< Bharumi 16 >

1 Enimutula kwimwe Fibi omusubhati weswe, oyo ali mukosi wa likanisa elyo Lili Kenkrea,
Ine ndikupereka kwa inu mlongo wathu Febe, mtumiki wa mpingo wa ku Kenkreya.
2 Koleleki ati omutula okumulamila mu Latabhugenyi. Mkole kutya mu je chibhalo Cha bhekilisha, na mwimelegulu amwi nage mu musango gwona gwona elyo alabha no bhukene nalyo. Okubha omwene-ela abhee mukosi wa bhafu, na ku songa yani omwene.
Ine ndikukupemphani kuti mumulandire mwa Ambuye mʼnjira yoyenera oyera mtima ndi kumupatsa thandizo lililonse limene akulifuna kuchokera kwa inu, pakuti iye wakhala thandizo lalikulu kwa anthu ambiri kuphatikiza ine.
3 Mukeshe Priska na Akila, abhakosi bhe milimu anye, mu Kristo Yesu,
Perekani moni kwa Prisila ndi Akura, atumiki anzanga mwa Khristu Yesu.
4 abho ku bhulame bhwani bhabhuutasishe obhulame bhwebhwe abhene. Enisosha isime ku bhene, atali anyela nawe one ku makanisa gona aga Maanga.
Iwo anapereka miyoyo yawo chifukwa cha ine. Osati ine ndekha komanso mipingo yonse ya a mitundu ina ikuyamika.
5 Nulikeshe likanisa elyo Lili Ika ewebhwe. Nuukesishe Epaineto omwendwa wani, oyo ali mwibhulwa wo kwamba wa Kristo mu Asia.
Perekaninso moni kwa mpingo umene umasonkhana mʼnyumba mwawo. Perekani moni kwa mʼbale wanga wokondedwa Epeneto, amene ndi woyamba kukhulupirira Khristu mʼchigawo cha Asiya.
6 Numukeshe Mariamu oyo akolele emilimu kwo kwikomesha ingulu yemwe.
Perekani moni kwa Mariya, amene wakhala akukugwirirani ntchito kwambiri.
7 Nuukesishe Androniko na Yunia, abhabhili bhani, na bhabhoywa amwi nanye. Ni bhaisonga agati gati ya jitumwa, abho one bhanu bhanyilabhie okumumenya Kristo.
Perekani moni kwa Androniko ndi Yuniya abale anga amene anali mʼndende pamodzi ndi ine. Iwo amadziwika ndi atumwi, ndipo iwo anali mwa Khristu ine ndisanakhale.
8 Numukeshe Ampliato, omwendwa wani mu Latabhugenyi.
Perekani moni kwa Ampliato, amene ine ndimamukonda mwa Ambuye.
9 Numukeshe Arbano, omukosi we milimu amwi nanye mu Kristo, na Stakisi omwendwa wani.
Perekani moni kwa Urbano, mtumiki mnzathu mwa Khristu ndi wokondedwa wanga Staku.
10 Numukeshe Apele, unu ekilisibhwe mu Kristo. Nubhakeshe bhona bhanu bhali munyumba ya Aristobulo.
Perekani moni kwa Apele, woyesedwa ndi wovomerezeka mwa Khristu. Perekani moni kwa a mʼbanja la Aristobulo.
11 Nuukesishe Herodioni, omuyili wani. Nubhakeshe bhona abho bhali mu nyumba ya Narkiso, bhanu bhali mu Latabhugenyi.
Perekani moni kwa Herodiona, mʼbale wanga. Perekani moni kwa a mʼbanja la Narkiso amene ali mwa Ambuye.
12 Nuukesishe Trifaina na Trifosa, bhanu abhakola emilimu kwo kwikomesha mu Latabhugenyi. Numukeshe Persisi omwendwa, oyo akolele emilimu myafu ku Latabhugenyi,
Perekani moni kwa Trufena ndi Trufosa, amayi aja amene amagwira ntchito ya Ambuye molimbika. Perekani moni kwa mnzanga wokondedwa Persida, mayi winanso amene wagwira ntchito kwambiri mwa Ambuye.
13 Nuukesishe Rufo, unu asolelwe na Latabhugenyi na nyilamwene wae no wani.
Perekani moni kwa Rufo, wosankhidwa mwa Ambuye, ndi amayi ake, amene akhala amayi anganso.
14 Numukeshe Asinkrito, Flegon, Herme, Patroba, Herman, na bhasu bhona bhanu bhali amwi nabho.
Perekani moni kwa Asunkrito, Felego, Herima, Patroba, Herima ndi abale amene ali nawo pamodzi.
15 Nuunkesishe Filologo na Yulia, Nerea na muyala wabho, na Olimpa, na abhekilisha bhona bhanu bhali amwi nabho.
Perekani moni kwa Filologo, Yuliya, Neriya ndi mlongo wake, ndi Olumpa ndi oyera mtima onse amene ali nawo pamodzi.
16 Nuunkesishe bhuli umwi kwo kunyunyana kwelu. Amakanisa gona mu Kristo agabhakesha.
Mupatsane moni wina ndi mnzake mwachikondi choona. Mipingo yonse ya Khristu ikupereka moni.
17 Woli enibhelembelesha, bhana bhasu, mu kwiganilisha ingulu ya bhanu abhaletelela okwaukana ne bhyo kuganya okulema okubha amwi. Bhanu abhagenda bhatasikene na meigisho ganu mwamalile okwiingisibhwa. Muinduke mubhasokeko.
Abale, ine ndikukupemphani kuti musamale chifukwa cha amene ayambitsa mipatuko ndi kuyika zokhumudwitsa panjira yanu, motsutsana ndi chiphunzitso chimene mwachiphunzira. Muwapewe iwo.
18 Kulwo kubha abhanu lwa bhanu bhatamukolela Kristo Latabhugenyi, mbe nawe jinda jebhwe abhene. Ku misango jebhwe emyololo na isime yo lulimi bhanu abhajigajiga emyoyo ja bhanu bhatana ntambala.
Pakuti otero sakutumikira Ambuye athu Khristu koma zilakolako zawo. Ndi mawu okoma ndi oshashalika iwo amanamiza anthu osalakwa.
19 Kwe chijejekanyo cho bhwolobhe bhwemwe omumukingila bhuli umwi. Kwibhyo, enikondelwa ingulu yemwe, mbe nawe enibhenda emwe mubhe no bhwenge mu bhe kisi, nokulema okubha na intambala imbele ya bhebhibhi.
Aliyense anamva za kumvera kwanu, choncho ndine odzaza ndi chimwemwe chifukwa cha inu. Koma ine ndikufuna kuti inu mukhale anzeru pa zabwino, ndi wopanda cholakwa pa zimene zili zoyipa.
20 Nyamuanga wo mulengelesi atakuko-ola okumusimagisha Shetani emwalo ye bhigele bhyemwe. Echigongo cha Latabhugenyi Yesu Kristo chibhega amwi nemwe.
Mulungu wamtendere adzaphwanya Satana msanga pansi pa mapazi anu. Chisomo cha Ambuye athu Yesu chikhale ndi inu.
21 Timotheo, omukosi we milimu amwi nanye, kabhakesha, na Lukio, Yasoni na Sospeter, abhaili bhani.
Timoteyo, mtumiki mnzanga, akupereka moni. Nawonso, Lusio, Yasoni ndi Sosipatro, abale anga akutero.
22 Anye, Tertio, unu nandikile inyalubha inu, enibhakesha mwisina Lya Latabhugenyi.
Ine Tertio, amene ndalemba kalatayi, ndi kupereka moni mwa Ambuye.
23 Gayo, unu ankumile kisi na kwi Kanisa lyona elibhakesha. Erasto, omubhiki we bhinu bhya mumusi, kabhakesha, amwi na Kwarto unu ali wasu.
Gayo, amene chifukwa cha chisamaliro chake, ine ndi mpingo wonse kuno tikusangalala, akupereka moni. Erasto, amene ndi msungichuma wa mzinda wonse ndiponso mʼbale wathu Kwato, akupereka moni.
Chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu chikhale ndi inu nonse. Ameni.
25 Mbe woli ewae unu ali no bhutulo bhwo kukola mwimelegulu okulubhana ne misango jo bhwana na meigisho aga Yesu Kristo, okulubhana no kuswelulwa kwa ibhisike eyo yalinga iselekelwe kwo mwanya mulela, (aiōnios g166)
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios g166)
26 mbe nawe woli yasweluywe no kukola okumenyekana na maandiko go bhulagi bhwo okulubhana ne bhilagilo bhya Nyamuanga owa kajanende, kwo bhwolobhe bhwe likilisha agati-gati ya Maanga gone? (aiōnios g166)
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios g166)
27 Ku Nyamuanga enyele owo bhumenyi, okulabha ku Yesu Kristo, kubhe na likusho kajanende kone. Amina. (aiōn g165)
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn g165)

< Bharumi 16 >