< 1 Tawarikh 5 >

1 Ruben adalah anak sulung Yakub. Tetapi karena Ruben telah menodai kehormatan salah seorang selir ayahnya, maka haknya sebagai anak sulung dicabut dan diberikan kepada Yusuf. Meskipun begitu yang terkuat dari antara keturunan Yakub bukan suku Yusuf melainkan suku Yehuda. Bahkan yang pertama-tama menjadi raja seluruh umat Israel adalah dari suku Yehuda itu.
Ana a Rubeni mwana woyamba wa Israeli (iye anali woyamba kubadwa, koma atagona ndi mkazi wamngʼono wa abambo ake, ulemu wake wokhala mwana woyamba unaperekedwa kwa ana a Yosefe. Kotero iye sanalembedwe pa mndandanda wa mayina ngati mwana woyamba kubadwa,
2
ndipo ngakhalenso Yuda anali wamphamvu kwambiri pakati pa abale ake, ndi kuti wolamulira anachokera mwa iye, ulemu wa mwana woyamba kubadwa unaperekedwa kwa Yosefe)
3 Ruben anak sulung Yakub, mempunyai empat anak laki-laki: Henokh, Palu, Hezron dan Karmi.
ana a Rubeni mwana woyamba wa Israeli ndi awa: Hanoki, Palu, Hezironi, ndi Karimi.
4 Inilah urutan keturunan Yoel: Semaya, Gog, Simei, Mikha, Reaya, Baal dan Beera. Beera adalah pemimpin suku Ruben ketika ia ditangkap oleh Tiglat-Pileser raja Asyur, dan dibawa ke pembuangan.
Ana a Yoweli anali awa: Semaya, Gogi, Simei,
5
Mika, Reaya, Baala,
6
ndiponso Beeri, amene Tigilati-Pileseri mfumu ya Asuri anamugwira ukapolo. Mtsogoleri wa fuko la Rubeni anali Beeri.
7 Dalam silsilah tercatat juga kepala-kepala kaum yang berikut ini dalam suku Ruben: Yeiel, Zakharia,
Abale awo mwa mabanja awo, potsata mndandanda wa mʼbado wawo, ndi awa: Yeiyeli, mtsogoleri, Zekariya,
8 dan Bela anak Azas, cucu Sema dari kaum Yoel. Suku Ruben tinggal di Aroer dan di wilayah yang mulai dari Aroer ke arah utara sampai ke Nebo dan Baal-Meon.
ndiponso Bela mwana wa Azazi, mwana wa Sema, mwana wa Yoweli. Iwo ankakhala ku Aroeri mpaka ku Nebo ndi Baala-Meoni.
9 Mereka mempunyai banyak sekali ternak di daerah Gilead. Karena itu, mereka menempati wilayah sebelah timur sampai ke padang gurun yang terbentang sejauh Sungai Efrat.
Iwo anakhala cha kummawa mpaka kukafika polowera mʼchipululu cha mbali ina ya Mtsinje wa Yufurate, chifukwa ziweto zawo zinaswana kwambiri mʼdziko la Giliyadi.
10 Pada zaman Raja Saul, suku Ruben menyerang dan mengalahkan orang Hagri di sebelah timur Gilead, lalu menduduki negeri itu.
Pa nthawi ya Sauli anachita nkhondo ndi Ahagiri ndi kuwagonjetsa. Tsono iwo anakhala mʼmatenti a Ahagiri ku dera lonse la kummawa kwa Giliyadi.
11 Di sebelah utara wilayah suku Ruben tinggal suku Gad di tanah Basan sampai sejauh Salkha di sebelah timur.
Anthu a fuko la Gadi anakhala moyandikana ndi fuko la Rubeni ku Basani mpaka ku Saleka:
12 Dari suku Gad itu Yoel adalah leluhur kaum yang terkemuka, dan Safam adalah leluhur kaum nomor dua. Yaenai dan Safat adalah leluhur kaum-kaum lainnya di Basan.
Mtsogoleri wawo ku Basani anali Yoweli, wachiwiri anali Safamu, kenaka Yanayi ndi Safati.
13 Orang-orang lain dalam suku Gad termasuk dalam tujuh kaum yang berikut ini: Mikhael, Mesulam, Syeba, Yorai, Yakan, Ziya dan Eber.
Abale awo mwa mabanja awo anali awa: Mikayeli, Mesulamu, Seba, Yorayi, Yakani, Ziya ndi Eberi, onse ali asanu ndi awiri.
14 Mereka keturunan Abihail anak Huri. Urutan silsilah mereka dari bawah ke atas adalah sebagai berikut: Abihail, Huri, Yaroah, Gilead, Mikhael, Yesisai, Yahdo, Bus.
Amenewa ndiwo anali ana a Abihaili, mwana wa Huri, mwana wa Yarowa, mwana wa Giliyadi, mwana wa Mikayeli, mwana wa Yesisayi, mwana wa Yahido, mwana wa Buzi.
15 Kepala kaum-kaum itu adalah Ahi anak Abdiel, cucu Guni.
Ahi mwana wa Abdieli, mwana wa Guni, anali mtsogoleri wa banja la makolo awo.
16 Mereka tinggal di wilayah Basan dan Gilead, dan kota-kota di wilayah itu serta di seluruh padang rumput di Saron.
Fuko la Gadi linakhala ku Giliyadi, ku Basani ndi midzi yozugulira, madera onse a msipu a ku Saroni mpaka kumene amalekezera.
17 Silsilah ini dibuat pada zaman Yotam raja Yehuda, dan Yerobeam raja Israel.
Mayina onsewa analembedwa potsata mndandanda wa mibado yawo pa nthawi ya ulamuliro wa Yotamu mfumu ya Yuda ndi Yeroboamu mfumu ya Israeli.
18 Di dalam suku Ruben, Gad dan suku Manasye yang di sebelah timur Yordan ada 44.760 prajurit yang terlatih dan berpengalaman dalam menggunakan perisai, pedang dan busur.
Mafuko a Rubeni, Gadi ndi theka la Manase, anali ndi anthu 44, 760 okonzeka kulowa usilikali; anthu amatupi amphamvu, amene amatha kugwiritsa ntchito chishango ndi lupanga, amene amatha kugwiritsa ntchito uta, amene anaphunzitsidwa kumenya nkhondo.
19 Mereka berperang melawan suku Yetur, Nafis dan Nodab, yaitu suku-suku di dalam bangsa Hagri.
Iwo anachita nkhondo ndi Ahagiri, Yeturi, Nafisi ndi Nodabu.
20 Prajurit-prajurit itu percaya kepada Allah dan minta tolong kepada-Nya, maka Allah mengabulkan permintaan mereka dan memberikan kemenangan kepada mereka atas orang-orang Hagri itu dan sekutu mereka.
Iwowo anathandizidwa polimbana nawo ndipo Mulungu anapereka Ahagiri mʼmanja mwawo; popeza iwo anafuwulira kwa Mulungu pa nkhondopo. Iye anayankha mapemphero awo chifukwa anamudalira.
21 Karena peperangan itu terjadi atas kehendak Allah, maka banyak musuh yang mereka bunuh. Mereka juga menawan 100.000 orang, dan merampas 50.000 unta, 250.000 domba dan 2.000 keledai. Setelah itu mereka menetap di daerah itu sampai pada masa bangsa Israel ditawan dan dibawa ke pembuangan.
Choncho iwo analanda ziweto za Ahagiri: ngamira 50,000, nkhosa ndi mbuzi 250,000 ndi abulu 2,000. Ndiponso anagwira akapolo 100,000,
enanso ambiri anaphedwa, chifukwa nkhondoyo inali ya Mulungu. Ndipo iwo anakhala mʼdzikomo mpaka pa nthawi ya ukapolo.
23 Sebagian suku Manasye tinggal di wilayah Basan sampai ke utara sejauh Baal-Hermon, Senir dan Gunung Hermon. Mereka makin lama makin banyak.
Theka la fuko la Manase linkakhala ku dziko la kummawa kuyambira ku Basani mpaka ku Baala-Herimoni, kumene ndi ku Seniri (Phiri la Herimoni) ndipo anthuwo anali ochuluka kwambiri.
24 Inilah kepala-kepala kaum mereka: Hefer, Yisei, Eliel, Azriel, Yeremia, Hodawya dan Yahdiel. Mereka semua adalah prajurit-prajurit yang perkasa.
Atsogoleri a mabanja awo anali awa: Eferi, Isi, Elieli, Azirieli, Yeremiya, Hodaviya ndi Yahidieli. Iwo anali asilikali olimba mtima, anthu otchuka, ndiponso atsogoleri a mabanja awo.
25 Orang Israel tidak setia kepada Allah yang disembah leluhur mereka. Mereka meninggalkan Dia dan beribadat kepada dewa-dewa bangsa-bangsa yang telah diusir oleh Allah dari negeri Kanaan.
Koma iwo anali osakhulupirika kwa Mulungu wa makolo awo ndipo anadzipereka okha kwa milungu ya anthu okhala mʼdzikomo amene Mulungu anawawononga pamene iwowo ankafika.
26 Karena itu Allah menggerakkan hati Pul raja Asyur, maka pergilah ia menyerbu negeri itu. Pul juga dikenal sebagai Tiglat-Pileser. Lalu suku Ruben, Gad dan suku Manasye yang di sebelah timur Yordan diangkutnya sebagai tawanan dan dibuang ke Halah, Habor, Hara dan ke suatu tempat dekat Sungai Gozan. Di sana mereka tinggal dan menetap sampai hari ini.
Kotero Mulungu wa Israeli anayika mkwiyo mwa Puli mfumu ya Asuri (ameneyu ndi Tigilati-Pileseri mfumu ya Asuri) amene anatenga fuko la Rubeni, Gadi ndi theka la fuko la Manase kupita nawo ku ukapolo. Iye anapita nawo ku Hala, Habori, Hara ndi ku mtsinje wa Gozani, kumene ali mpaka lero lino.

< 1 Tawarikh 5 >