< 1 Cronache 2 >

1 Questi sono i figliuoli d’Israele: Ruben, Simeone, Levi, Giuda, Issacar e Zabulon;
Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,
2 Dan, Giuseppe, Beniamino, Neftali, Gad e Ascer.
Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
3 Figliuoli di Giuda: Er, Onan e Scela; questi tre gli nacquero dalla figliuola di Shua, la Cananea. Er, primogenito di Giuda, era perverso agli occhi dell’Eterno, e l’Eterno lo fece morire.
Ana a Yuda anali awa: Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha.
4 Tamar, nuora di Giuda, gli partorì Perets e Zerach. Totale dei figliuoli di Giuda: cinque.
Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
5 Figliuoli di Perets: Hetsron e Hamul.
Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.
6 Figliuoli di Zerach: Zimri, Ethan, Heman, Calcol e Dara: in tutto, cinque.
Ana a Zera anali awa: Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
7 Figliuoli di Carmi: Acan che conturbò Israele quando commise una infedeltà riguardo all’interdetto.
Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
8 Figliuoli di Ethan: Azaria.
Mwana wa Etani anali Azariya.
9 Figliuoli che nacquero a Hetsron: Jerahmeel, Ram e Kelubai.
Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
10 Ram generò Amminadab; Amminadab generò Nahshon, principe dei figliuoli di Giuda;
Ramu anabereka Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda.
11 e Nahshon generò Salma; e Salma generò Boaz. Boaz generò Obed.
Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,
12 Obed generò Isai.
Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
13 Isai generò Eliab, suo primogenito, Abinadab il secondo, Scimea il terzo,
Yese anabereka Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea,
14 Nethaneel il quarto, Raddai il quinto,
wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,
15 Otsem il sesto, Davide il settimo.
wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.
16 Le loro sorelle erano Tseruia ed Abigail. Figliuoli di Tseruia: Abishai, Joab ed Asael: tre.
Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.
17 Abigail partorì Amasa, il cui padre fu Jether, l’Ismaelita.
Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
18 Caleb figliuolo di Hetsron, ebbe dei figliuoli da Azuba sua moglie, e da Jerioth. Questi sono i figliuoli che ebbe da Azuba: Jescer, Shobab e Ardon.
Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.
19 Azuba morì e Caleb sposò Efrath, che gli partorì Hur.
Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.
20 Hur generò Uri, e Uri generò Betsaleel.
Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
21 Poi Hetsron prese la figliuola di Makir, padre di Galaad; egli avea sessant’anni quando la sposò; ed essa gli partorì Segub.
Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.
22 Segub generò Jair, che ebbe ventitre città nel paese di Galaad.
Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.
23 I Gheshuriti e i Siri presero loro le borgate di Jair, Kenath e i villaggi che ne dipendevano, sessanta città. Tutti cotesti erano figliuoli di Makir, padre di Galaad.
(Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
24 Dopo la morte di Hetsron, avvenuta a Caleb-Efratha, Abiah, moglie di Hetsron, gli partorì Ashhur padre di Tekoa.
Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
25 I figliuoli di Jerahmeel, primogenito di Hetsron, furono: Ram, il primogenito, Buna, Oren ed Otsem, nati da Ahija.
Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali: Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya.
26 Jerahmeel ebbe un’altra moglie, di nome Atara, che fu madre di Onam.
Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
27 I figliuoli di Ram, primogenito di Jerahmeel, furono: Maats, Jamin ed Eker.
Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa: Maazi, Yamini ndi Ekeri.
28 I figliuoli di Onam furono: Shammai e Jada. Figliuoli di Shammai: Nadab e Abishur.
Ana a Onamu anali awa: Shamai ndi Yada. Ana a Shamai anali awa: Nadabu ndi Abisuri.
29 La moglie di Abishur si chiamava Abihail, che gli partorì Ahban e Molid.
Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
30 Figliuoli di Nadab: Seled e Appaim. Seled morì senza figliuoli.
Ana a Nadabu anali awa: Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
31 Figliuoli di Appaim: Jscei. Figliuoli di Jscei: Sceshan. Figliuoli di Sceshan: Ahlai.
Ana a Apaimu anali awa: Isi, amene anabereka Sesani. Sesani anabereka Ahilai.
32 Figliuoli di Jada, fratello di Shammai: Jether e Jonathan. Jether morì senza figliuoli.
Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa: Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
33 Figliuoli di Jonathan: Peleth e Zaza. Questi sono i figliuoli di Jerahmeel.
Ana a Yonatani anali awa: Peleti ndi Zaza. Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
34 Sceshan non ebbe figliuoli, ma sì delle figlie. Sceshan aveva uno schiavo egiziano per nome Jarha.
Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.
35 E Sceshan diede la sua figliuola per moglie a Jarha, suo schiavo; ed essa gli partorì Attai.
Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
36 Attai generò Nathan; Nathan generò Zabad;
Atayi anali abambo ake a Natani, Natani anali abambo ake a Zabadi,
37 Zabad generò Efial; Efial generò Obed;
Zabadi anali abambo a Efilali, Efilali anali abambo a Obedi,
38 Obed generò Jehu; Jehu generò Azaria;
Obedi anali abambo a Yehu, Yehu anali abambo a Azariya,
39 Azaria generò Helets; Helets generò Elasa;
Azariya anali abambo a Helezi, Helezi anali abambo a Eleasa,
40 Elasa generò Sismai; Sismai generò Shallum;
Eleasa anali abambo ake a Sisimai, Sisimai anali abambo a Salumu,
41 Shallum generò Jekamia e Jekamia generò Elishama.
Salumu anali abambo a Yekamiya, Yekamiya anali abambo a Elisama.
42 Figliuoli di Caleb, fratello di Jerahmeel: Mesha, suo primogenito che fu padre di Zif, e i figliuoli di Maresha, che fu padre di Hebron.
Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa: Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
43 Figliuoli di Hebron: Kora, Tappuah, Rekem e Scema.
Ana a Hebroni anali awa: Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema.
44 Scema generò Raham, padre di Jorkeam, Rekem generò Shammai.
Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.
45 Il figliuolo di Shammai fu Maon; e Maon fu il padre di Beth-Tsur.
Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
46 Efa, concubina di Caleb, partorì Haran, Motsa e Gazez. Haran generò Gazez.
Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
47 Figliuoli di Jahdai: Reghem, Jotham, Gheshan, Pelet, Efa e Shaaf.
Ana a Yahidai anali awa: Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
48 Maaca, concubina di Caleb, partorì Sceber e Tirhana.
Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.
49 Partorì anche Shaaf, padre di Madmanna, Sceva, padre di Macbena e padre di Ghibea. La figliuola di Caleb era Acsa.
Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.
50 Questi furono i figliuoli di Caleb: Ben-Hur, primogenito di Efrata, Shobal, padre di Kiriath-Jearim;
Izi zinali zidzukulu za Kalebe. Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa: Sobala abambo a Kiriati Yearimu,
51 Salma, padre di Bethlehem; Haref, padre di Beth-Gader.
Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
52 Shobal, padre di Kiriath-Jearim, ebbe per discendenti: Haroe, e la metà di Menuhoth.
Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,
53 Le famiglie di Kiriath-Jearim furono: gli Ithrei, i Puthei, gli Shumatei e i Mishraei; dalle quali famiglie derivarono gli Tsorathiti e gli Eshtaoliti.
ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
54 Figliuoli di Salma: Bethlehem e i Netofatei, Atroth-Beth-Joab, la metà dei Manahatei, gli Tsoriti.
Zidzukulu za Salima zinali izi: Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori,
55 E le famiglie di scribi che abitavano a Jabets: i Tirathei, gli Scimeathei, i Sucathei. Questi sono i Kenei discesi da Hammath, padre della casa di Recab.
ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.

< 1 Cronache 2 >