< مزامیر 100 >

ای تمامی روی زمین خداوند راآواز شادمانی دهید. ۱ 1
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
خداوند را باشادی عبادت نمایید و به حضور او با ترنم بیاید. ۲ 2
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
بدانید که یهوه خداست، او ما را آفرید. ما قوم اوهستیم و گوسفندان مرتع او. ۳ 3
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
به دروازه های او باحمد بیایید و به صحنهای او با تسبیح! او را حمدگویید و نام او را متبارک خوانید! ۴ 4
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
زیرا که خداوند نیکوست و رحمت او ابدی و امانت وی تا ابدالاباد. ۵ 5
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.

< مزامیر 100 >