< مزامیر 100 >
ای تمامی روی زمین خداوند راآواز شادمانی دهید. | ۱ 1 |
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
خداوند را باشادی عبادت نمایید و به حضور او با ترنم بیاید. | ۲ 2 |
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
بدانید که یهوه خداست، او ما را آفرید. ما قوم اوهستیم و گوسفندان مرتع او. | ۳ 3 |
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
به دروازه های او باحمد بیایید و به صحنهای او با تسبیح! او را حمدگویید و نام او را متبارک خوانید! | ۴ 4 |
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
زیرا که خداوند نیکوست و رحمت او ابدی و امانت وی تا ابدالاباد. | ۵ 5 |
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.