< 1 USamuyeli 18 >

1 Kwasekusithi eseqedile ukukhuluma loSawuli, umphefumulo kaJonathani wabotshelwa emphefumulweni kaDavida; uJonathani wasemthanda njengomphefumulo wakhe.
Davide atatha kuyankhula ndi Sauli, mtima wa Yonatani unagwirizana ndi mtima wa Davide, ndipo iye ankamukonda Davide monga momwe ankadzikondera yekha.
2 USawuli wasemthatha ngalolosuku, kaze amvumela ukubuyela endlini kayise.
Choncho Sauli anamusunga Davideyo kuyambira tsiku limenelo ndipo sanamulole kuti abwerere ku nyumba ya abambo ake.
3 UJonathani loDavida basebesenza isivumelwano ngoba wamthanda njengomphefumulo wakhe.
Ndipo Yonatani anapanga pangano ndi Davide chifukwa ankamukonda monga momwe ankadzikondera.
4 UJonathani wasezikhulula ibhatshi ayeligqokile, walinika uDavida, lezembatho zakhe, kuze kube senkembeni yakhe, kuze kube sedandilini lakhe, njalo kuze kube sebhantini lakhe.
Yonatani anavula mkanjo umene anavala ndipo anamupatsa Davide pamodzi ndi zovala za nkhondo, lupanga, uta ndi lamba.
5 UDavida wasephuma waya loba ngaphi lapho uSawuli amthuma khona, waziphatha ngenhlakanipho, uSawuli waze wambeka phezu kwamadoda empi. Njalo wayelungile emehlweni abantu bonke njalo lemehlweni ezinceku zikaSawuli.
Davide ankapita kulikonse kumene Sauli ankamutuma kuti apite kukamenya nkhondo, ndipo ankapambana. Choncho Sauli anamupatsa udindo woyangʼanira gulu lankhondo. Ichi chinakondweretsa anthu onse ngakhalenso atsogoleri a nkhondo a Sauli.
6 Kwasekusithi ekufikeni kwabo, uDavida esebuye ekubulaleni umFilisti, abesifazana baphuma emizini yonke yakoIsrayeli, behlabela, begida, ukuhlangabeza uSawuli inkosi ngezigubhu, ngentokozo, langamachacho.
Anthu akubwerera kwawo Davide atapha Mfilisiti uja, amayi anatuluka mʼmizinda yonse ya Israeli, akuyimba ndi kuvina kukachingamira mfumu Sauli. Ankayimba ndi kuvina mokondwa, kwinaku ngʼoma ndi zitoliro zikulira.
7 Abesifazana basebevumelana bedlala bathi: USawuli utshayile izinkulungwane zakhe, kodwa uDavida izinkulungwane zakhe ezingamatshumi.
Amayiwo ankalandizana nyimbo mokondwera namati: “Sauli wapha 1,000, Koma Davide wapha miyandamiyanda.”
8 USawuli wasethukuthela kakhulu, lalelolizwi lalilibi emehlweni akhe, wathi: Banike uDavida izinkulungwane ezingamatshumi, kodwa mina banginika izinkulungwane; usesalelwe ngumbuso kuphela.
Koma Sauli anapsa mtima kwambiri ndipo mawu amenewa anamuyipira. Iye anati, “Iwo amuwerengera Davide miyandamiyanda, koma ine 1,000 okha. Nanga chatsalanso nʼchiyani kuti atenge? Si ufumu basi?”
9 USawuli wasemqaphela uDavida kusukela kulolosuku kusiya phambili.
Ndipo kuyambira tsiku limeneli Sauli ankamuchitira nsanje Davide.
10 Kwasekusithi kusisa umoya omubi ovela kuNkulunkulu wafika ngamandla phezu kukaSawuli, waprofetha phakathi kwendlu; uDavida wasetshaya ichacho ngesandla sakhe njengensuku ngensuku; njalo kwakulomkhonto esandleni sikaSawuli.
Mmawa mwake mzimu woyipa uja unabwera mwamphamvu pa Sauli. Sauli anayamba kubwebweta mʼnyumba mwake. Davide ankamuyimbira zeze monga nthawi zonse. Sauli anali ndi mkondo mʼdzanja lake.
11 USawuli wasewuphosa umkhonto wathi: Ngizammbandakanya uDavida ngitsho emdulini. Kodwa uDavida wavika kabili esuka phambi kwakhe.
Tsono anawuponya mkondowo, namati mu mtima mwake, “Ndimubaya Davide ndi kumukhomera ku khoma.” Koma Davide anawulewa kawiri konse.
12 USawuli wayemesaba-ke uDavida ngoba iNkosi yayilaye, kodwa yayisisukile kuSawuli.
Pambuyo pake Sauli amamuopa Davide chifukwa Yehova anali ndi Davideyo, nʼkumusiya Sauli.
13 Ngakho uSawuli wasemsusa kuye, wambeka waba yinduna yakhe yabayizinkulungwane; njalo wayephuma engena phambi kwabantu.
Kotero Sauli anamuchotsa Davide pamaso pake ndi kumuyika kukhala mtsogoleri wa ankhondo 1,000. Choncho Davide ankapita ndi kubwera akutsogolera ankhondowa.
14 UDavida waseziphatha ngenhlakanipho endleleni zakhe zonke, leNkosi yayilaye.
Davide ankapambana kwambiri pa chilichonse chimene amachita chifukwa Yehova anali naye.
15 Lapho uSawuli ebona ukuthi waziphatha ngenhlakanipho enkulu, wamesaba.
Sauli ataona momwe Davide ankapambanira, iye anamuopa kwambiri.
16 Kodwa uIsrayeli wonke loJuda bamthanda uDavida, ngoba wayephuma engena phambi kwabo.
Koma Aisraeli onse ndi anthu a Yuda ankamukonda Davide chifukwa ankawatsogolera pa nkhondo zawo.
17 USawuli wasesithi kuDavida: Khangela, indodakazi yami endala uMerabi, ngizakunika yona ibe ngumkakho; kuphela bana liqhawe kimi, ulwe izimpi zeNkosi. Ngoba uSawuli wathi: Isandla sami kasingabi phezu kwakhe, kodwa isandla samaFilisti kasibe phezu kwakhe.
Tsiku lina Sauli anawuza Davide kuti, “Nayu Merabi mwana wanga wamkazi wamkulu. Ine ndakupatsa kuti umukwatire. Koma unditumikire molimba mtima pomenya nkhondo za Yehova.” Poteropo Sauli ankanena kuti, “Ndisamuphe ndi manja angawa koma aphedwe ndi Afilisti!”
18 Kodwa uDavida wathi kuSawuli: Ngingubani mina? Lempilo yami iyini, losendo lukababa koIsrayeli, ukuthi ngibe ngumkhwenyana wenkosi?
Ndipo Davide anati kwa Sauli, “Ine ndine yani, ndipo abale anga kapena banja la abambo anga ndife yani mʼdziko la Israeli kuti ndikhale mpongozi wa mfumu?”
19 Kodwa kwathi ngesikhathi uMerabi indodakazi kaSawuli ayezanikwa ngaso uDavida, wayesenikwe uAdriyeli umMehola ukuba ngumkakhe.
Koma pa nthawi yoti Merabi mwana wa Sauli akwatiwe ndi Davide, Sauli anamupereka kwa Adrieli wa ku Mehola kuti amukwatire.
20 UMikhali indodakazi kaSawuli wamthanda-ke uDavida; basebemtshela uSawuli, lalolodaba lwaluqondile emehlweni akhe.
Koma Mikala mwana wamkazi wa Sauli anamukonda Davide ndipo Sauli atamva za zimenezi, anakondwera.
21 USawuli wasesithi: Ngizamnika yena ukuze abe ngumjibila kuye, lokuze isandla samaFilisti simelane laye. Ngakho uSawuli wathi kuDavida: Ngokwesibili uzakuba ngumkhwenyana wami lamuhla.
Sauli ankaganiza kuti, “Ndimupatse amukwatire kuti akhale ngati msampha kwa Davideyo, ndipo adzaphedwe ndi Afilisti.” Choncho Sauli anawuza Davide kachiwiri, “Tsopano udzakhala mkamwini wanga.”
22 USawuli waselaya inceku zakhe wathi: Khulumani loDavida ngensitha lithi: Khangela, inkosi iyathokoza ngawe, lazo zonke inceku zayo ziyakuthanda; ngakho-ke woba ngumkhwenyana wenkosi.
Sauli analamulanso nduna zake kuti, “Muyankhuleni Davide mwamseri ndi kumuwuza kuti, ‘Taona, mfumu imakondwera nawe, ndipo nduna zake zonse zimakukonda. Tsono ukhale mkamwini wa mfumu.’”
23 Izinceku zikaSawuli zasezikhuluma lawomazwi endlebeni zikaDavida. UDavida wasesithi: Kuyinto elula yini emehlweni enu ukuba ngumkhwenyana wenkosi, lokhu mina ngingumuntu ongumyanga lodelelekayo?
Iwo anakamuwuza Davide mawu amenewa, koma Davide anati, “Kodi inu mukuganiza kuti ndi chinthu chapafupi kukhala mpongozi wa mfumu? Ine ndine wosauka ndiponso wosatchuka.”
24 Lenceku zikaSawuli zamtshela zisithi: UDavida wakhuluma ngalindlela.
Nduna za Sauli zinamuwuza zonse zimene anayankha Davide.
25 USawuli wasesithi: Lizakutsho njalo kuDavida lithi: Inkosi kayiloyisi lobolo, kodwa amajwabu aphambili alikhulu amaFilisti, ukuze kuphindiselwe ezitheni zenkosi. Kodwa uSawuli wacabanga ukwenza uDavida awe ngesandla samaFilisti.
Sauli anayankha kuti, “Kamuwuzeni Davide kuti, ‘Mfumu sikufuna malowolo a mtundu wina uliwonse koma timakungu ta msonga za mavalo a Afilisti 100 kuti ilipsire adani ake.’” Maganizo a Sauli anali akuti Davide aphedwe ndi Afilisti.
26 Lapho inceku zakhe zimtshela uDavida lawomazwi, udaba lwalulungile emehlweni kaDavida ukuthi abe ngumkhwenyana wenkosi. Kodwa insuku zazingakagcwaliseki.
Nduna za Saulizo zitamuwuza Davide zimenezi, anakondwera kuti akhale mpongozi wa mfumu. Koma nthawi imene anapatsidwa isanathe,
27 Ngakho uDavida wasukuma wahamba, yena labantu bakhe, basebetshaya phakathi kwamaFilisti amadoda angamakhulu amabili; uDavida waseletha amajwabu awo aphambili, wawasa enkosini ephelele ukuze abe ngumkhwenyana wenkosi. USawuli wasemnika uMikhali indodakazi yakhe ukuthi abe ngumkakhe.
Davide ndi anyamata ake anapita ndi kukapha Afilisti 200. Iye anabwera ndi timakungu tija natipereka tonse kwa mfumu kuti akhale mpongozi wa mfumu. Kotero Sauli anapereka mwana wake wamkazi, Mikala, kwa Davide kuti amukwatire.
28 USawuli wasebona wazi ukuthi iNkosi iloDavida, loMikhali indodakazi yakhe yamthanda.
Sauli atazindikira kuti Yehova anali ndi Davide ndiponso kuti mwana wake Mikala amamukonda Davide,
29 Njalo uSawuli waya lokhu emesaba kakhulu uDavida; njalo uSawuli waba yisitha sikaDavida zonke izinsuku.
iye anapitirirabe kumuopa Davide ndi kumadana naye moyo wake wonse.
30 Iziphathamandla zamaFilisti zaseziphuma; kwasekusithi seziphumile uDavida waziphatha ngenhlakanipho okwedlula zonke izinceku zikaSawuli, laze laduma kakhulu ibizo lakhe.
Nthawi zonse pamene atsogoleri a Afilisti ankatuluka kukamenya nkhondo, Davide ankapambana kuposa nduna zonse za Sauli. Choncho dzina lake linatchuka kwambiri.

< 1 USamuyeli 18 >