< II Kronik 16 >

1 Roku trzydziestego i szóstego królowania Azy, wyciągnął Baaza, król Izraelski, przeciwko Judzie, i zbudował Ramę, aby nie dopuścił wychodzić i wchodzić nikomu do Azy, króla Judzkiego.
Mʼchaka cha 36 cha ufumu wa Asa, Baasa mfumu ya Israeli inapita kukathira nkhondo dziko la Yuda. Anamangira mpanda mzinda wa Rama kuletsa aliyense kutuluka kapena kulowa mʼdziko la Asa mfumu ya Yuda.
2 Tedy wziąwszy Aza srebro i złoto ze skarbów domu Pańskiego i domu królewskiego, posłał je do Benadada, króla Syryjskiego, który mieszkał w Damaszku, mówiąc:
Ndipo Asa anatenga siliva ndi golide ku malo osungirako a mʼNyumba ya Mulungu ndi ku nyumba yake yaufumu ndi kuzitumiza kwa Beni-Hadadi mfumu ya Aramu imene inkakhala mu Damasiko.
3 Przymierze jest między mną i między tobą, i między ojcem moim i między ojcem twoim: otoć posyłam srebro i złoto. Idźże, a wzrusz przymierze twoje z Baazą, królem Izraelskim, aby odciągnął odemnie.
Iye anati, “Pakhale pangano pakati pa inu ndi ine, monga zinalili pakati pa abambo anu ndi abambo anga. Taonani, ine ndikutumiza kwa inu siliva ndi golide. Tsopano thetsani mgwirizano wanu ndi Baasa mfumu ya Israeli kuti achoke kwa ine.”
4 I usłuchał Benadad króla Azy, a posławszy hetmanów z wojskami, które miał, przeciwko miastom Izraelskim, zburzył Hijon i Dan i Abelmaim, i wszystkie miasta obronne Neftalimskie, w których były skarby.
Beni-Hadadi anagwirizana ndi mfumu Asa ndipo anatumiza olamulira nkhondo ake kukathira nkhondo mizinda ya Israeli. Iwo anagonjetsa Iyoni, Dani, Abeli-Maimu ndi mizinda yonse yosungira chuma ya Nafutali.
5 To gdy usłyszał Baaza, przestał budować Ramy, i zaniechał roboty swej.
Baasa atamva izi, anasiya kumanga Rama ndipo anayimitsa ntchito yakeyo.
6 Tedy król Aza wziąwszy z sobą wszystek lud Judzki, pobrali z Ramy kamienie, i drzewo jego, z którego budował Baaza, a zbudował z niego Gabaa i Masfa.
Ndipo mfumu Asa anabwera ndi Ayuda onse, ndipo anachotsa miyala ndi matabwa ku Rama amene Baasa amagwiritsa ntchito. Ndi zimenezi Asa ankamangira Geba ndi Mizipa.
7 A onegoż czasu przyszedł Hanani, widzący, do Azy, króla Judzkiego, i mówił do niego: Iżeś spoległ na królu Syryjskim, a nie spoległeś na Panu, Bogu twoim, dlatego uszło wojsko króla Syryjskiego z ręki twojej.
Nthawi imeneyi mlosi Hanani anabwera kwa Asa mfumu ya Yuda ndipo anati kwa iye, “Chifukwa chakuti munadalira mfumu ya Aramu osati Yehova Mulungu wanu, gulu la ankhondo la mfumu ya ku Aramu lapulumuka mʼmanja mwanu.
8 Azaż Etyjopczycy, i Lubimczycy nie mieli wojsk bardzo wielkich z wozami i z jezdnymi w mnóstwie bardzo wielkiem? a wżdy gdyś spoległ na Panu, podał je w rękę twoję.
Kodi Akusi ndi Alibiya sanali gulu lankhondo lamphamvu lokhala ndi magaleta ochuluka ndi okwera magaleta ake? Koma pamene inu munadalira Yehova, Iye anawapereka mʼdzanja lanu.
9 Albowiem oczy Pańskie przepatrują wszystkę ziemię, aby dokazywał mocy swej przy tych, którzy przy nim stoją sercem doskonałem. Głupioś to uczynił: przetoż od tego czasu powstaną przeciwko tobie wojny.
Pakuti Yehova amayangʼana uku ndi uku pa dziko lonse lapansi kuti alimbikitse iwo amene mitima yawo ayipereka kwathunthu kwa Iye. Inu mwachita chinthu chopusa ndipo kuyambira lero mudzakhala pa nkhondo.”
10 Tedy Aza rozgniewawszy się na widzącego, podał go do więzienia; bo się był nań o to rozgniewał; i utrapił Aza niektórych z ludu onego czasu.
Asa anamupsera mtima mlosi uja chifukwa cha izi mwakuti anakwiya kwambiri namuyika mʼndende. Pa nthawi yomweyonso Asa anazunza mwankhanza anthu ena.
11 Ale inne sprawy Azy pierwsze i pośledniejsze, zapisane są w księgach o królach Judzkich i Izraelskich.
Ntchito zina za mfumu Asa, kuyambira pachiyambi mpaka kumapeto zalembedwa mʼbuku la mafumu a Yuda ndi Israeli.
12 Potem rozniemógł się Aza roku trzydziestego i dziewiątego królowania swego, na nogi swoje, chorobą bardzo ciężką; a wszakże w onej chorobie swej nie szukał Pana, ale lekarzy.
Mʼchaka cha 39 cha ufumu wake, Asa anayamba kudwala nthenda ya mapazi. Ngakhale nthendayo inali yaululu kwambiri, komabe iye sanafunefune Yehova, koma anafuna thandizo kwa asingʼanga.
13 A tak zasnął Aza z ojcami swymi, a umarł roku czterdziestego i pierwszego królowania swego.
Ndipo mʼchaka cha 41 cha ufumu wake, Asa anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda pamodzi ndi makolo ake.
14 I pochowano go w grobie jego, który sobie był wykopał w mieście Dawidowem; i położono go na łożu, które był napełnił rzeczami wonnemi, i rozmaitemi maściami aptekarską robotą przygotowanemi. I palili mu zapał wonny bardzo wielki.
Iye anayikidwa mʼmanda amene anadzisemera yekha mu Mzinda wa Davide. Anagoneka mtembo wake pa chithatha chimene anayikapo zonunkhira zamitundumitundu, ndipo anasonkha chimoto chachikulu pomuchitira ulemu.

< II Kronik 16 >