< Estery 10 >

1 Potem ułożył król Aswerus podatek na ziemię swoję, i na wyspy morskie.
Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse.
2 Awszystkie sprawy mocy jego, i możności jego, z opisaniem zacności Mardocheuszowej, którą go wielmożnym uczynił król, to zapisano w księgach kronik o królach Medskich i Perskich.
Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya?
3 Albowiem Mardocheusz Żyd był wtórym po królu Aswerusie, i wielkim u Żydów, i zacny u mnóstwa braci swych, starając się o dobro ludu swego, i sprawując pokój wszystkiemu narodowi swemu.
Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.

< Estery 10 >