake.
2 I rzekł: Wołałem z ucisku swego do Pana, a ozwał mi się; z głębokości grobu wołałem, a wysłuchałeś głos mój. (Sheol h7585)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
3 Boś mię wrzucił w głębokość w pośrodek morza, i rzeka ogarnęła mię; wszystkie nawałności twoje i powodzi twoje zwaliły się na mię.
Munandiponya mʼnyanja yozama, mʼkati mwenimweni mwa nyanja, ndipo madzi oyenda anandizungulira; mafunde anu onse ndi mkokomo wake zinandimiza.
4 Jużem był rzekł: Wygnanym jest od oczów twoich, wszakże jeszcze będę patrzał na kościół twój święty.
Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa pamaso panu; komabe ndidzayangʼananso ku Nyumba yanu yopatulika.’
5 Ogarnęły mię wody aż do duszy, przepaść mię ogarnęła, rogożem obwiniona była głowa moja.
Madzi wondimiza anandichititsa mantha, nyanja yozama inandizungulira; udzu wa mʼmadzi zinakuta mutu wanga.
6 Zstąpiłem aż do spodku gór, ziemia się zaworami swemi zawarła nademną na wieki; tyś jednak wywiódł z dołu żywot mój, o Panie, Boże mój!
Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri; mipiringidzo ya dziko inanditsekereza kosatha. Koma Inu munatulutsa moyo wanga mʼmandamo, Inu Yehova Mulungu wanga.
7 Gdy ustawała we mnie dusza moja, wspomniałem na Pana; modlitwa moja przyszła do ciebie, do świętego kościoła twego.
“Pamene moyo wanga umachoka mwa ine, ine ndinakumbukira Inu Yehova, ndipo pemphero langa linafika kwa inu, ku Nyumba yanu yopatulika.
8 Którzy pilnują marności nikczemnych, pozbawiają się miłosierdzia Bożego;
“Iwo amene amagwiritsitsa mafano achabechabe amataya chisomo chawo.
9 Ale ja z głosem dziękczynienia ofiarować ci będę, com ślubował, spełnię; od Pana jest obfite wybawienie.
Koma ine ndidzapereka kwa Inu nsembe ndikuyimba nyimbo yamayamiko. Chimene ndinalonjeza ndidzachikwaniritsa. Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.”
10 I rozkazał Pan onej rybie, a wyrzuciła Jonasza na brzeg.
Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja.

< Jonasza 2 >