< Dagiti Salmo 21 >

1 Agragrag-o ti ari iti pigsam, O Yahweh! Anian iti panag-ragrag-ona unay iti impaaymo a panangisalakan!
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Inu Yehova, mfumu ikusangalala mu mphamvu yanu, chimwemwe chake nʼchachikuludi pa kupambana kumene mumapereka!
2 Intedmo kenkuana ti tarigagay ti pusona ken saanmo nga impaidam ti kiddaw dagiti bibigna. (Sela)
Inu mwayipatsa zokhumba za mtima wake ndipo simunayimane zopempha za pa milomo yake. (Sela)
3 Ta iyegmo kenkuana ti adu a bendision; kinoronaam ti ulona iti kapupuroan a balitok.
Inu munayilandira ndi madalitso ochuluka ndipo munayiveka chipewa chaufumu chagolide weniweni pa mutu wake.
4 Dinawatna kenka ti biag; intedmo daytoy kenkuana; inikkam isuna iti atiddog nga al-aldaw iti agnanayon nga awan patinggana.
Iye anakupemphani moyo, ndipo munamupatsa masiku ochuluka kwamuyaya.
5 Naindaklan ti dayagna gapu iti balligim, intedmo kenkuana ti kinadayag ken kinatan-ok.
Kudzera mʼzigonjetso zimene munapereka, ulemerero wake ndi waukulu; Inu mwapereka pa iyo ulemerero ndi ufumu.
6 Ta impaayam isuna kadagiti agnanayon a bendision; pinaragsakmo isuna babaen iti rag-o iti presensiam.
Zoonadi Inu mwayipatsa madalitso amuyaya, Inu mwayipatsa chisangalalo ndi chimwemwe chimene chili pamaso panu.
7 Ta agtaltalek ti ari kenni Yahweh; babaen iti kinapudno ti tulag ti Kangangatoan ket saanto isuna a magaraw.
Pakuti mfumu imadalira Yehova; kudzera mʼchikondi chake chosatha cha Wammwambamwamba, iyo sidzagwedezeka.
8 Dayta imam ket tiliwennanto dagiti amin a kabusormo; dayta kannawan nga imam tiliwennanto dagiti manggurgura kenka.
Dzanja lanu lidzayimitsa adani anu onse; dzanja lanu lamanja lidzagwira adani anu.
9 Iti tiempo ti pungtotmo, uramemto ida a kas iti gumilgil-ayab nga orno. Ibusento ida ni Yahweh babaen iti pungtotna, ken alun-unento ida ti apoy.
Pa nthawi ya kuonekera kwanu mudzawasandutsa ngʼanjo yamoto yotentha. Mu ukali wake Yehova adzawameza, ndipo moto wake udzawatha.
10 Dadaelemto dagiti annakda manipud iti daga ken dagiti kaputotanda manipud kadagiti sangkataoan.
Inu mudzawononga ana awo pa dziko lapansi, zidzukulu zawo pakati pa anthu.
11 Ta pinanggeda ti dakes a maibusor kenka; nagpanunotda iti maysa a plano a saanda a pagballaigian!
Ngakhale iwo akukonzereni chiwembu mwa kuchenjera kwawo sadzapambana;
12 Ta pagsanodemto ida, iturongmonto ti bai ti panam iti sangaonanda.
pakuti mudzawapirikitsa ndipo adzaonetsa misana yawo pamene mudzawaloza ndi mivi yanu.
13 Maitantan-okka, O Yahweh, iti kinapigsam; agkantakaminto ken idaydayawmi ti pannakabalinmo.
Mukwezeke Inu Yehova mʼmphamvu yanu, ife tidzayimba nyimbo ndi kutamanda mphamvu yanu.

< Dagiti Salmo 21 >