< Bhakolosai 4 >

1 Bheso bhugenyi, nimusoshega ku bhagaya emisango jinu jili jo bhulengelesi ne ja Jintugwa je kisi. Mumenyele one ati munage Latabhugenyi mu lwile.
Mabwana, antchito anu muzikhala nawo mwachilungamo ndi moyenera, podziwa kuti nanunso muli nawo Ambuye anu mmwamba.
2 Nimugendelelega okukomela mu kusabhwa. Nimutengejenga mwijo mu sime.
Pempherani modzipereka, mukhale atcheru ndiponso oyamika.
3 Nimusabhwega muli amwi ingulu yeswe one, koleleki ati Nyamuanga egule omulyango ingulu yo musango, okwaika imbisike ye chimali eya Kristo. Kunsonga ya linu nibhoyelwe ne bhibhoyelo.
Ndipo muzitipemphereranso ife kuti Mulungu atitsekulire khomo la uthenga wathu, kuti tilalikire chinsinsi cha Khristu, chimene ndine womangidwa nacho mʼndende.
4 Na nimusabhwega ati nitule okuguta abhwelu, lwa kutyo jinyiile okwaika.
Pempherani kuti ndilalikire momveka bwino, monga ndikuyenera.
5 Nimulibhatega mu bhwengeso ku bhaliya bhanu bhali emwila, muguchuse omwana.
Mayendedwe anu pakati pa akunja, akhale anzeru ndipo mugwiritse ntchito mpata uliwonse umene muli nawo.
6 Emisango jemwe na jibhe ne chigongo mu mwanya gwona, na galungwe omunyu katungu Kona, koleleki ati mutule okumenya lwa kutyo kubheile okumusubhya bhuli munu.
Mayankhulidwe anu nthawi zonse akhale odzaza ndi chisomo ndi okoma, kuti mudziwe kuyankha aliyense.
7 Ku misango jinu ejilubhililana nanye, Tikiko kakola jimenyekane kwemwe. Omwene ni wasu omwendwa, omukosi omwiikanyibhwa, no mugaya wejasu mu Latabhugenyi.
Tukiko adzakuwuzani zonse za ine. Iye ndi mʼbale wokondedwa, mtumiki wokhulupirika ndiponso wantchito mnzanga mwa Ambuye.
8 Enimutuma kwemwe ingulu ya linu, ati mutule okumenya emisango jinu ejo kulubhililana neswe one ati mutule okubhatamo omwoyo.
Ine ndikumutumiza kwa inu ndi cholinga choti mudziwe zimene tikukumana nazo ndiponso kuti alimbikitse mitima yanu.
9 Enimutuma amwi na Onesimo, owasu omwendwa omwiikanyibhwa, no oumwi wemwe. Abhajo okubhabhwila bhuli chinu chinu chabhonekene anu.
Iye akubwera ndi Onesimo, mʼbale wathu wokhulupirika ndi wokondedwa, amene ndi mmodzi mwa inu. Iwo adzakuwuzani zonse zimene zikuchitika kuno.
10 Aristarko, omubhoywa wejasu, kabhakesha, one na Marko omwana wa mama-wabho na Bharnabha unu mwalamiye obhwitondi okusoka kwaye, “Nolwo akaja kwemwe, mumulamile,”
Aristariko, wamʼndende mnzanga akupereka moni, Marko akuperekanso moni, msuweni wa Barnaba. (Inu munawuzidwa kale za Iye. Iye akabwera kwanuko, mulandireni).
11 Nawe Yesu one unu kabhilikilwa Yusto. Bhanu bhenyele ni bho olutendo ni bhakosi bhe bhilimu bhejasu ingulu yo bhukama bhwa Nyamuanga. Bhwebhwe bhanu bho kusilisha anye.
Yesu wotchedwa Yusto, akuperekanso moni. Amenewa ndi Ayuda okhawo pakati pa atumiki anzanga mu ufumu wa Mulungu, ndipo aonetsa kuti ndi chitonthozo kwa ine.
12 Epafra one kabhakesha. Omwene ni umwi wemwe na ni mugaya wa Kristo Yesu. Mwenene akomee mu okusabhwa koleleki ati mutule okwimelegulu kwo bhukumiye no kumenyegesha mu kukumila kwe lyenda lyona elya Nyamuanga.
Epafra ndi mmodzi mwa inu ndiponso mtumiki wa Khristu Yesu, akupereka moni. Iyeyu nthawi zonse amakupemphererani mwamphamvu, kuti mukhazikike pa chifuniro chonse cha Mulungu, mukhale okhwima ndi otsimikiza kwathunthu.
13 Kulwo kubha enimubhambalila, ati akomee okukola emilimu ingulu emwe, kubhanu bhali Laodekia, na kubhanu bhali Hierapoli.
Ine ndikumuchitira umboni kuti amagwira ntchito mwamphamvu chifukwa cha inu ndiponso kwa amene ali ku Laodikaya ndi Herapoli.
14 Luka ulya omufumu omwendwa, na Dema abhabhakesha.
Luka, dotolo wathu wokondedwa ndi Dema, akupereka moni.
15 Abhabhakesha abhasu bhanu bhali Laodekia, na Nimfa, na likanisa lilya linu Lili eyo ika ewae.
Perekani moni kwa abale a ku Laodikaya, ndiponso kwa Numfa ndi mpingo wa mʼnyumba mwake.
16 Inyalubha inu alibha yasomwa kwimwe, isomwe one mwi Kanisa lya bhalaodekia, nemwe one mukomeleshe ati omuisoma inyalubha ilya okusoka Laodekia.
Kalata iyi ikawerengedwa pakati panu, muonetsetse kuti ikawerengedwenso ku mpingo wa ku Laodikaya ndipo inunso muwerenge kalata yochokera ku Laodikaya.
17 Yaika kwa Arkipo, “Lola obhufulubhendi bhulya bhunu ulamiye mu Latabhugenyi, ati kukwiile okuikumisha.”
Uzani Arkipo kuti, “Wonetsetsa kuti wamaliza ntchito imene unayilandira mwa Ambuye.”
18 Obhukesha bhunu ni bwo kubhoko kwani Anye omwene -Paulo. Nimujichuke jimboyelo jani. Echigongo chibhe amwi nemwe.
Ine Paulo, ndikulemba ndi dzanja langa moni uwu. Kumbukirani kuti ndili mu unyolo. Chisomo chikhale ndi inu.

< Bhakolosai 4 >